Balaka Community Radio

Balaka Community Radio Balaka Community Radio is a radio fully owned by the people of Balaka
"LIWU LATHU LA CHITUKUKO"
Private Bag 1, Balaka,Malawi

   #107.4 FM Nduna yazachuma a Joseph Mwanamveka ati pali ndondomeko zosiyanasiyana zomwe boma likutsatira zothandizira ...
03/06/2026



#107.4 FM

Nduna yazachuma a Joseph Mwanamveka ati pali ndondomeko zosiyanasiyana zomwe boma likutsatira zothandizira kukonzaso chuma cha dziko lino.

Poyankhula mu mzinda wa Lilongwe pa mkumano owunikira chuma cha dziko lino ndi nthambi zokhudzidwa, a Mwanamveka ati njirazi zithandizira kuti ndalama zakunja zisamasowe, mankhwala adzipezeka mzipatala komaso kuti ntchito zisamasowe kwa omwe amaliza sukulu zawo za ukachenjede.

Iwo ati unduna wawo uwonetsetsa kuti ukutsatira mfundo zomwe akambirana ku mkumanowu ndicholinga choti zinthu ziyambeso kuyenda bwino.

Wolemba: Joyce Luwani - Lilongwe
(3 June, 2026)

03/06/2026
03/06/2026

8:30 MADZULO ANO

MONGA MNZIKA ZA BOMA LA BALAKA, MUKUGANIZA KUTI TINGAPANGE BWANJI KUTI TAWUNI YATHU YA BALAKA IPITILIRE KUKHALA YAUKHONDO NTHAWI ZONSE?

PELEKANI MAGANIZO ANU POMPANO

   #107.4 FMMalawi has assumed the chairpersonship of the Communications Regulators’ Association of Southern Africa (CRA...
03/06/2026



#107.4 FM

Malawi has assumed the chairpersonship of the Communications Regulators’ Association of Southern Africa (CRASA) for the 2026/27 term.

The role will be led by the Director General of the Malawi Communications Regulatory Authority, Mayamiko Nkoloma, following the association’s 15th Annual General Meeting held in Lilongwe.

CRASA says Malawi will focus on strengthening regional cooperation and regulatory harmonisation, particularly in addressing emerging issues such as artificial intelligence, cybersecurity, digital trade, and advanced network technologies.

Reported by Francis Billiat -Balaka
(03,June,2026)

📢 PUBLIC NOTICEBalaka Community Radio (BCR)Balaka Community Radio (BCR) is located in the town of Balaka, just after Chi...
03/06/2026

📢 PUBLIC NOTICE
Balaka Community Radio (BCR)

Balaka Community Radio (BCR) is located in the town of Balaka, just after Chimalira South Bottles Balaka Depot and before Banja Lamtsogolo.
You can easily identify our premises by the building clearly marked “Balaka Community Radio.”

For more information, please contact:

The Chief Executive Officer
Balaka Community Radio
Private Bag 1
Balaka, Malawi

📞 Calls/WhatsApp:
+265 993 594 211
+265 887 301 555
+265 888 433 997
+265 992 534 766

🌐 Website: www.balakaradio.blogspot.com
📧 Email: [email protected]

A group known as Friends of Balaka District, on 2, November, 2022 donated assorted items to a standard seven 14 year old boy with albinism, Misheck James of Traditional Authority Nsamala, Ntonya village.

UTHENGA WABWINO Balaka Community Radio iyamba kuwulutsa mawu posachedwa ndipo tizimveka kudzera pamilongoti wa 107.4 FMW...
03/06/2026

UTHENGA WABWINO

Balaka Community Radio iyamba kuwulutsa mawu posachedwa ndipo tizimveka kudzera pamilongoti wa 107.4 FM

Wofuna kuziwa Zambiri za wayilesiyi tchayani thenifolo kapena WhatsApp pa nambala izi:
+265993594211 / +265887301555
+265992534766 /+265888433997

Email: [email protected]

03/06/2026

Kodi kwacha bwanji ku Kachenge, Toleza, tchulani komwe muli

  Boma la Malawi lati liyamba kubweretsa kumudzi a Malawi omwe ali mdziko la South Africa omwe apempha kubwerera, kutsat...
02/06/2026




Boma la Malawi lati liyamba kubweretsa kumudzi a Malawi omwe ali mdziko la South Africa omwe apempha kubwerera, kutsatira nkhanza zomwe zikuchitika m’dzikolo.

Unduna owona za ubale wa dziko lino ndi mayiko ena wati zokonzekera zikupitilira ndipo nthawi yoyamba ntchitoyi ilengezedwa posachedwapa.

Udunawu wawuzaso anthu kuti akuyenera kutsatira njira za Boma zokha kudzera ku ofesi ya kazembe yomwe ili mdziko la South Africa.

Wolemba Williams Chande
(02,June,2026)

Kuyambira 8:30 madzulo ano, tiyeninso tikhale limodzi...Tikhala tikucheza ndi Mlakatuli Gogo NASOKO
02/06/2026

Kuyambira 8:30 madzulo ano, tiyeninso tikhale limodzi...
Tikhala tikucheza ndi Mlakatuli Gogo NASOKO

  CHISOMO NKHOMA TSOPANO NDI  MPHUNZITSI WONGOGWILIZIRA WA CRECK SPORTING CLUBChisomo Nkhoma wapanga mbiri pa masewero a...
02/06/2026




CHISOMO NKHOMA TSOPANO NDI MPHUNZITSI WONGOGWILIZIRA WA CRECK SPORTING CLUB

Chisomo Nkhoma wapanga mbiri pa masewero ampira mdziko muno pomwe wasankhidwa kukhala mphunzitsi yekhayo wamkazi mu mpikisano wa FDH Bank Premiership.

Nkhoma wasankhidwa kukhala mphunzitsi wongogwilizira wa timu ya Creck Sporting Club ndipo walowa mmalo mwa Eliya Kananji yemwe wayimitsidwa ntchito.

Kananji yemwe anali mphunzitsi wamkulu wa timuyi ndi wothandizira wake Harry Saidi ayimitsidwa chifukwa cha kusachita bwino kwa timuyi mu mpikisano wa FDH Bank Premiership.

Mlembi Wamkulu wa timuyi, Aaron Mtaya, watsimikizira nkhaniyi ndipo sadafotokoze ngati anthuwa adzabwererenso mu timuyi.

Timu ya Creck Sporting ili pansi pa tebulo la magulu 16 a FDH Bank Premiership, ndipo ili ndi ma points awiri okha m'masewero asanu ndi limodzi.

Wolemba Tendayi Chabvunguma
(02,June,2026)

Address

Private Bag 1
Balaka
PRIVATEBAG1

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Balaka Community Radio posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Balaka Community Radio:

Share