NewConnect Malawi

NewConnect Malawi CREATE TO TEACH
Visible In An Invisible Visibility

14/05/2026


MALEMU CHILIMA ANALI NDI NKHAWA

   Boma lati aliyese amene atapezeke akusaka ,kupha kapena kugulitsa mbewa azimangidwa. IziZikudza pambuyo pa kafukufuku...
10/05/2026


Boma lati aliyese amene atapezeke akusaka ,kupha kapena kugulitsa mbewa azimangidwa. Izi
Zikudza pambuyo pa kafukufuku wa Wildlife Watch yemwe wasonyeza kuti mmaboma ambiri anthu akunonga tinyamati. Mkulu

Wa bungweli a Fronix Gausi ,ati Boma la mangochi ndili lili pamwamba pamaboma onse kamba koti ngakhale anthu ambiri samadya mbewa kumeneku amapha ndikupakira mmatumba nkumakagulitsa mmaboma Ena omwe kumadyedwa mbewazi.

Choncho Apolisi Ali pa kalikiliki mmaboma onse kuti amange anthu Osaka,kupha ndi kugulitsa mbewazi, ndipo ntchito yayamba kale kuntcheu komwe anthu 14 amangidwa sabata latha.
Tikupatsirani zambiri pangani folo NewConnect Malawi

09/05/2026


MAKOLO ANAWA KODI TIKUMAKHALA NAWO BWANJI MANYUMBAMU??

Wa HSA kumtero??😭

  List πŸ‘‡πŸ‘‡ you can also WAP me on 0222 200 806 1.MADZANJE SECONDARY SCHOOLBertha kasiya -------------------Lilongwe TTCEs...
08/05/2026


List πŸ‘‡πŸ‘‡ you can also WAP me on 0222 200 806
1.MADZANJE SECONDARY SCHOOL
Bertha kasiya -------------------Lilongwe TTC
Esmy Chipembere------------Lilongwe TTC
Samson Ngoma---------------Lilongwe TTC
Madalitso Kamalira---------Machinga TTC
Simon Wayiyatsa---------------Machinga TTC
Kelvin Ndoma------------------Machinga TTC
2.DOMBOLE SECONDARY SCHOOL
Shyreen Zalira--------------------Blantyre TTC
Kennedy Amos-------------------Kasungu TTC
Moureen Ntuwana. Lilongwe TTC
Geoffrey Dzunde. Lilongwe TTC
Yollam Lossi. Machinga TTC
Cidreck Potani. Machinga TTC
Luke Macson. Mchinji TTC
3.NSIPE COMMUNITY
Joyce Chautsi. Blantyre TTC
Keanne Lunduka. Chiradzulo TTC
Madalitso Mtsitsa. Chiradzulo TTC
Ida chiwamba. Lilongwe TTC
Chisomo Kachimanga. Machinga TTC
4.NTCHEU SECONDARY
Benson Chikaliso. Chiradzulo TTC
Halino Phiko. Kasungu TTC
Praise kalonga. Lilongwe TTC
Jinny Johannes. Lilongwe TTC
Jean Nthala. Lilongwe TTC
Nephtali Nthala. Lilongwe TTC
Hastings Masamba. Lilongwe TTC
Fanuel David. Machinga TTC
Aaron Braston. Machinga TTC
Prince lapken Machinga TTC
Chimwemwe Phiri. Machinga TTC
Josophat Kaphwiti. Mchinji TTC
5.VAKUSI MODEL HS
Fanita Suga. Blantyre TTC
Evelet Mvulaatera. Blantyre TTC
Blessings mbano. Blantyre TTC
Jablan Marshal. Chiradzulo TTC
Ester Mackenzie. Kasungu TTC
Ireen Vyakusi. Kasungu TTC
Miracle kachisi. Lilongwe TTC
Vitumbiko Manda. Lilongwe TTC
Christina kulapani. Machinga TTC
Temwa samila. Machinga TTC
Charles kagona. Mchinji TTC
Steve Mailos Phalombe TTC
6.MASASA COMMUNITY NTCHEU
Alinafe Nyadani. Blantyre TTC
Chiyamiko Alfred. Machinga TTC
7.NTHUMBI COMMUNITY
Yankho Elia. Machinga TTC
8.MALONDA COMMUNITY
Medson Gongonya. Lilongwe TTC
9.NACHITHEME SECONDARY

Follow NewConnect Malawi as List continues...... WhatsApp 02222 00 806

   Mfumu yachingoni, Inkosi Champiti yamuboma la Ntcheu yamwalira lero ili ndi zaka 84.Tikupatsirani zambiri,tsatirani t...
17/04/2026


Mfumu yachingoni, Inkosi Champiti yamuboma la Ntcheu yamwalira lero ili ndi zaka 84.
Tikupatsirani zambiri,tsatirani tsamba lino.
Mzimu wawo uuse mumtendere

26/03/2026



AWA NDIWO AKUFUNIKIRA PA KAFUKUFUKU WA NGOZI YA NDEGE, AKUONEKA KUTI AKHOZA KUTHANDIZAPO CHINACHAKE

  Ka chiphadzuwa kachichepere,kofatsa mukukaona apaka ndi kakuBalaka, Ndipo kakupanga Maphunziro aUtolankhani apooo pa p...
22/03/2026


Ka chiphadzuwa kachichepere,kofatsa mukukaona apaka ndi kakuBalaka, Ndipo kakupanga Maphunziro aUtolankhani apooo pa poly. Chosangalatsa nchakuti zaka zonse 18 zomwe kakhala pa dziko pano sikadziwa ndipo kalibe khumbo lodziwa mwamuna Kaye pakali pano, Mwachidule kakamaliza za utolankhanizi Chaka chamawa kakukayamba zausisiteri.
Lerotu ndi birthday yake ameneyu,MERCY JOB.
Wish Her Happy 18th birthdayπŸŽ‚πŸŽ‰πŸŽ‚πŸŽ‰πŸŽ‚πŸŽ‰πŸŽ‚

 Magulu osiyanasiyana a zipembedzo lero akuchita zionetsero muboma la Dowa ati kamba kosakondwa ndi utsogoleri wa DPP mo...
10/03/2026


Magulu osiyanasiyana a zipembedzo lero akuchita zionetsero muboma la Dowa ati kamba kosakondwa ndi utsogoleri wa DPP motsogozedwa ndi aPeter Mutharika.

Mkulu woyang'anira mipingo yonse yachi khristu mu bomali a Pull Kokani Majawa, ati zionetserozi nzokakamiza adindo aboma kutula pansi ma udindo.
Iwo ati Boma lalephera kugawa fetereza ndi Ufa pomwe anthu mu bomali akuvutika. Aonjezeraso kuti Boma likusala achewa chonsecho nawo ndi aMalawi aphindu pa chitukuko komanso kuti achewa ndiwo eni dziko.
A Majawa atinso ndi wodabwa kuti bwanji boma silikuchitapo kanthu kuchita zokambirana ndi maiko a US Israel ndi Iran zothetsa nkhondo kuti mavuto amafuta athe mdziko muno.

Iwo atinso zomwe yachita mfumu ya Mzinda wa Blantyre a Jomo Osuman potseka ofesi ya MCP ndi ndale chabe choncho akuyenera atule pansi udindo.

M'busayu watsindikira nzika kuti ngati akufuna kusintha mdziko muno asalekere panjira kuma kuchita nawo zionetserozi zomwe nzamasiku asanu.
Pakali pano mateyala ayamba kuotchedwa pa Mponera kuyambira mammawa ndipo ati akufuna akafike Ku Blantyre Kwa Jomo akapereke nkhawa zawo uku mu Mseu wa M1 onse mateyala akungofuka. Tikupatsirani zambiri pangani folo
NewConnect Malawi

Kwa anthu akuntcheu ,Lilongwe, Zomba ,Mwanza ndimaboma ena ,abambo awa akwanitsa kumene zaka 41, amakhala kuntcheu ndipo...
08/03/2026

Kwa anthu akuntcheu ,Lilongwe, Zomba ,Mwanza ndimaboma ena ,abambo awa akwanitsa kumene zaka 41, amakhala kuntcheu ndipo simunthu wa chilendo. Ndi builder odziwika bwino kamba Ka luso lake, komanso ndi mulimi wa mbeu zakumunda ndi kudimba odziwika bwino Madera ozungulira kampepuza. Mu
November 2025 tinapangapo post zoti akufuna mkazi chifukwa mkazi wawo anawathawa atawadyeradyera. Lero
Tapangaso post chifukwa mkazi yemwe adapezeka ndipo zinkaonetsa kuti atha kukwatirana naye ,watengana ndi munthu wina, Athawitsirana Ku south. A Steve tsopano akufuna mkazi yekhayo amene Ali serious ndipo zoti awapusitseso sakufuna, chomwe akufuna ndi mkazi wa serious ofunadi banja.zaka 35 to 40 ,mkaziyo akhale from Ntcheu,or Balaka,or Dedza, or Salima.

 Mayi wina ali mu ululu woopsya pa chipatala chachikulu cha Nchinji atavulazidwa ndi bulu mmamawa walero.Nkhaniyi ikuti,...
03/03/2026


Mayi wina ali mu ululu woopsya pa chipatala chachikulu cha Nchinji atavulazidwa ndi bulu mmamawa walero.

Nkhaniyi ikuti,mayiyu yemwe ndi Maness Sekanawo WA zaka 73 ,amapita kumunda ndipo ali mkati mwaulendo anapeza bulu panjira ali wotopa( wabere) ndipo amavutika kuti aswe.

Mokhudzika ndi chisoni polingalira ululu womwe buluyo amamva,Mayiyu anayandikira ndikuyamba kumuthandiza buluyo mpaka anakwanitsa kubereka koma atalefuka.
Ali chilefukire mayi uja anatenga mwana wabulu uja kumusiya pambali pabwino kuti manthu wake mphamvu zikabwera amupeze Ali pabwino.

Zachisoni,bulu uja atatsitsimuka,anaona Mayi uja Ali mkati mosamala kamwana kaja,apo bulu mpamene analusa kwambiri nkuyamba kulimbana ndimayiyo poganiza kuti akufuna abe mwanawake.
Chifukwa chopanda mphamvu Mayiyo anagwa ndipo buluyo anampondaponda Mayi kumutu ndi pamimba.
Anthu achifundo anathandiza Mayiyo kumuchotsa pamalopo kupita naye kuchipatala komwe akulandira thandizo.

Tsatirani zambiri pano popanga folo NewConnect Malawi

Address

Ntcheu

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when NewConnect Malawi posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share