Living Waters Church Radio

Living Waters Church Radio Living waters church radio 96.0 FM Southern region 96.2 FM Central region. Http://livingwaters-dexterity.radioca.st/stream

 Mtsogoleri wadziko lino Professor Arthur Peter Mutharika wagawa unduna wa mphamvu yamagetsi komanso migodi kukhala maun...
29/05/2026



Mtsogoleri wadziko lino Professor Arthur Peter Mutharika wagawa unduna wa mphamvu yamagetsi komanso migodi kukhala maunduna awiri.

A Mutharika asankha Dr Jean Mathanga kukhala nduna mphamvu zamagetsi pamene a Thoko Tembo ndi nduna yazamigodi.

Kutsatira kalata yomwe mlembi wamkulu mu ofesi yamtsogoleri wadziko lino komanso nduna Dr Justin Saidi, ati ndunazi zayamba kale kugwira ntchito.

Wemba Mphatso Nkhoma

 Goshen City Dedza Dynamos has robbed in Haswell Gamphani as their Chief Executive Officer.The leadership has confirmed ...
29/05/2026



Goshen City Dedza Dynamos has robbed in Haswell Gamphani as their Chief Executive Officer.

The leadership has confirmed the upshot.

Gamphani brings experience and professional leadership to the team that is anchoring the 16 team member league.

Currently, the Goshen City sponsored team is having 1 point from 5 games and this weekend, they are playing Kamuzu Barracks at Dedza Stadium.

Reported by Mphatso Nkhoma

 MDF soldier lost his life early Thursday morning when an ERF truck he was in overturned at Box Hunga, along the Chikang...
28/05/2026



MDF soldier lost his life early Thursday morning when an ERF truck he was in overturned at Box Hunga, along the Chikangawa/Jenda stretch of the M1 road.

The truck was traveling from Mzuzu to Lilongwe when the accident happened, Mzimba Police spokesperson Maria Banda confirmed.

Banda identified the deceased as Vincent Mwenifumbo and he was pinned under bags of rice that spilled after the truck rolled and was later pronounced dead at Mzimba District Hospital.

Another passenger, Kasonkanji Nkhoma, survived with an injury to his right leg.

Police say the truck driver fled the scene immediately after the crash. His whereabouts and other details remain unknown as investigations continue.

Reported by John Bruce Jonathan

 Apolisi ku Lilongwe agwira abambo awiri omwe kale anali kundende chifukwa chogwidwa ali ndi mfuti ya mtundu wa pistol n...
27/05/2026



Apolisi ku Lilongwe agwira abambo awiri omwe kale anali kundende chifukwa chogwidwa ali ndi mfuti ya mtundu wa pistol ndi zipolopolo zopanda chilolezo.

Malinga ndi m'neneri wa Polisi ya Lilongwe, Hastings Chigalu, awiriwa ndi Steven Kanongola Kambwiri wa zaka 54 ndi Philip Lazaro wa zaka 51. Mzawo wawo wina, Jack Semu Kapilikitsa, adathawa apolisi asanawagwire.

Chigalu adati chochitikacho chidachitika pa 26 May 2026 ku Bwalolanjovu mumzinda wa Lilongwe. Apolisi adachita chipikisheni mgalimoto yomwe anthuwa anali kuyendamo ndipo ndipamene adapeza mfutiyo.

Iye adanenanso kuti Kambwiri ndi Kapilikitsa amene wathawayu adangotuluka kumene pa belo pa mlandu wakuba. Komanso awiriwa akuganiziridwa kuti kale adachita chiwembu ndi nzika ya ku India. Akuti adaphwetsa matayala agalimoto yake, kenako nambera chikwama chokhala ndi ndalama.

Pakadali pano Kambwiri ndi Lazaro adzaonekera kubwalo la milandu kuti ayankhe mlandu wokhala ndi mfuti yopanda kalata yovomerezeka.

Wolemba John Bruce Jonathan

 Timu ya Mighty Wanderers tsopano yafika pa nambala yachitatu itasambitsa chokweza timu ya Karonga United ndi zigoli zin...
27/05/2026



Timu ya Mighty Wanderers tsopano yafika pa nambala yachitatu itasambitsa chokweza timu ya Karonga United ndi zigoli zinayi kwa Chimodzi.

Isaac Kaliati ndi yemwe anatsegula pa golo la Karonga united pa mphindi 15 zachigawo choyamba, Lameck Mithi asanabwere ndi chigoli cha chiwiri cha timuyi pa mphindi 22.

Koma pomwe pamafika mphindi 34, muchigawo choyamba chomwechi, Alex Benson wa Karonga United anakaodira pa golo la Manoma zomwe zinapeleka mkwiyo kwa Mithi kuti abwerenso ndi chigoli china chachitatu cha manoma pa mphindi 38, kuti azipita kopumulira, Wanderers ikutsogola ndi zigoli zitatu kwa chimodzi.

Chigawo chachiwiri chinayamba mwa pamwamba pomwe Karonga United inamanga linga kumbuyo kwawo kuti Wanderers isadutse koma izi zinatsemphana ndi maganizo a Mithi yemwe anakhoma msomali otsiliza pa bokosi la ng'ona za ku Karonga pa mphindi 84.

Masewerowa anathera ndi zigoli zinayi kwa chimodzi kukomera timu ya Mighty Wanderers ndipo Lameck Mithi ndiyemwe anasankhidwa kuti wasewera bwino kuposa aliyense mumasewero a pakati pa Mighty Wanderers ndi Karonga United pa bwalo la zamasewero la Mpira ku Blantyre.

Wolemba Abdullahziz Losa (Mulanje)

 Malawi Electoral Commission Chief Elections Officer Andrew Mpesi has stepped down, LWC confirms.Mpesi himself confirmed...
27/05/2026



Malawi Electoral Commission Chief Elections Officer Andrew Mpesi has stepped down, LWC confirms.

Mpesi himself confirmed the resignation. MEC Commissioner Limbikani Kamlongera also verified it.

Kamlongera said the announcement was made during an internal meeting led by MEC Chairperson Justice Annabel Mtalimanja.

LWC will share more details as they come in.

Reported by John Bruce Jonathan

27/05/2026

Shout out to our newest followers! Excited to have you onboard! Hisborne Mweta Gift Nedi Mwadini Ndacha Mpasa Loster Saiwala Adreck Chiweza Fathre Jeremiah Mwakayoka Austin Murphy Elizabeth Makwakwa Tiwonge Carlton Phiri Patrick B Cement Precious TK Mnenulah Sar Sandulani Thokozani Wa Glory Mpinda Geofu Ngwira Emmanuel Mashatin Felix Chauluka Lēòñärdö Mäqüï Jölämö Samuel Daudi Mlakatuli Bright Kaduya Benson Poya Fïrst King Dan Brian Jim Tryness Mkandawire Stevelia Julayeh Frank J Chombo Ellinah Frank Neverson Washington Tsoka Everlasting Gracious Olive Danwell Thiyas Innocent Brave Blessings Isaac Mangwere Ine Lingwa Bamali Ruth Brighton Doctors Maloko Chiccoh Andrew Malamulo Chimbende Jnr George Makhalira Josephy Jonathan Manuel Mario Mario Fre MA Mathews Jimu Patiemour Minikwa Wexton Mangandale Nanenso Chirwa Alex Nkhoma Chikopa Patrick Alfred Richard Nedson Laston Çhíçóól J Féél Dàhsour

26/05/2026



Murder case convict Annie Mumba Dies Before Appeal Hearing at the Supreme court of apeal and she was on bail, according to the family sources.

Mumba was convicted by High Court Judge Mzonde Mvula for the murder of her husband, Professor Peter Mumba who was then lecturer at Lilongwe University of Agriculture and Natural Resources (LUANAR).

She had been granted bail pending her appeal at the Supreme Court of Appeal. The appeal hearing had not started before her death.

Reported by John Bruce Jonathan (Blantyre).

26/05/2026



Apolisi ku Mponela boma la Dowa ati akusakasaka bambo wina yemwe sakudziwika pomuganizira kuti anachotsera nkhawa zake pa msikana wa zaka zisanu ndi chimodzi (6) wa mmudzi wa Nyengere m'boma lomweli la Dowa.

Malinga ndi mneneri wa polisi ya Mponela McPatson Msadala, oganidzilidwayu anaona mwanayu akusewera ndi amzake pa bwalo la zamasewero la sukulu ina asanamukokere mwanayi m'munda wachimanga ndikupanga zakukhosi kwake.

Msadala anapitiliza kunena kuti anthu ena ongodutsa ndiwo anawona mwanayu atakomoka kwinako akutuluka mwadzi kumalo ake obisika. Ndipo anthuwa anamutengera ku Chipatala cha ching'ono cha Mponera kuti akalandire thandizo la mankhwala.

Mkulu wa chipatala cha Mponela Owen Chipewa, watsimikizira kuti mwanayu anavuladzidwadi kumalo ake obisika ndipo anamutulutsa atalandira mankhwala.

Wolemba Abdullahziz Losa (Mulanje)

 Timu ya Goshen City Dedza Dynamos yapititsa kutchuthi chokakamiza mphunzitsi wawo wamkulu Alex Ngwira kamba kosachita b...
26/05/2026



Timu ya Goshen City Dedza Dynamos yapititsa kutchuthi chokakamiza mphunzitsi wawo wamkulu Alex Ngwira kamba kosachita bwino kwa timuyi.

Timuyi yomwe siinapambaneko ngakhalenso kugoletsa chigoli mumpikisano wa chaka chino wa FDH ndipo ilipansi penipeni pamatimu khumi asanu ndi imodzi (16) omwe akutenga nawo gawo.

Izi zikudza patangopita tsiku limodzi wapampando wa timuyi a Gerald Kampanikiza atalemba patsamba lawo lamchezo kunena kuti anawalangiza aphunzitsi atimuyi kuti akhazikitse mwambo kwa osewera kuti timuyi iyambirenso kuchita bwino koma izi sidzikuchitika.

Pansi pa a Ngwira, chaka Chatha timuyi inakwanitsa kufika ndime yomaliza yampikisano wa Castel ndipo anagonja ndi timu ya FCB Nyasa Big Bullets yomwe inakhala akatswiri.

Posachedwa matimu a Ekhaya, Creck Sporting komanso Kamuzu Barracks naonso anaimitsa amphinzitsi amatimu awo.

Wolemba Mphatso Nkhoma

25/05/2026



The body of the unknown person was found dead inside the ceiling of Mpingwe Hostel at the Malawi University of Business and Applied Sciences (MUBAS) in Blantyre.

University workers discovered the body in an advanced state of decomposition. The deceased is suspected to be a MUBAS student.

Authorities are conducting investigations to determine the cause of death and to formally identify the deceased.

Report by John Bruce Jonathan (Blantyre)

Address

Blantyre

Telephone

+265999878093

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Living Waters Church Radio posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Living Waters Church Radio:

Share

Category