Nkhwinimba Online

Nkhwinimba Online Arts and entertainment
(3)

16/12/2025

2011 President Bingu akuchokera ku Perth Australia anamuthilapo fire Dickson Kashoti chifukwa chofusa zopepela 😂😂

16/12/2025

Mfumu ya nzinda wa Blantyre Cllr. Isaac Jomo Osman yati ili ndi mapulani aakulu okonzanso nzindawu ndipo anthu ayikhulupilire kuti isintha zinthu

Osman wayankhula izi pa 15 December 2025 ndi atolankhani osiyana-siyana kuchokeranso ku nyumba zoulusira mawu zosiyana-siyana

Iye waulura kuti pa 21 December 2025 akhala ndi mwambo wapadera otulusa tsatane-tsatane wa mapulani amenewa ku hotero ya Armalylis munzinda omwewu wa Blantyre

"Anthu ena akungoona ngati Jomo wabwera kuzasesa m'miseu kapena kuzasuntha anthu opanga malonda malo osayenelera ayi, pali zambiri, muona zinthu zikusintha ndikufuna ndikamadzachoka pa udindowu Blantyre asazakhale chimodzi-modzi, bwerani ku Armalylis muzamve zomwe Jomo wakonza" yatero mfumuyi

16/12/2025

Mawa ndilachabe esh

16/12/2025

Chimwendo wakhala akunyoza Police posayipatsa zofunika nthawi yomwe anali Nduna lero nde akumana maso ndi maso ku cello.

Khalidwe ndi chuma ndipo ndalama zandale sumadya wekha.

Mutipo chani paza Jesse kabwila?
16/12/2025

Mutipo chani paza Jesse kabwila?

Minister of Information and Communications Technology Dr Shadric Namalomba, on Tuesday met with officials from MultiChoi...
16/12/2025

Minister of Information and Communications Technology Dr Shadric Namalomba, on Tuesday met with officials from MultiChoice Malawi at the ministry headquarters.

The meeting was aimed at introducing MultiChoice Malawi to the minister and discuss its operations in the country, with focus on the growth of the creative and broadcasting industry and possible areas of partnership with government.

Her name is Thokozire Munthali, newly appointed District Commissioner for Salima District. Prior to her appointment, Mun...
16/12/2025

Her name is Thokozire Munthali, newly appointed District Commissioner for Salima District. Prior to her appointment, Munthali was serving as Director of Planning and Development (DPD) for Thyolo. She also held the same position in Chikwawa district.

APM is on the drive to empower women by appointing them in decision making positions. Isn't this beautiful amangwethu...!!!?

Mbali ina ya bwalo la Joyce Chitsulo yagwa m'boma la Mwanza kutsatira mvula yomwe yakhala ikugwa chigawo chakumwera. Izi...
16/12/2025

Mbali ina ya bwalo la Joyce Chitsulo yagwa m'boma la Mwanza kutsatira mvula yomwe yakhala ikugwa chigawo chakumwera.

Izi zachitika patangodutsa miyezi itatu mtsogoleri wakale wa dziko lino, Lazarus Chakwera atasegulira bwaloli.

Inu MCP isadzabwelenso

Where Is the Media Now?By Raymond LimbaniIn recent months, headlines were dominated by grim reports of fuel shortages, f...
16/12/2025

Where Is the Media Now?

By Raymond Limbani

In recent months, headlines were dominated by grim reports of fuel shortages, forex scarcity, fertilizer unavailability, food insecurity, and soaring commodity prices. The airwaves and front pages painted a picture of an economy on the brink, leaving Malawians anxious and uncertain about the future.

Today, however, the situation has markedly improved. Fuel is available, forex access has stabilized, agricultural inputs are within reach, markets are functioning, and prices—while still a concern—are no longer spiraling at the alarming pace once reported. Supporters of former President Arthur Peter Mutharika and the DPP credit these improvements to decisive leadership and sound economic management.

Yet this raises an unavoidable question: where is the media now?

If the media were vocal and relentless in highlighting the challenges, should they not be equally visible in reporting improvements? Balanced journalism demands consistency. Silence in moments of progress creates the impression of selective reporting and fuels public suspicion about bias and hidden agendas.

The role of the media is not to cheerlead for any political side, but neither is it to amplify only failure while muting success. Malawians deserve a full picture—one that reports problems when they arise and acknowledges solutions when they materialize.

A free press is vital to democracy, but so is fairness. As the country moves forward, the media must reflect honestly on its role and recommit to informing the public without fear, favor, or political alignment. Anything less risks eroding public trust and undermining the very democracy the media is meant to protect.

NKHANI YOPATSA PHUNZIRO Taphunzila limodzi kuchokera tili ku primary. Nzangayu adali wabwinobwino, amayenda ekha. Tsiku ...
16/12/2025

NKHANI YOPATSA PHUNZIRO

Taphunzila limodzi kuchokera tili ku primary. Nzangayu adali wabwinobwino, amayenda ekha.

Tsiku lina anzanga adapangana kuti andimenye tikaweruka. Tsiku limenelo nzangayu ataweruka adandidikila kufikira pomwe adanditetedzera ku ndewu yomwe adandipanganila.

Tidanyamuka ulendo wobwerera makwathu, tili mnjila driver yemwe panthawiyo adali atalezera adamugunda nzangayu mpaka kukomoka.

Adakatsitsimuka ku chipatala patatha matsiku awiri only to see kuti sakukwanisa kuyenda ekha😢 .

Adayamba kuyendera wheelchair koma kuchokera tsiku limenelo ndidaulonjeza ntima wanga kuti ndidzakhala naye limodzi nthawi zonse .

Pano padusa dzaka 25.

16/12/2025

Nde lero mnyamata ngati iwe udziti msana ukuwawa asa.😂😂

Mkulu uyu anafikapotu

16/12/2025

Mkulukuta Moyo anthu amamukonda heavy 🔥🔥

Address

Johannesburg
46614

Telephone

+27724745081

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Nkhwinimba Online posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Nkhwinimba Online:

Share