Ting'alure

Ting'alure Advertisment, Music pro, Business, politics, football, netball, volleyball, basketball, and many more...

MTENGO WA CHIMANGA WASIKA KUCHOKA PA K78 000 KUFIKA PA K45 000 THUMBA LA 50KG MUMADELA AMBILI ADZIKO LINOMtengo wa chima...
26/09/2025

MTENGO WA CHIMANGA WASIKA KUCHOKA PA K78 000 KUFIKA PA K45 000 THUMBA LA 50KG MUMADELA AMBILI ADZIKO LINO

Mtengo wa chimanga sopano wasika kuchoka pa K78 000 kufika pa K45 000 thumba la 50kg.

Pali chiyembekezo choti chimangachi chitha kusika mpaka pa, K20 000 thumba pa K50kg kaamba kakusankhidwa kwa a, Professor Arthur Peter Muntharika.

Nayo dollar yaku America yagwa mphavu pa black market kuchoka pa K5 000 kufika pa K2500.

Tiyembekezele kusikaso kwazakudya ndi katundu mumasiku ochepa omwe akuzawa.

Ziwanda zija osazazipwekesa zimazuza mbuyache
26/09/2025

Ziwanda zija osazazipwekesa zimazuza mbuyache

Ma content creators a ku Malawi, izi so tu awonetseni ma followers anuwo.. God's instruction was crystal clear.
Koma nah, Liabunya's enemies will only push for what will work for them... (Umbuli ndi umene unachuluka ku Malawi), God help us.

Iwetu utitukwsnisa ukufuna amalawi tizioneka anthu oyipa kwa inu ??Ndipo muliladi simunati mesa mumamudyera ukumuku muna...
26/09/2025

Iwetu utitukwsnisa ukufuna amalawi tizioneka anthu oyipa kwa inu ??

Ndipo muliladi simunati mesa mumamudyera ukumuku munamiza

Muzamukumbukile ndi inu osati ife ndipo iwuze milungu yako ya pansi panyanjayo kuti amakunamiza u have to know God yehova

"A Malawi mudzamuliranso Dr Laz, zinthu zitaipa kuposa pano, mudzati bolanso uja, anali munthu wa bwino, chifukwa pompano mtsogoleri asintha, 2030 nkudzafuna kudzasithanso",says the LORD!

-Experts from the previous prophecy delivery LIVE
VIDEO link below:

26/09/2025

Mulungu anati Osatchula dzina langa pachabe.
Koma momwe amalitchulila dzina laMulungu pachabe awawa ..😂

Mauneneli awuyu ndichimodzi modzi kumakuza kuti ndikuona utaika phone pa charge ndipo itagona pompo mawa podzuka battery pa phone yako ndikuona ilipa 100% . 😂

Or kumakuwuza kuti ndikuona a president anyowani atasankha nduna ..😂

Anyways zabhobho

anandipabikiza nawo ma message ku inbox koma ine sinayakhe kalikonse ndimadikila kuti azawayakhe ndi amalawi pa 16 Septe...
26/09/2025

anandipabikiza nawo ma message ku inbox koma ine sinayakhe kalikonse

ndimadikila kuti azawayakhe ndi amalawi pa 16 September apa ndiye akuyakhanino

Mau anu kwa dan lu ndi otani   ngat oyimba wankulu waku malawi kuno?
25/09/2025

Mau anu kwa dan lu ndi otani ngat oyimba wankulu waku malawi kuno?

A malawi mau anu amodzi kwa president wanu Peter muthalika ndiotani ??
25/09/2025

A malawi mau anu amodzi kwa president wanu Peter muthalika ndiotani ??

25/09/2025

we got this 😀

Idalipo time achinyamata ambili mumankonda mumba lero chavuta ndichani mwayamba kumuda mukut ndi okuba??
25/09/2025

Idalipo time achinyamata ambili mumankonda mumba lero chavuta ndichani mwayamba kumuda mukut ndi okuba??

Ngati mkotheka bwana please gwilan tchito ndiachinyamata atatu awa mosatengera chipani kuti mwina malawi pang'ono pokha ...
25/09/2025

Ngati mkotheka bwana please gwilan tchito ndiachinyamata atatu awa mosatengera chipani kuti mwina malawi pang'ono pokha ingasithe ku mavuto tilinawo

Cz aliyense apa alindi mfundo zake zoyendesa dziko ndiye mfundo zonsezija kuzika pamozi zitha kupanga chinthu choneka

Mwina tingachoke mu uphawi omwe tilinawo
Chonde bwana Peter Mutharika musataye achinyamatawa

To be honest I blame this two people Bambo chimwendo banda akamayakhula amayakhula ngat anzeru koma amayakhula mo ononga...
25/09/2025

To be honest I blame this two people

Bambo chimwendo banda akamayakhula amayakhula ngat anzeru koma amayakhula mo ononga iwo amaona ngati akukonza koma ayi akuononga guys akamati xool ndiyofunika sananame uyu zoti xool anapita ndakaika

Andi mayiawa kabwera naonso samayakhula bwino anayiwala kuti alipo nditchito ndipo ma bwana ake ndi amalawi ife owalipila ndi amalawi ife ndiye sungapange against ndi bwana wako ayi

Chikhala amayakhula bho komanso amanva zonena anzawo I don't think malawi inakakhala chonchi koma this 2 people there very evil 😳

Mr Prophet Austin Liabunya Pali anthu ambili omwe amakupangani follow ndipo amakukondani kwambiri ku mpingo wanuKoma izi...
25/09/2025

Mr Prophet Austin Liabunya
Pali anthu ambili omwe amakupangani follow ndipo amakukondani kwambiri ku mpingo wanu

Koma izi zomuyika Mulungu ku ndale sizabwino mukufuna kutionesa ngati ife anthu ndife oyipa osalemekeza anthu a mulungu

U can't say iweyo umawinisa ma president if you real man of God Bible imati mulungu amadana ndi anthu ozikweza iwe uli busy kuzikweza why

Mu church mwako muli anthu a zipani zosiyana siyana ena mcp ena dpp ana utm ana pp ana udf

So do u think anthu ampingo mwako angakondwe ndi izi if u are real man of God sumafunika uzipanga za ndale komanso ma ulaliki ako onse umatamanda zinthu za nziko lapansi

I can say your not real man of God ndipo u must stop to use name of God pomwe u worship for others gods not mulungu tikunziwayi

Ndipo every prophets for you ndiyaboza umangofuna kupanga scam the people

Please stop to use name for God

Address

Blantyre

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Ting'alure posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share