Prophet Peter Phiri

Prophet Peter Phiri Mulungu wositha Nyengo asitheso zanu ndipo kudziwike Kuti Mulungu Ali Nanu Amen 🙏

Mwezi uno wa June Pompano usangalala madalitso atakupanikiza ndipo uchita kumuuza Ambuye kuti Ambuye madalitso Andi chul...
18/06/2026

Mwezi uno wa June
Pompano usangalala madalitso atakupanikiza ndipo uchita kumuuza Ambuye kuti Ambuye madalitso Andi chulukila ine

Usazikayikile uthengawo ndi wako ndithu zichitika mudzina la Yesu khristu

09/06/2026

Ndikuona Mulungu Akuchotsa Chitonzo pa Moyo Wanu!
Week Ino Mukuchitira Umboni.

03/06/2026
Ambiri satana anawamanga pankhani ya za chuma chifukwa amadziwa Munthu opanda ndalama ndi Kophweka kuchimwa Lero Mulungu...
03/06/2026

Ambiri satana anawamanga pankhani ya za chuma chifukwa amadziwa Munthu opanda ndalama ndi Kophweka kuchimwa

Lero Mulungu akumasule mpaka utabowoleza pa za chuma , Mulungu abwezeretse ma business ndi ntchito za kufa pa moyo wako , Mudzina la Yesu Khristu!!.

Join man of God (Prophet Peter Phiri) Lero 7:30 madzulo Pomwe alowe live kupempherera anthu omwe akufuna kubowoleza pa zachuma

Don't miss

Shalom!!

Ngati ku mtundu kwanu amadalira iweyo, Mulungu akukumbukile week inoo mudzina la Yesu khristuMulungu akupatse moyo wauta...
29/05/2026

Ngati ku mtundu kwanu amadalira iweyo, Mulungu akukumbukile week inoo mudzina la Yesu khristu

Mulungu akupatse moyo wautali ndi wosadwala mudzina la Yesu khristu

Ifa ikhale kutali ndi moyo wako in Jesus might name

28/05/2026

Mulungu achititse manyazi anthu amene amakuyang'anila pasi awone umboni wako mudzina la Yesu khristu

Mulungu yemwe ankadalitsa , ankachilitsa yemwe a nkateteza aliyemwe lero ndipo achite ndi moyo wanuso lero mudzina la Ye...
22/05/2026

Mulungu yemwe ankadalitsa , ankachilitsa yemwe a nkateteza aliyemwe lero ndipo achite ndi moyo wanuso lero mudzina la Yesu Khristu!!

Prophet Peter Phiri adzakhala akupempherera anthu mamasulidwe, machilitso komaso kuboworeza pa 13 June 2026 pa Katoto Secondary School Hall boma la Mzuzu.

Mukumemedwa nonse kuti tidzakumane malo amanewa ndipo Mulungu wa mphavu zonse sadzatisiya chimodzi modzi. Amen 🙏

Ndikuyankhula ndi iweyo wagwila phone iwe kuti ulandile mdalitso wako omwe wakhala ukuwudikila kwa nthawi yaitali uja uf...
18/05/2026

Ndikuyankhula ndi iweyo wagwila phone iwe kuti ulandile mdalitso wako omwe wakhala ukuwudikila kwa nthawi yaitali uja ufike pa moyo wako in Jesus might name 🙏

Lero Mulungu achite chodabwitsa pa moyo wako,  indee Mulungu yemwe anali, alipo ndipo adzakhala achotse cha manyazi chil...
17/05/2026

Lero Mulungu achite chodabwitsa pa moyo wako, indee Mulungu yemwe anali, alipo ndipo adzakhala achotse cha manyazi chili chonse pa moyo wako Mudzina la Yesu Khristu!!

Landira Mudzina la Yesu Khristu 🙏

Follow 👉 Prophet Peter Phiri 👈

Address

Lilongwe

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Prophet Peter Phiri posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share