18/11/2025
Dear Alfred Gangata π and Norman Chisale π, tikupemphani inu ngati achinyamata anzathu omwe mulikudigolo ndinu mau athu
Ku Malawi π²πΌ achinyamata ambiri tikuvutika kwambiri.
Jobs tilibe π, ndalama za business tilibe, ndipo nthawi zambiri timapezeka tilibe tsogolo iliyonse
Every day we wake up with hope, koma moyo ukulimba kusitha kulibe.
Social media ndiye yatsala kukhala njira yathu yokhayo, but stillβ¦ we donβt earn anything ππ±.
Timangotaya data, timangoyesera, koma palibe chimene tikupindula kuchokera pa khama lathu.
Ine limodzi ndi anzanga achinyamata, tinakhala pansi nati:
βKodi boma likatiganizira ife? Kodi achinyamata tingapeze mwayi woti social media izitilipira monga momwe anzathu ku South Africa πΏπ¦ akupindulira?β
Ngati izi zingatheke, zikhoza kuchepetsa uphawi kwambiri ku Malawi π²πΌ.
So many youths are talentedβgraphics, entertainment, news, creativity, vloggingβbut no support, no payment, no opportunity π.
Please, Alfred Gangata π and Normal Chisale π,
mutimvere chisoni ife ana anu.
We are not asking for too muchβjust a chance, a small door to open for our future β¨.
Achinyamata tikufuna mwayi wosinthira miyoyo yathu, tikufuna thandizo, tikufuna tsogolo labwino π.
Tikupempha, mutifikisile uthenga uwu.
Tikufuna Malawi where youth can survive through their skills, not only through luck π