SirAlfred Kanjasko Mswati Jele

SirAlfred Kanjasko Mswati Jele Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from SirAlfred Kanjasko Mswati Jele, Digital creator, Mzimba.

Lest well star boy 😭
03/07/2025

Lest well star boy 😭

26/06/2025

23/06/2025

Maranatha Academy has announced a K5 million prize for any student nationwide who scores six points in the upcoming Malawi School Certificate of Education (MSCE) exams, starting next week, Tuesday.

The pledge was made during the academy’s 2025 graduation ceremony at Lilongwe’s Golden Peacock Hotel, where top-performing students also received cash awards of K200,000 to K300,000.

Managing Director Ernest Kaonga emphasized the academy’s commitment to academic excellence, encouraging all MSCE candidates to strive for outstanding results.

23/06/2025
07/05/2025

Football can kill

29/04/2025

MBIRI YA HASTINGS KAMUZU BANDA WENIWENI

( Muzithunzizo uyo wa diso la mng'alayo ndiye yemwe anali Kamuzu weniweni wathu🇲🇼, winayo wavala ma garasiyo dzina lake lenileni linali Richard Armstrong ochokera ku dziko la Ghana 🇬🇭 ndipo analamulila dziko la Malawi ngati Kamuzu kwa dzaka 31, ma buku a history ak*telo)

PART 1

Akimu Kankhwala Banda, mwana wa mayi Akupingama Phiri ndi Bambo Mphonongo Banda, a m'mudzi mwa nyakwawa chiwengo, mfumu yaikulu chilowamatambe, m'boma la Kasungu, anali ndi Diso la ng'ala lakumazele.

Ndipo Dzina loti Kamuzu linachokera pa muzu, kapena k*ti mankhwala a zitsamba, omwe mayi ake Akupingama Phiri, anakatenga kwa Sing'anga, kamba koti anali ndi vuto la uchembere.

Mayi Akupingama Phiri, anapatsidwa Kamuzu kamodzi kakang'ono komwe anauzidwa k*ti akanyike m'madzi ndipo adzimwa madziwo k*ti apeze mphatso ya mwana.

Ndipo pambuyo pogwilitsa ntchito mankhwalawo, Mwana anabadwa, ndipo anamutchura Dzina k*ti Akimu Kankhwala Banda.

Akimu ali m'nyamata, anachotsa dzina loti Kankhwala ndikuyikapo Kamuzu, ka mankhwala aja amene mayi ake Akupingama Phiri anapatsidwa ndi Sing'anga, ndipo iye anapita limodzi ndi amalume ake a Hannoch Msokera Phiri, ku Dziko la Zimbabwe.

Akimu akupitiliza maphunziro ake, anasinthanso dzina lake, pochotsa Dzina loti Akimu, ndikukhala Hastings Kamuzu Banda.

Ameneyu ndiye anali Hastings Kamuzu Banda, nzika ya Dziko lathu la Malawi, osati zina zija ayi, mchewa weni weni anali ameneyu.

Mukafufuza kwambiri mbiri ya Kamuzu Banda, mumapeza Anthu awiri, ali pachithunzipa ndi Richard Armstrong waku Ghana uja.

Mbiriyo imapitiliza kufotokoza k*ti, Hastings Kamuzu Banda, wa Diso la ng'ala, ankaphunzira limodzi ndi Richard Armstrong, mayi ake aku Ghana, Bambo ake aku America.

Ndipo Hastings Kamuzu Banda ndi Richard Armstrong, ankagwilizana kwambiri ndipo zonse ku sukulu ankapangira limodzi.

Koma chilichonse chomwe ankachita kapena kuyankhulana ndi Abale ake, Hastings Kamuzu Banda, ankammufotokozera nzake Richard.

28/04/2025

Arkangel Angel Woyera Tembo you are a hard worker. You bring a lot of confidence to punters. Keep on sharing codes. One day tizayiphura through your codes. God bless you.

MUNTHU YEMWE ANALIBE MWAYI PA DZIKO LONSE.ZINA UKAMVA!!!Munthu yemwe amadziwika k*ti analibe mwai onse padziko lonse lap...
18/04/2025

MUNTHU YEMWE ANALIBE MWAYI PA DZIKO LONSE.

ZINA UKAMVA!!!

Munthu yemwe amadziwika k*ti analibe mwai onse padziko lonse lapansi, ndi W Foralter Summeford.

Akuluwa anali mzika ya dziko la England ndipo zinthu zodabwisa zinakhala zikuwachitikila nthawi yomwe anali moyo mpaka atafa.

Chodabwisa choyamba chinamuchitikila Walter mu 1918 pamene ankagwila ntchito ku Belgium nthawi ya World war 1, Mr Summerford anali officer mu army. Tsiku lina pamene ankayenda ching'aning'ani (lightning) inamumuenya zomwe zinapangisa k*ti mbali yake yathupi kuyambila mumchuno lisiye kugwra ntchito (Paralyzed). Ngakhale anachila patatha miyezi yochepa anaumilizidwa kusiya ntchito.

Mr Walter Summerford anasamukila ku Canada kukayamba moyo wao watsopano, tsiku lina pomwe amagwira nsomba ku Pond mu 1924 chozwizwisa china chinachitika pamene ching'aning'ani chinawakwapulaso pamene anakhala pansi pamtengo ndipo mbali yayikulu la thupi lake linasiya kugwiranso ntchito.

Patatha zaka ziwiri anachila ngakhale zinkaoneka k*ti sangachile ndipo tsiku lina pamene anapita konjoya town kunja kunasintha mosaziwika bwno umo munali mu 1930 ndipo kunayamba mvula yosakhala bwino zomwe mapeto ake ching'aning'ani chinawamenyaso zomwe zinapangisa k*t avulale kwambiri, mbali yayikulu isiyenso kugwira ntchito. Analimbana nawo moyo koma zachisoni anamwalira mu 1932.

Mr Walter anayikidwa ku Vancouver, Canada, ndipo chodabwisa chachikulu chinachitika mu 1936 atamwalilabe k*ti ching'aning'ani chinamenya pamtumbila wake ndipo mwala umene unayikidwa pamwamba pamtumbila uja unanyenyeka. Patatha zaka 6 ching'aning'ani china chinamenyaso pamtumbila paja. Zimamvekabe k*ti pazaka 6 zilizonse or kuposela apo ching'aning'ani chimamenyabe ndipo chimene chimapangisa izi anthu saziwabe mpaka lero.

Address

Mzimba

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when SirAlfred Kanjasko Mswati Jele posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share