𝑺𝑼𝑡𝑨𝑰𝑷𝑯𝑢𝑡𝒀𝑬 265

  • Home
  • Malawi
  • Blantyre
  • 𝑺𝑼𝑡𝑨𝑰𝑷𝑯𝑢𝑡𝒀𝑬 265

𝑺𝑼𝑡𝑨𝑰𝑷𝑯𝑢𝑡𝒀𝑬 265 WELCOME TO 𝑺𝑼𝑡𝑨𝑰𝑷𝑯𝑢𝑡𝒀𝑬 WHERE YOU CAN FIND ANY NEWS FROM ANY COUNTRY 🀝

05/01/2025

: Kafukufuku watsopano wapeza kuti kusuta kumachepetsa nthawi yokhala ndi moyo kuposa m'mene madotolo amaganizira.

Malingana ndi kafukufuku yemwe anachitika pa anthu osuta fodya mdziko la Britain, ndudu imodzi ya fodya imachotsa pafupifupi mphindi 20 pa moyo wa munthu, kutanthauza kuti paketi ya ndudu 20 ingafupikitse moyo wa munthu ndi pafupifupi maola asanu ndi aΕ΅iri.

Pambuyo powerengera nkhani ya za chuma komanso zinthu zina, Ochita zofufuza pa sukulu ya University College London apeza kuti amayi amachepetsa moyo wawo ndi mphindi 22 pa ndudu iliyonse yomwe asuta pamene amuna amachepetsa moyo wawo ndi mphindi 17 pa ndudu iliyonse.


-Alex Batison-
Source: CNN

03/01/2025

Mwana wa zaka zisanu ndi zitatu (8) m'dziko la Zimbabwe wakhala ali m’nkhalango yomwe muli nyama zolusa monga Mikango komanso Njobvu kwa masiku asanu akudya zipatso.

Phungu wa nyumba ya malamulo, Mutsa Murombedzi, kudzera patsamba lake la X wati mwanayu ndi Tinotenda Pudu ndipo anali m’nkhalango ya Matusadona Game Park.

β€œMwanayu wakhala ali m’nkhalangoyi kwa masiku asanu ndipo amagona pamwala ndikumadya zipatso m’nkhalango yomwe muli Mikango, Njobvu ndi nyama zina zolusa,” watero Murombedzi.

Bungwe la African Parks lati nkhalango ya Matusadona ili ndi chiwerengero cha Mikango pafupi-fupi makumi anayi (40), ndipo ati kumbuyoku inakhalapo imodzi mwa nkhalango momwe chiwerengero cha Mikango chinali chachikulu.

M’nyamatayu wati amakumba tizitsime ndi manja kuti azitha kupeza madzi akumwa.

Chithunzi: BBC
Wolemba: Johans Mumba

16/11/2024




A police officer, Zuzeni Samalani, 32, tragically lost his life while assisting at an accident scene on the Salima-Lilongwe road.

The incident occurred when a Nissan Navara hit a parked police vehicle, which then struck Officer Samalani.

He was rushed to Dowa District Hospital but was pronounced dead on arrival.

The driver of the Nissan, John Maganga, 40, has been arrested and is awaiting a court hearing as investigations continue.

Reported by Ephraim Mkali Banda

16/11/2024



Veteran broadcaster, Joshua Kambwiri has died this morning in Blantyre.

Malawi Broadcasting Corporation spokesperson Chisomo Mwamadi has confirmed about the death of Kambwiri who worked for many years at MBC before retiring few years ago.

More details about funeral arrangements will be provided later according to Mwamadi.

Kambwiri was a newsreader and presenter of a radio programme, "Sunday morning show on MBC".

(by Cassim Aubi -Blantyre:11/16/2024)
.

16/11/2024

MALAWI DEFENCE FORCE

RECRUITMENT EXERCISE

1. The Malawi Defence Force (MDF) will conduct a recruitment exercise for suitably qualified Malawian young men and women wishing to pursue a career in the MDF as regular soldiers.

2. The exercise shall be conducted in four (4) regions: (Northern, Central, Southern and Eastern). Successful candidates shall undergo an intensive six (6) months Military training at Malawi Armed Forces College
(MAFCO) in Salima.

3. The following are the requirements:

a.Must be a Malawian citizen with a valid National Identity Card (ID).

b. Must have a Malawi School Certificate of Education (MSCE).

c.Must be physically, mentally and medically fit.

d.Must have no criminal record.

e.Must have not served in any National Security Organisation.

f.Must be between 18 and 24 years of age.

8. Must be not less than 165 cm tall for men and 158 cm tall for women.

h. Must be single and without dependants or child support legal obligations.

i. Must be prepared to undergo comprehensive physical and medical examinations.

4. Interested candidates should send their applications in own handwriting with copies of academic certificate, curriculum vitae (CV) and National ID to the address nearest to the Applicants' District of origin by post as
follows:

Northern Region Districts
The Commanding Officer
Moyale Barracks
Post Office Box 23
MZUZU

Central Region Districts
The Commanding Officer
Kamuzu Barracks
Private Bag 43
LILONGWE

Southern Region Districts
The Commanding Officer
Cobbe Barracks
Private Bag 50
ZOMBA

5. Deadline for receiving applications is on 15th December, 2024. Only shortlisted candidates will be invited for interviews.

Higher Education in Malawi- HEMA
A Journey to Excellence

16/11/2024

NKHAN ZINA πŸ˜ŠπŸ™Œ Ku Kenya

Munthu wina anaba phone, anthu atamuona anayamba kumuthamangitsa iyeyo ataona kuti kwachema anthuwa atha kumupha anathawila ku police nkukazimangitsa, a police adamupeza olakwa ndipo adamutchaja ndalama kuti atuluke pa bail.

Anthu omwe amamuthamangitsa munthu aja anali akungodikira panja pa police kudikira kuti munthuyu atuluke athane naye chifukwa business yawo sidathe.

Iyeyu adakanika kulipira ndalama zomwe police idamuchaja, izi zidapangitsa kuti anthu akumudikira panja aja ayambe kusonkhelana ndalama akamulipilire bail atuluke athane naye 🀣

14/04/2024

𝑺𝑼𝑡𝑨𝑰𝑷𝑯𝑢𝑡𝒀𝑬 265?𝑡𝒀𝑬 265?

Madz osefukira akuwonga katundu, sitolo ndi nyumba za anthu ku dela la Chintheche m'boma la Nkhata Bay.

Madziwa akuyambira kuchokera pa mtsinje wa Lweya kukafika chapa Malaza ndipo nyumba zambiri za anthu zili m'madzi.

Bwanamkubwa wa boma la Nkhata Bay a Rodges Newa watsimikiza za ngoziyi ndipo akuti izi ndi kamba ka mvula yomwe yakhala ikugwa m'bomali.

A Newa akuti pakadali pano owona za ngozi ku khonsolo ya bomali ali pakalikiliki kuwerengera nyumba ndi katundu wina yemwe wakhudzidwa.

Dzana, ntchito za umoyo zinasokonera pa chipatala chapa Chintheche kamba kamadzi omwe analowa mzipinda za anthu odwala ndikuwonga katundu wawo ndi wachipatalachi.

Wolemba: Sam Kalimira

14/04/2024

𝑺𝑼𝑡𝑨𝑰𝑷𝑯𝑢𝑡𝒀𝑬 265

Thambo lokuda lagwa m'boma la Machinga komwe mfumu yaikulu Kapoloma yamwalira.

M'neneri wa khonsolo ya bomali a Martin Chiwanda watsimikiza za imfayi ndipo wati a Kapoloma amwalira dzulo usiku pa chipatala cha Queens ku Blantyre.

A Chiwanda ati thupi la mfumu Kapoloma lilowa m'manda lero nthawi ya 3 koloko madzulo m'boma lomweli la Machinga .

Wolemba: Blessings Tambala

09/04/2024



37-year old Dalitso Mtonyo has been slapped with a 16-year jail term for defiling an eight year old girl.

State Prosecutor Sergeant Winfred Nkhuniwa told the Dedza Senior Resident Magistrate Court that Mtonya defiled the girl in full view of her seven-year old friend.

He said the convict lured the victim and her friend to Tanyaza Private Secondary School in Dedza, demanded them to undress and defiled her.

Mtonyo reportedly warned her not to tell anyone after giving them K300.

But the victim's friend narrated the ordeal to her mother and a medical report confirmed the minor had been defiled.

Sensing danger, Mtonyo went into hiding but community policing forum members found and arrested him.

He pleaded not guilty in court, prompting the state to parade witnesses who proved the case beyond reasonable doubt.

Passing sentence, Senior Resident Magistrate James Mankhwazi handed Mtonyo a16-year jail term with hard as a deterrent to other would be offenders.

Reported by Imam Wali

08/04/2024

𝑺𝑼𝑡𝑨𝑰𝑷𝑯𝑢𝑡𝒀𝑬 265?𝑡𝒀𝑬 265

malo a chisangalalo a Illusionz ku Lilongwe a Martin Nyirenda wati khumbo lawo ndikuthandiza kutukula luso la oyimba mdziko lino komanso kuti Malawi akhale ndi malo ochuluka omwe alendo akhoza kuloza komanso kufikirako kukasangalala.

Kuyankhula m'banda kucha walero litatha phwando la oyimba waku South Africa Musa Keys, a Nyirenda ati akufuna kuti malo oterewa achulukire mdziko lino.

Pankhani yotukula oyimba anati, akuyesetsa kuyitanitsa oyimba akunja, osati kuti adzangoyimba kokha ayi, komanso kuti azipanga ubale wabwino ndi oyimba a mdziko lino woti athe kuyimbila limodzi, kamba kakuti nthawi zonse ayitana oyimba akunja amayitananso oyimba amdziko lino pa phwando loyimbalo.

Iwo atiso, a Malawi chaka chino sapuma chifukwa choti alipira kale ndalama yachikole pofuna kusunga tsiku, kwa oyimba angapo akunja kuti abwere adzayimbe mdziko lino.

(by Innocent Kumchedwa-Lilongwe:04/07/24)

08/04/2024

𝑺𝑼𝑡𝑨𝑰𝑷𝑯𝑢𝑡𝒀𝑬 265

About nine villages around Mwacheya area under Traditional Authority Sitola in Machinga district will no longer cover long distances to access health care services following the construction of the Mwacheya Health Centre.

The health post and a health worker's house have been constructed with funding from Constituency Development Fund {CDF} to a tune of about 20 million kwacha.

Speaking during the opening ceremony of the facility, Machinga Likwenu MP Bright Msaka said he was sad seeing how communities were struggling in accessing health care services hence the intervention.

Fortune Chilongo from Machinga District Hospital said the facility will go a long way in improving delivery and access to antenatal care and other health services.
Chilongo added most women were attending antenatal care clinics late due to long distances; a situation that endangered their lives and those of unborn babies.

Fatima Jailosi from Sonjera Village in the area described the facility as a big relief to women; saying they were travelling about 20 kilometers to Machinga District Hospital to access health services.

Meanwhile, Traditional Authority Sitola has since promised to encourage his counterparts to take ownership of the facility while urging health authorities in the district to ensure that drugs are always available at the facility.

Reported by Blessings Tambala

08/04/2024



M’nyamata mukumuona muchithuziyu ndi Chifuniro James, amene ali Fomu 1 pa sukulu ya sekondale ya Ntchisi.

Chifuniro amachokera m’mudzi mwa Kavwenje m'dera la mfumu yayikulu Chilooko m'boma la Ntchisi ndipo akupempha anthu akufuna kwabwino kuti amuthandize kuti akayambirenso sukulu.

Iye adalephera kupita ku sukuluyi telemu yathayi chifukwa chosowa fizi ndipo wakhala ali pakhomo telemu yathayi.

Chifuniro amakhala ndi amayi ake omwe akuti amalephera kupeza ndalama yokwana K130,000 yolipira pa telemu.

A Charles Josiah, omwe ndi a bursar pa sukuluyi atsimikizira za vuto la mnyamatayu ndipo ati sanamalize nawo telemu yathayi kaamba kavutoli.

Amene angafune kuthandiza akhoza kulumikizana naye pa nambala iyi 0987203470 kapena a bursar pa 0999679082.

Wolemba: Mphatso M'bang'ombe

Address

Blantyre

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when 𝑺𝑼𝑡𝑨𝑰𝑷𝑯𝑢𝑡𝒀𝑬 265 posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share