10/31/2025
Matupi a anthu Asanu ndi atatu, omwe anamwalira pangozi ya bus mu Mzinda Limpopo mdziko la South Africa Alowa mdziko muno kudzera pa chipata cha Mwanza.
Boma lakonza mapemphero pofuna kupereka ulemu otsiliza komwe Mlangizi wa mtsogoleri wa dziko lino pa nkhani za Chipembezo Apostle Timothy Khoviwa akhala nawo pa mwambowu