Kukaya DAILY

Kukaya DAILY π—™π—’π—’π—§π—•π—”π—Ÿπ—Ÿ 𝗧𝗩 | π— π—¨π—¦π—œπ—– & π— π—’π—©π—œπ—˜π—¦ π—¨π—£π——π—”π—§π—˜π—¦ | π—‘π—˜π—ͺ𝗦 | 𝗧𝗒𝗣 𝗦𝗧𝗒π—₯π—œπ—˜π—¦
β€”π”œπ”¬π”²π”― 𝔏𝔦𝔫𝔨 𝔗𝔬 𝔗𝔬𝔭 π”π”žπ”©π”žπ”΄π”¦ π”˜π”­π”‘π”žπ”±π”’π”°

Bringing you the best of Malawi's entertainment and news scene! πŸŽΆπŸ“° Stay in the loop with the latest music, movies, events, and trending stories. Your one-stop destination for all things Malawi!

Rashley WaliraRashley wafika polira pa live yake uku akupepha a malawi kuti amukhululukire pakuti video yomwe munaona ij...
26/08/2025

Rashley Walira

Rashley wafika polira pa live yake uku akupepha a malawi kuti amukhululukire pakuti video yomwe munaona ija wina anachita kupanga edit. Nyamata wapempha chikhululuko chanu amalawi

Chaka chino kulibe kupuma. inu mwakwera iti pamenepa
26/08/2025

Chaka chino kulibe kupuma. inu mwakwera iti pamenepa

MANEB YAKOZA ZOLAKWIKA PA NKHANI ZA ZOTSATIRA ZA JCE 2025Malawi National Examinations Board (MANEB) yalengeza kuti pa li...
26/08/2025

MANEB YAKOZA ZOLAKWIKA PA NKHANI ZA ZOTSATIRA ZA JCE 2025

Malawi National Examinations Board (MANEB) yalengeza kuti pa lipoti la JCE 2025 panalembedwa molakwika kuti St Mary’s Secondary School, yomwe ili m’gulu la masukulu 10 apamwamba kwambiri, ili ku Mzuzu City.

Koma zoona zake ndi zakuti sukuluyi ili ku Zomba Urban education district.

MANEB yalapa chifukwa cha zolakwikazo.

🚨 PETER MUTHARIKA AYANKHULA MOKWANA!Mtsogoleri wa DPP, Prof. Peter Mutharika, wati misonkhano yomwe akuchititsa sabata i...
26/08/2025

🚨 PETER MUTHARIKA AYANKHULA MOKWANA!

Mtsogoleri wa DPP, Prof. Peter Mutharika, wati misonkhano yomwe akuchititsa sabata ino yanyozetsa onse amene amawafunira zoyipa.

Iye wayankhula izi ku Nkhotakota, atachokera ku Mzuzu komwe anachititsa msonkhano waukulu.

Mutharika wati akabwerera m’boma pa 16 September, DPP idzalimbana ndi njala, kukonza misewu ndi kukonza chuma cha dziko chomwe akuti chasokonekera mu boma lomwe lilipo.

Misonkhano ikupitirirabe ndipo ulendo wotsatira ndi pa msika wa Kaphatenga ku Salima.

Kodi mukuona ngati Mutharika ali ndi mwayi wobwerera mu boma?
πŸ‘‡ Lembani maganizo anu!

🚨 Ngozi Yaikulu Ku Lilongwe!Zomwe zinkayamba ngati mwambo wa mapemphero zatha mwatsoka – mkazi wamwalira pambuyo pa kume...
26/08/2025

🚨 Ngozi Yaikulu Ku Lilongwe!

Zomwe zinkayamba ngati mwambo wa mapemphero zatha mwatsoka – mkazi wamwalira pambuyo pa kumenyedwa mobwerezabwereza ku tchalitchi cha Zamkutu Zion.

Mnyamata wazaka 19 Yohane Mphatso, ali kale m’manja mwa apolisi pakuti iye ndi amene anamenya mzimayiyu ndi ndondo mobwelezabweleza zomwe iwo amati akuchotsa ziwanda, ndipo anthu a m’dera ali ndi mantha kwambiri.

Kodi inu mukuganiza chiyani za mwambo wa mapempherowu?
πŸ‘‡ Lembani maganizo anu pansipa.

Abwalo la milandu ndi apolisi m'boma la Ntcheu lero aotcha matumba a Chamba olemera matani 1.5.Motsogozedwa ndi oweluza ...
26/08/2025

Abwalo la milandu ndi apolisi m'boma la Ntcheu lero aotcha matumba a Chamba olemera matani 1.5.

Motsogozedwa ndi oweluza mlandu Alley Abu, gulu la apolisi ndi oweluza milandu komanso nthambi yoona za nkhalango aotcha matumba 18 achambawa kufupi ndi bwalo la milandu m'bomali.

Malingana ndi mneneri wa apolisi m'bomali a Jacob Khembo matumba achambawa adawalanda kwa munthu wina yemwe tsopano akugwira ukaidi.

Yemwe akugwira ukaidiyo ananyamula matumba achambawo mu galimoto la mtundu wa Honda Freed ndipo amalowera mu mzinda wa Blantyre.

Akhembo ati atamugwira bamboyo anathawa ndikusiya galimoto pomwepo koma atakwanitsa kumugwira adamulamula kuti akakhale kundende ndi kugwira ntchito yakalavulagaga kaamba kopezeka ndi chamba popanda zikalata zomuyeneleza.

Credit times

Kuphedwa kwa mkulu wina ochita malonda😭Anthu amene anapha ochita MALONDA otchedwa Omar Mbewe yemwe ankafuna kupikisana n...
26/08/2025

Kuphedwa kwa mkulu wina ochita malonda😭

Anthu amene anapha ochita MALONDA otchedwa Omar Mbewe yemwe ankafuna kupikisana nawo mpando wau khansala ku Chileka tsopano agwidwa.

Anthuwa anapha ndikubera ndalama a Mbewe akuchoka kushop yawo madzulo.. A police ya Chileka atsimikiza zakumangidwa kwa anthuwa.

Mu zinthuzi izi kumamzere kwanu kuli Omar Mbewe yemwe anaphedwayo pomwe okuphawo ali kumanja kwanu mukaona ..

Mu December 2020. Nthawi yafika kuti mupange chisankho choyenera nu September
26/08/2025

Mu December 2020. Nthawi yafika kuti mupange chisankho choyenera nu September

KwachemelatuNde akuti mawa kuli Live tikumane kumeneko
25/08/2025

Kwachemelatu
Nde akuti mawa kuli Live tikumane kumeneko

25/08/2025

MWAMVATU ETI? πŸ€£πŸ’€πŸ”ž

AMBIRI MWAIFE, TAKULIRA ZOMWEZI πŸ€£πŸ’€
25/08/2025

AMBIRI MWAIFE, TAKULIRA ZOMWEZI πŸ€£πŸ’€

24/08/2025

CHAKWERA YO ADALAKWA ZENIZENI, MPAKA APA?πŸ˜‚πŸ€£πŸ’€πŸ”žπŸ™Œ

Address

Lilongwe

Telephone

+265998060972

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Kukaya DAILY posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Kukaya DAILY:

Share