Montfort Media

Montfort Media A print and publishing house

04/08/2026

Pofika pa 3 August 2026, ntchito yobweretsa abale athu kuchokera ku South Africa yayenda motele:

Chiwerengero cha onse obwerera: 56,723
Amuna: 38,866
Akazi: 17,857
Ana osakwana zaka 5: 3,988
Amayi oyembekezera: 694
Mabasi omwe agwiritsidwa ntchito: 840
Anthu olandira thandizo la zaumoyo: 13,564

Tikuthokoza mabungwe, ma kampani ndi anthu onse omwe akutithandizira pantchitoyi.

Malawi News Agency
MBC Digital
Times 360 Malawi
Malawi Government
Zodiak Online
Nation Publications Limited
MIJ Online
TWR Malawi
Luntha television
Malawi Red Cross Society - MRCS
Ministry of Local Government and Rural Development-Malawi
Mibawa TV
Capital FM Malawi

Malawi Queens arrive homeThe Malawi national netball team has today returned from Glasgow, Scotland where they participa...
04/08/2026

Malawi Queens arrive home

The Malawi national netball team has today returned from Glasgow, Scotland where they participated in the Commonwealth Games and managed a 7th-position finish.

The queens registered three wins, beating Northern Ireland, Tonga and Scotland but lost to England, Australia and South Africa.

Netball Association of Malawi (NAM) had earlier challenged the team's technical panel to finish on position seven and has since expressed delight for achieving the target.

By Precious Msosa


Pictures by NAM

Kodi Scorchers ilemba mbiri?Timu ya mpira wa miyendo ya dziko lino ya atsikana ya Scorchers ili ndi mwayi wolemba mbiri ...
04/08/2026

Kodi Scorchers ilemba mbiri?

Timu ya mpira wa miyendo ya dziko lino ya atsikana ya Scorchers ili ndi mwayi wolemba mbiri yatsopano yofika mu ndime ya makotafayinolo a mpikisano wa Women Africa Cup of Nations (WAFCON) ngati ingafanane mphamvu kapena kugonjetsa timu ya Zambia mawa madzulo pa bwalo la Stade El Barid mu mzinda wa Rabat m’dziko la Morocco.

Masewero a mawa akuyembekezeka kukhala a maferano kaamba koti iliyonse siidzalola kugonja pofuna kukhala ndi mwayi waukulu wopitilira mu ndime ina.

Padakali pano timu ya Scorchers ili ndi mapointi asanu ndi amodzi ndipo ndiyomwe ikutsogolera gulu C, Nigeria ndiyachiwiri ndi mapointi atatu, Zambia ndiyachitatu ndi mapointi atatu ndipo kumapeto kuli timu ya Egypt imene ilibe pointi iliyonse. Matimu onsewa asewera masewero awiri aliyense.

Ngati Malawi ingagonje ndi Zambia ndipo Nigeria kugonjetsa Egypt, matimu onse adzakhala ndi mapointi asanu ndi amodzi aliyense. Ndipo zikatere, opitirira adzasankhidwa potengera lamulo loti opitirira asankhidwe powunikira zigoli zimene agoletsa, kumwetsedwa komanso mmene adachitira pokumana ndi amnzawo omwe afanana nawo mapointiwo (head to head).

Aka ndikoyamba timu ya Malawi kusewera mu mpikisano wa WAFCON ndipo siinakhumudwitsepo kaamba koti yapambana masewero ake onse awiri, kugonjetsa akatswiri omwe akuteteza chikhochi a Nigeria 3-2 ndinso Egypt 3-1 omwe akumanenso mawa.

Wosewera kutsogolo wa timu ya Zambia Barbra Banda ndiamene akutsogola pomwetsa zigoli pamene ali ndi zigoli zinayi motsatizana ndi Temwa Chawinga yemwe wamwetsa zigoli zitatu pa masewero awiri omwe asewera.

Wolemba Blessings Bakali



Chithunzi ena mwa osewera a Scorchers kusangalalira chigoli ku WAFCON |FAM

Speaker orders fresh probe into Kangankunde mine amid licensing concernsParliament has intensified scrutiny of the Kanga...
04/08/2026

Speaker orders fresh probe into Kangankunde mine amid licensing concerns

Parliament has intensified scrutiny of the Kangankunde Rare Earths Mine in Balaka, with the Speaker of the National Assembly directing the Parliamentary Committee on Natural Resources, Energy and Climate Change to institute a fresh investigation into the project’s operations within 30 days amid concerns over licensing and the export of mineral samples.

The directive followed presentation of the committee’s report by its vice chairperson, Khadijah Leah Chunga, who said the committee found that the mine is operating under a medium-scale mining licence issued in April 2022 despite the scale of operations suggesting it qualifies for a large-scale licence.

Chunga said the committee also established that the mining company failed to produce key technical, financial and environmental documents, including an Environmental Impact Assessment (EIA), during its oversight visit.

She further said the committee was concerned that raw mineral samples were being exported to Zambia and Australia for testing, but the Geological Survey Department could not account for the quantities exported or confirm whether test results had been returned to Malawi.

“We have given the Geological Survey Department two weeks to provide the information, but we are still waiting for the responses,” she said, adding that the absence of a laboratory at the mine means all raw materials are exported for testing.

While acknowledging the mine’s significant potential to contribute to Malawi’s economy, Chunga said the committee remained concerned that the country could be losing value from its mineral resources because of inadequate monitoring and regulatory compliance.

Responding to the report, Speaker of the National Assembly, Sameer Suleman said Parliament would not accept large-scale mining operations being conducted under a medium-scale licence.

“The figures we are hearing here are not medium-scale. That's large-scale. So maybe there's something they don't want to expose by using a large-scale licence,” Suleman said.

He gave the committee 30 days to verify all documentation and report back to Parliament, warning that the mine could be closed if the investigation uncovers irregularities or shows that Malawians are not benefiting from the country's mineral resources.

“We are not going to allow our minerals to be stolen anymore. We’d rather keep them,” he said.

By Khumbo Msambala Salanje, Malawi News Agency




Picture: Lilongwe Kamhuno legislator, Chunga

Artists’ representatives get clarity on COSOMA royalty distributionRepresentatives of some artists say they have gained ...
04/08/2026

Artists’ representatives get clarity on COSOMA royalty distribution

Representatives of some artists say they have gained clarity on how the Copyright Society of Malawi (COSOMA) distributes royalties following a closed-door meeting held on Monday at the society’s offices in Lilongwe.

The meeting, which involved representatives of Akometsi Limited, Madness Entertainment and 4kaya Films Inc., followed concerns from artists over the distribution of funds collected through the blank media levy system.

In a video shared by Akometsi Limited after the meeting, COSOMA Executive Director Dora Makwinja acknowledged that many people do not fully understand how the organisation collects and distributes royalties.

During the discussions, artist representative Kelvin Sulungwe said the meeting helped clarify the percentage of funds that ultimately reaches rights holders, as well as the methodology used in distributing the money.

“The meeting has helped us understand how COSOMA calculates the distribution of royalties, including the methodology used and how the final amount received by rights holders is arrived at,” Sulungwe said.

According to the representatives, rights holders receive about 48 percent of the total amount collected after various deductions and statutory allocations, clarifying that the commonly cited 60 percent figure does not represent the final amount received by rights holders.

They also explained that the distribution methodology is based on data collected from licensed compact disc (CD) and digital versatile disc (DVD) burning centres.

Meanwhile, Kelvin Ngumuya, popularly known as Jaa Kev, who represented Madness Entertainment during the meeting, raised concerns over what he described as the continued reliance on analogue systems within COSOMA’s operations.

In a video shared by Akometsi Limited, Jaa Kev called for the introduction of digital systems to improve the collection, tracking and distribution of royalties.

The meeting also addressed concerns surrounding a 20 percent deduction that appeared on some royalty statements as an administration fee.

The artists’ representatives said the issue was clarified during the meeting, with the deduction explained as withholding tax rather than a fee charged by COSOMA.

The meeting followed growing calls from artists for greater transparency and accountability in the administration of royalties collected through the blank media levy system.

By Roy Howa, Malawi News Agency




Picture: Representatives of artists arriving at Cosoma Offices

Amayi ambiri akukumanabe ndi mavuto pa nkhani yoyamwitsa ana Unduna wa Zaumoyo ndi Ukhondo wati ngakhale ubwino wa kuyam...
04/08/2026

Amayi ambiri akukumanabe ndi mavuto pa nkhani yoyamwitsa ana

Unduna wa Zaumoyo ndi Ukhondo wati ngakhale ubwino wa kuyamwitsa ana mkaka wa m’mawere ndi wodziwika bwino, amayi ambiri amakumanabe ndi zopinga zomwe zimalepheretsa kuyamwitsa mwana kwa miyezi isanu ndi umodzi yoyambirira komanso kupitiriza kwa nthawi yoyenera.

Mu chikalata chomwe undunawu watulutsa pa 3 Ogasiti, 2026 kudzera mwa mlembi wake wamkulu a Bestone Chisamile, undunawu wapempha makhonsolo a maboma ang’ono, zipatala, olemba ntchito, atsogoleri a m’madera, adindo ena komanso mabungwe othandizana pa chitukuko kuti agwirizane poteteza, kulimbikitsa ndi kuthandiza kuyamwitsa ana mkaka wa m’mawere m’malo onse.

Malawi mogwirizana ndi mayiko ena padziko lapansi ali mu sabata yokumbukira za kuyamwitsa ana mkaka wa m’mawere yomwe ndikuyambira pa 1 mpaka 7 Ogasiti 2026.

Chaka chino, dziko lino likuyang’ana kwambiri za kulimbikitsa ntchito za umoyo kuti mayi aliyense wapakati ndi mayi wobereka alandire upangiri wabwino komanso kulimbikitsa njira zothandizira m’madera pogwirizanitsa mabanja, ogwira ntchito za m’madera, atsogoleri a m’madera komanso magulu othandiza amayi kuti azipereka chithandizo choyenera kwa amayi oyamwitsa.

Ndipo poyankhula pomwe amakhazikitsa sabatayi mu mzinda wa Lilongwe, wachiwiri kwa nduna ya zaumoyo ndi ukhondo a Charles Chilambula anati kuti amayi omwe angathe kuyamwitsa azitero chifukwa mkaka wa m’mawere umakhala ndi zofunikira kwambiri kwa mwana.

“Tikutsindika kuti kwa amayi omwe ali ndikuthekera koyamwitsa azitero potengera kuti zofunika zambiri sizimapezeka mu zolowa m’malo mwa mkaka wa m’mawere,” anatero a Chilambula.

Undunawu wati ndikoyenera kugwirana manja pochotsa zopinga zonse zomwe amayi oyamwitsa amakumana nawo komanso kukhazikitsa njira zokhazikika zothandiza mayi aliyense kuyamwitsa mwana wake mokwanira.

Wolemba: Evison Nansenya



Chithunzi, mayi kuyamwitsa mwana |Internet

01/08/2026
Ansembe a Montfort akondwerera zaka 125Mwambo wa nsembe ya ukaristiya  yokondwerera zaka 125 ya chipani cha ma mishonale...
01/08/2026

Ansembe a Montfort akondwerera zaka 125

Mwambo wa nsembe ya ukaristiya yokondwerera zaka 125 ya chipani cha ma mishonale a Montfort (Montfort Missionaries) kuno ku Malawi wayamba pa tchalitchi cha St Louis m'boma la Balaka.

Pa mwambowu pakukumbukiridwanso zaka 25 za African delegation m'dziko muno ndipo ukutsogoleredwa ndi Ambuye Montfort Stima a dayosizi ya Mangochi.

Pa nsembe ya ukaristiyayi pakudzodzedwanso brother Filex Nimanya kukhala dikoni.

Mu mau awo, Ambuye Stima alangiza a dikoni Nimanya kugwiritsa ntchito mphamvu zawo mokomera Mulungu komanso kudzudzula ngati zinthu sizikuyenda bwino m'dziko.

Bishopu Stima atinso monga munthu wodzodzedza, sajuyenera kuwopa kudzudzula pomwe zinthu zalakwika.

Wolemba Precious Msosa



Zithunzi zikuonetsa akhristu komanso ansembe ku mwambowu

 Malawi's Queens thrash Scotland to grab position 7The Malawi national netball team has beaten host Scotland 54-47  in i...
31/07/2026



Malawi's Queens thrash Scotland to grab position 7

The Malawi national netball team has beaten host Scotland 54-47 in its last game at the Commonwealth games and has since climbed to position seven from position nine on the world netball rankings.

The queens started the first quarter on a positive note, finishing it with 17 baskets against Scotland's 12.

In the second quarter, the home side fought hard and reduced the margin to 13-11, bringing the total scores to 30-23 at halftime.

Things heated up in the third and last quarter which both ended 12-12 but it was Malawi which had the last laugh following the 54-47 baskets.

Veteran shooter Mwawi Kumwenda was on song, banging most of the baskets. She combined well with fellow old-timer Takondwa Lwazi who provided her with killer passes.

With this win, the queens now have registered four wins and losing three at this year's commonwealth games. They have won against Northern Ireland, Tonga and Scotland, losing to South Africa, Australia and England.

By Precious Msosa



Pictures: The queens in today's game, by NAM

 Malawi vs Scotland
31/07/2026



Malawi vs Scotland

Address

Andiamo Loop Road
Lilongwe
NONE

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Montfort Media posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Montfort Media:

Shortcuts

Share