Ticheze media

Ticheze media All things media
(2)

02/12/2025

Kukumbukila Essau Kanyenda A.K.A Black Mamba.🕊

Confirmed:- Former Malawi national team soccer star Essau Kanyenda is no more. May the good lord comfort his Family and ...
02/12/2025

Confirmed:- Former Malawi national team soccer star Essau Kanyenda is no more.

May the good lord comfort his Family and friends and those who loved him.

Rest in Peace, Mamba. 🕊

01/12/2025

Koma zomwe akuchita anyamata aku Ndande abale.

Ambiri akugona:- winatu akuona ngati  ndi AI koma ayi ndithu nkulukuta moyo ali safe and sound.
01/12/2025

Ambiri akugona:- winatu akuona ngati ndi AI koma ayi ndithu nkulukuta moyo ali safe and sound.

01/12/2025

Amuna ena mukapsala za zii.

Ena akuti bola isakhale ya Pemphero Mphande.Dorothy Kingston nayenso akuti akukalandira honors moti pompano akhala Dr. D...
01/12/2025

Ena akuti bola isakhale ya Pemphero Mphande.

Dorothy Kingston nayenso akuti akukalandira honors moti pompano akhala Dr. Dorothy Kingston

Former Malawi national team football player Essau Kanyenda had been diagnosed with liver cancer in the UK. Prayers to hi...
01/12/2025

Former Malawi national team football player Essau Kanyenda had been diagnosed with liver cancer in the UK.

Prayers to him and his family. 🙏

“kukhala mamuna weniweni sikuti ndikuimba mizere yabwino mu nyimbo ya African Queen chabe.Mamuna weniweni amakhala dolo ...
01/12/2025

“kukhala mamuna weniweni sikuti ndikuimba mizere yabwino mu nyimbo ya African Queen chabe.

Mamuna weniweni amakhala dolo ozindikila kuti sakusenera kulalatira mkazi.

Ndimakukonda mene uliri ndiposo kupitilira apo koma sindingasekerele kusandilemekeza.”

- Natasha Osawaru, nkazi wa 2Baba wanyawani kufotokoza chifukwa chomwe oimbayu wakathera ku waya yapolisi ku U.K.

CC: Afrocania

01/12/2025

Azimai chomwe mumafuna muzachipeza:- Chipwilikiti ku Rongo University mdziko la Kenya pamene mai wina wagwidwa ndi gawoni ya graduate wina ndipo akuti amauza anthu kuti Iyeyo akupanga graduation. 😮

Ndani safuna kukhala graduate?

'Onse olimbana ndi ulendo wa APM ndi ouma mutu.':-Silvester Ayuba James watsila moto onse omwe akuti APM azilengeza ma u...
01/12/2025

'Onse olimbana ndi ulendo wa APM ndi ouma mutu.':-

Silvester Ayuba James watsila moto onse omwe akuti APM azilengeza ma ulendo ake onse monga mtsogoleri pakuti amakhala akugwilitsa ntchito ndalama za aMalawi.

Mau awo a Ayuba ati:- "Anthu owuma mitu sangasinthe olo mutawaphunzitsa chotani, chifukwa ubongo ndi chiwalo chokhacho chomwe chimabadwa chitakhwima kale, with no room for further development and/improvement.

Taonani lero ayambanso kulimbana ndi za umoyo wa President Arthur Peter Mutharika, pomwe amva kuti akupita kunja pa ulendo odziwa yekha. Zomwe zija zinatipweteketsa ndi zomwe akuzikakamira. Ine ndimaona ngati tinaphunzirapo kanthu-2."

'Kuwuma mutu ndi matenda akuti ngakhale operation singachize. Mavuto alipo.':- atsendera motero a Ayuba.

Chipongwe chabwanji ichi💔MWOS Malawi
01/12/2025

Chipongwe chabwanji ichi💔

MWOS Malawi

01/12/2025

Chipwilikiti mu love triangle:- Ku Ndirande Mg1 wapeza MG2 mgalimoto ya munake koma sigwilogwilo wake.

Address

Blantyre

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Ticheze media posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Ticheze media:

Share