Nkhani Za M'maboma

Nkhani Za M'maboma ๐ŸŒTHIS IS THE LATEST & FASTEST GROWING PAGE FOR BREAKING NEWS๐ŸŒ . Welcome ๐Ÿ˜Žkuing'alura osaopa๐Ÿ˜Ž๐Ÿ’ช๐Ÿ’ช

22/09/2025

Ndikuona anthu 1000 on this page Mulungu akutembenuza nyengo zawo kukhala umboni wachimwemwe, mu dzina la Yesu Christ๐Ÿ™๐Ÿ•Š๏ธ๐Ÿ•Š๏ธ

22/09/2025

Mwazuka bwanji kumeneko ๐Ÿ™๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ

19/09/2025

Lemekezani Yehova ndikusayiwala zokoma zonse wakuchitirani...moyo wa Lero ndi mphatso yayikulu๐Ÿ™๐Ÿ™๐Ÿ™๐Ÿ™๐Ÿ™

17/09/2025

Be ready ma results azisankho tikulandra apa tikuyamba kuponya ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ

Nkhan yotipeza kumeneKu Namatapa-Bangwe ena mwa mzika zomwe zabwera kudzaponya voti zikunyinyirika chifukwa cha kuchedwa...
16/09/2025

Nkhan yotipeza kumene

Ku Namatapa-Bangwe ena mwa mzika zomwe zabwera kudzaponya voti zikunyinyirika chifukwa cha kuchedwa kapena kuvuta kwa makina zomwe akuti zikukanikisa mizele ina (stream) kuyamba kuponya voti.

Mwachitsanzo, stream 7 pa malopa, ayamba kusakasaka mayina powona m'buku lakalembera (Manual) pakuti makina sakutheka.

Oyang'anira ati apereka uthenga kwa Constituency returning officer (CRO) kuti ma technician abwere ndi kuzathandizira.

Wolemba Llywellenie Mpasa

08/09/2025

Ngati ukava Dzina la
Mulungu limakubowa
Dusa
Usalembe AMEN ๐Ÿ™๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ

06/09/2025

๐Ÿ’™๐Ÿ’™๐Ÿ’™Usanathimitse Data yanu madzulo alero tangolembani โœ๏ธโœ๏ธโœ๏ธ amen.Nthawi iyi Mulungu akupanga za inu.๐Ÿ’™๐Ÿ’™๐Ÿ’™

Nkhani Za LeroBambo Gerhardus Albertus Janse Van Rensburg, azaka 72 ochokera ku south Africa adasowa ku nkhalangi ya Nyi...
05/09/2025

Nkhani Za Lero

Bambo Gerhardus Albertus Janse Van Rensburg, azaka 72 ochokera ku south Africa adasowa ku nkhalangi ya Nyika National Park m'boma la Rumphi District pa 17 July, 2025.

Ndipo ntchito yofufuza idakalibe imkati

Nkhani Za M'mabomaWoyimba nyimbo zauzimu wodziwika bwino mmasamba a mchezo  wa mdziko la Rwanda Gloriose Musabyimana wam...
04/09/2025

Nkhani Za M'maboma

Woyimba nyimbo zauzimu wodziwika bwino mmasamba a mchezo wa mdziko la Rwanda Gloriose Musabyimana wamwalira ali ndi zaka 36.

Woyimbayu yemwe amadziwika bwino ndi nyimbo yoti Everyday, I Need Blood of Jesus wamwalira akulandila thandizo pa chipatala china mdziko la Uganda komwe anapita kuti akaimbe ku phwando lina.

Malinga ndi nyuzipepala zina kumeneko, ngakhale nthenda yomwe yamutengera kumanda sikudziwika pakanali pano , woyimbayu yemwe amadziwika ndi dzina loti Gogo adauzapo atolankhani kuti amavutika ndi nthenda ya mtima.

Anthu ambiri mmasamba a mchezo akupitilira kulemba mauthenga achisoni.

(Wolemba Jimmy Chazama)

27/08/2025

Tsiku loyamba ndi pemphero limatha ndi zisomo ๐Ÿ™

Lero mulungu akuchitileni zozizizwa pa moyo wanu๐Ÿ™๐Ÿ•Š๏ธ

Zochitika ๐Ÿ”ฅApolisi ku Lilongwe amanga mneneri Zelesi Divason ndi atumiki ake atatu powaganizira kuti amasunga mokakamiza...
26/08/2025

Zochitika ๐Ÿ”ฅ

Apolisi ku Lilongwe amanga mneneri Zelesi Divason ndi atumiki ake atatu powaganizira kuti amasunga mokakamiza mnyamata wina yemwe ali ndi matenda a mu ubongo, yemwe iwo amati amuukitsa ku akufa.

Malinga ndi wachiwiri kwa mneneri wa apolisi ya chigawo cha Central West a Foster Benjamin, mneneri Divason ndi atumiki akewo analosera kuti mwana wa mayi Mary Chelewani yemwe anachita kuphedwa mu 2023, auka ndipo abwelera kwa mayi ake.

Kutsatira chikhulupiliro, mayi Chelewani akuti anaona mnyamata yemwe anaoneka ngati mwana wawo ku Area 36 ndipo nthawi yomweyo anamutenga nkumupititsa kwa mneneri Divason.

"Ngakhale mnyamatayo anali ndi nkhope yosiyana ndi mwana wa mayi Chelewani yemwe anamwalirayo, mneneri Divason akuti anatsimikizira mayi Chelewani kuti mwana wawo ndiyemweyo ndipo wauka. Mneneriyu akuti anauza mayiyo kuti asunge mnyamatayo ndipo azipemphera tsiku lililonse kuti nkhope ya mnyamatayo ibwelere ndikufanana ndi nkhope yomwe mwana wawo anali nayo," atero a Benjamin.

Koma patatha masiku, mayi wina anakanena ku polisi ya 36 kuti mwana wake wa zaka 27 wasowa ndipo mayiyo anati mnyamata amasungidwayo ndi mwana wake.

Pakadali pano apolisi amanga mneneri Divason wa zaka 40, aneneri ake; Emily Chanunkha (35), Konsolata Osikala (46), ndi Flora Gamulani (42) ndipo apatsidwa mlandu obisa kubedwa kwamunthu komanso kuzembetsa munthu zomwe ndi zosemphana ndi lamulo 264 la penal code.

Kumangidwa kwawo kukudza pomwe enanso ku Mchinji ndi ku Area 36 anamangidwanso kutsatira kunamiza anthu anthu kuti aukitsa akufa.

Wolemba Cathy Maulidi

Address

Lilongwe
INVITESOTHERSTOLIKETHISPAGEOF

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Nkhani Za M'maboma posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share