
21/02/2025
Phungu wa dera la ntcheu Bwanje souhth Alexander Mwisho chilikumtima ati sanakhutile ndi yankho la nduna mu unduna wa za chitetezo cha mdziko Ezeckiel Ching'oma pa pempho lawo lokhudza mayendedwe pa polisi ya bilira lomwe analipereka kunyumba ya Malamulo.
Phunguyu wati polisi ya Bilira imayenda mitunda itali itali kuti ikagwile ntchito zake pomwe mayendedwe palibepo.
Iwo ati madera otalika kuposa ma kilomita makumi atatu(30) imadila polisi yomweyi zomwe zimapangitsa iwo kugwilitsa ntchito ndalama za mthumba mwawo
Pepmholi akahala akulipereka mu nyumbayi kwanthawi yaitali koma palibepo yankho logwilika,pomwe undunawu wati ukukoza za vutoli.
Thomas Nakali Phiri -Lilongwe