Balaka Community Radio

Balaka Community Radio Balaka Community Radio is a radio fully owned by the people of Balaka
"LIWU LATHU LA CHITUKUKO"

  Liberation for Economic Freedom (LEF) president David Mbewe has responded after the Malawi Electoral Commission (MEC) ...
06/08/2025


Liberation for Economic Freedom (LEF) president David Mbewe has responded after the Malawi Electoral Commission (MEC) rejected his nomination papers for the September 16 presidential election.

Mbewe acknowledged the setback but hinted at a possible alliance with another party.

He urged supporters to remain calm as the party finalizes its next steps.

Reported by Francis Billiat
(August 06,205)

Zikutero ndithu
06/08/2025

Zikutero ndithu

05/08/2025

Balaka Community Radio 107.6 FM
Francis Maonjera
Mwaitha ntchito

02/08/2025

Mau a wachiwiri wa mtsogoleri wa dziko lino
Dr Michael Biziwiki Usi.

"Anthu akuyenera kusiyanitsa nkhani za ndale ndi ntchito za boma"

  SIMUZANDIMVA NDIKUNYOZA KAPENA KUTUKWANA ANZANGA OMWE NDIKUPIKISANA NAWO — DOSSAM'modzi mwa anthu omwe  akupikisana na...
31/07/2025


SIMUZANDIMVA NDIKUNYOZA KAPENA KUTUKWANA ANZANGA OMWE NDIKUPIKISANA NAWO — DOSSA

M'modzi mwa anthu omwe akupikisana nawo pa udindo wa Mphungu Wanyumba ya Malamulo kudera la Balaka Bwaila, wa chipani cha UTM, Mercy Dossa, wati satenga nawo gawo pa kunyoza kapena kutukwana anzake omwe akupikisana nawo pa chisankhochi.

Dossa wanena izi Lachitatu pa 30 July, 2025, pa msonkhano wokopa anthu omwe anachititsa pa bwalo la masewero la Mbera, pomwe amafotokozera anthu zina mwa ndondomeko zomwe akufuna kuchita m'deralo ngati atapatsidwa mwayi woti akawatumikile ku Nyumba ya Malamulo.

“Simuzandimva ndikunyoza kapena kutukwana anzanga omwe ndikupikisana nawo. Tikuyenera kukhala ndi kampeni yoyenera komanso yolemekezana chifukwa cholinga chathu tonse ndichimodzi, kutukula dera lino,” adatero Dossa.

Asanapange msonkhanowu, Dossa anakapereka kalata zake ku bungwe loyendetsa zisankho la MEC pa Mbera TDC, ngati gawo lofunikira kuti avomerezedwe kutenga nawo mbali pa chisankho chomwe chikhalepo pa 16 Seputembala chaka chino.

Wolemba: Francis Maonjera_ Balaka
(July,31,2025)

  Omwe akufuna mpando wa Phungu wa dera la Balaka Ngwangwa, Anthony Tony Ngalande, la  Lachiwiri, 30 Julayi 2025 akupere...
29/07/2025


Omwe akufuna mpando wa Phungu wa dera la Balaka Ngwangwa, Anthony Tony Ngalande,
la Lachiwiri, 30 Julayi 2025 akupereka zikalata zawo zozayima nawo pa sikankho za pa seputembala 16,2025

Polankhula ndi wailesi ya Bakala, a Ngalande adatsimikizira kudzipereka kwawo kupitiliza kutumikira anthu amderali, ndipo atiso chitukuko ndi chofunika kwambiri iwo.

"Cholinga changa ndi kupitiliza chitukuko, palibe china," atero Ngalande.

Iwo alengeza kuti akangopeka zikalatazo akukhazikitsa ntchito zokopa anthu (kampeni) pabwalo la Manica, komweso akatswiri odziwika bwino pa nkhani za mayimbidwe Charles Nsaku, Zeze, ndi ena akakhaleko.

Wolemba: Violet Ajasi – Balaka
(Julayi 29, 2025)

  Aspirant for the Ngwangwa Constituency parliamentary seat, Anthony Tony Ngalande, will officially submitte his nominat...
29/07/2025



Aspirant for the Ngwangwa Constituency parliamentary seat, Anthony Tony Ngalande, will officially submitte his nomination papers on Tuesday, July 30, 2025.

In an interview with Bakala Radio, Ngalande reaffirmed his commitment to continue serving the people of the area, emphasizing that development remains his top priority.

"My mission is simply to continue with developmentnothing more," he stated.

Ngalande is expected to launch his campaign at the Manica trading ground, featuring performances by popular artists including Charles Nsaku, Zeze, and others.

Reported by Violet Ajasi-Balaka
(July, 29,2025)

  Yemwe akupikisana nawo pa udindo wa Mphungu ya Nyumba ya Malamulo ku dera la Balaka Bwaila, Innocent King Banda, wati ...
29/07/2025


Yemwe akupikisana nawo pa udindo wa Mphungu ya Nyumba ya Malamulo ku dera la Balaka Bwaila, Innocent King Banda, wati cholinga chake ndi kuthana ndi mavuto omwe anthu akukumana nawo kuderali.

Banda wanena izi Lachiwiri pomwe anapereka mapepala ake a chisankho ku bungwe loyendetsa zisankho la MEC ku Mbera TDC.

“Ndimafuna kuti anthu a ku Balaka Bwaila, azikhala ndi zinthu zoti amachita. Anthu ambiri akuvutika ndi njala komanso kusowa kwa ntchito, koma ine ndikufuna kusintha mmene zinthu zikuyendera,” adatero Banda.

Wolemba: Francis Maonjera -Balaka
(July,29,2025)

  Independent Candidate Innocent King Banda Joins Race for Balaka Bwaila Parliamentary SeatIndependent candidate Innocen...
29/07/2025



Independent Candidate Innocent King Banda Joins Race for Balaka Bwaila Parliamentary Seat

Independent candidate Innocent King Banda has officially entered the race for the Balaka Bwaila parliamentary seat after submitting his nomination papers to the Malawi Electoral Commission (MEC) at Mbera TDC on Tuesday.

Following the submission, Banda pledged to address key issues such as hunger and unemployment, promising development initiatives aimed at empowering local residents and improving their livelihoods.

He joins a growing field of contenders ahead of the 2025 General Elections, as the MEC continues to receive nominations from across the country.

Reported by Francis Maonjera – Balaka
(July,29,2025)

  A polisi M'boma la Mangochi akusaka Saka anthu amene sakudziwika omwe akuwaganizira kuti agwililira mwana wa zaka zita...
29/07/2025


A polisi M'boma la Mangochi akusaka Saka anthu amene sakudziwika omwe akuwaganizira kuti agwililira mwana wa zaka zitatu ndikumupha.

Amina Tepani Daud yemwe ndi ofalitsa nkhani za polisi ku Mangochi wati, thupi la mwanalo analipedza mchimbuzi mmene akuganizida kuti anthu oipa mtimawo anakalisiya atamaliza zofuna zawozo " izi zachitika mmudzi mwa Chipoka Mfumu yaikulu Mponda.

Zotsatira za kuchipatala zatsimikiza kuti mwanayu anamugwililiradi..

Wolemba: Williams Chande
(July,29,2025)

27/07/2025

FULL-TIME
Blue Eagles claim the maximum points.

FCB Nyasa Big Bullets 0-1 Blue Eagles

  Mtsogoleri wa chipani cha UTM Dr Dalitso Kabambe wasankha Dr  Mathews Mtumbuka  kukhara wachiwiri wawo pachisankho cha...
27/07/2025


Mtsogoleri wa chipani cha UTM Dr Dalitso Kabambe wasankha Dr Mathews Mtumbuka kukhara wachiwiri wawo pachisankho cha pa seputembala 16,2025.

Address

Balaka
Nacite
PRIVATEBAG1

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Balaka Community Radio posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Balaka Community Radio:

Share