Upendo Tv

Upendo  Tv kugawana nkhani ndiku nthandizana manganizo

Nkazi wanga akugonana ndiabwana anga koma sindikupangapo kathu kuopa kuchotsedwa tchito🀌😰.Admin ndikuzivela chisoni kwam...
05/06/2026

Nkazi wanga akugonana ndiabwana anga koma sindikupangapo kathu kuopa kuchotsedwa tchito🀌😰.

Admin ndikuzivela chisoni kwambiri ndipo nditha kufa ndi BP ndizomwe akupanga abwana anga pomagonana ndinkazi wanga,
Izi zinayambika mwenzi watha pomwe ndinakatenga nkazi wanga kumudzi k*ti tidzikhalila limodzi, nkazi wanga wagulilidwa phatso ndi zovala zanyuwani zomwe agula abwana anga zoti or ineyo sindingakwanitse kugula and wayamba kundidelera k*ti palibe chomwe ndimapange paiyeπŸ˜°πŸ’”πŸ’”.

Abwana anga ngakhale akuonesa ngati palibepo ubale ulionse ndinkazi wanga koma ineyo chilungamo ndikuchidziwa moti ndikukanika kubwera poela chifukwa tchito yanga itha k*tha.

Malipiro anga andikwezela cholinga ndizikhala pheee so ineyo ndikukhala odzunguzika mutu kwambiri k*ti kodi ndipange bwanji?
Ndizingoyang'anila zimenezi osawayakhula ,nanga nditani abale ndithandizeni πŸ™.

Follow and share

Copied

HelloAlamu anu kuno ana choka la mulungu koma mpaka pano sakubwera mwina alipo omwe awawonakoamasanduka nkhosa ndikumaka...
04/06/2026

Hello
Alamu anu kuno ana choka la mulungu koma mpaka pano sakubwera mwina alipo omwe awawonako
amasanduka nkhosa ndikumakasa ziweto ndiye business amapanga kwa zaka 12.ndipo ndakhala ndikusunga chisisi ichi kwazaka zonsezi.ndipo pomwe amasandukila kumapita kosaka nkhosa ndipamenepo.malowo ndimaziwa ndine ndekha
Chikundidesa khawa ananyamuka sande kukasaka nkhosa koma mpaka pano sanafike .ndiye mwina anthu awonako nkhosa yachilendo chonde ndithandizeni musapange chipongwe ndi amuna anga.ndili ku Dedza kuno chonde ndithandizeni.
Sindikuziwa k*ti ndichita bwanji chifukwa kumbuyo konseku amati akachoka amabwera tsiku lomwelo sanagonelemo.chonde abale sindikugona tulo ndi kusabwerera kwa amuna anga.

HelloMaliseche anga anasowa Monday mpaka pano sakuwoneka 😭😭😭😭😭😭😭ndili chabe mwamuna koma ndilibe Maliseche. Ndikulilira ...
04/06/2026

Hello
Maliseche anga anasowa Monday mpaka pano sakuwoneka 😭😭😭😭😭😭😭ndili chabe mwamuna koma ndilibe Maliseche. Ndikulilira Maliseche anga sakuwoneka anangosowa after nditagona ndi nkazi ku blantyre 😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Ndinali ku blantyre kokaoda zinthu za business ndiye ndinamva njala ya nkazi poti nkazi wanga anapita kukakolola chimanga mwezi wathau.ndakhala ndekha pano ma week 3 atha
Nkazi yomwe ndinakokayo anali woyela wamatako angati lichelo wamabele ake .ndinampasa yake yomwe amafuna 50 pin .ndinadya ndithu bwino bwino mpaka anati 3rd round andinyengetsa ulele poti ndimapanga bwino ndinamaliza round yachitatu...nditamaliza ndinampempha number k*ti week yamawa ndikamabwera ndizamuimbire koma anakana anati iye samasunga ma number azimuna ndikazamufuna ndizamupeza pomwe ndamupezapo
Basitu ine nditamaliza ndinapita kukapanga za business yanga ndinaoda katundi wanga nditamaliza ndinakwera galimoto kupita kwathu.
Ndinafika ndithu bwinobwino mpaka ndinakataya madzi koma ndinadabwa usiku k*ti set yamaliseche anga kulibe.ndinamvula pant πŸ‘– kuwona k*ti kapena atsakamila pena pake koma ayi ndithu..ndinakhuchumula buluku k*ti mwina athothokela mubuluku koma sanapexeke mpaka pano ndine chabe muthu oti ndilibe Maliseche. Ndipo chindibeleni Maliseche anga sindikulemelaso ndine wopepuka kwambiri 😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Lero lino ndimayenela kupita kokatuma ndlama ya transport ya akazi anga koma ndalephela chifukwa ndikusakasaka njila yoti Maliseche anga abwere.ndinapita kumalo omwe ndinagona ndi nkazi kukafufuza koma ak*ti sakumuziwa nkaziyo pamalopo.ndili pano mutu waima 😭😭😭😭😭😭😭 nditani katundu wanga
Chonde ndithandizeni mwina alipo oti angathe kundithandiza kupeza maliseche anga.sindiliso bwino muganize nyumba yonse k*tenga ..mutu wa banja kungosowa just like that ngati ndi nkhuku πŸ” anthu ukamauza k*ti Maliseche asowa sakumvetsetsa
Ngati alipo wazitsamba oti angandithandize k*ti Maliseche anga abwere chonde ndithandizeni connection

Ndipezeleni mamuna andigone andipase ndalama ya rent mwenzi watha uwuπŸ€ŒπŸ’‹πŸ’‹.Admin a  chonde ndipezeleni cross ya mamuna yem...
03/06/2026

Ndipezeleni mamuna andigone andipase ndalama ya rent mwenzi watha uwuπŸ€ŒπŸ’‹πŸ’‹.

Admin a chonde ndipezeleni cross ya mamuna yemwe angakwanitse kundipasa ndalama yabwino ndipeleke kwa alandlord athuπŸ˜”.

Ndimakhala nyumba ya 80,000mwk ,ndili okozeka kupanga zomwe angakonde mamunayo ineyo ndingofuna ndilipile nyumbai thawi yabwino chifukwa landlord wake amavuta kwambiri ndiye panopa ndalama ndilibe.

Akafunaso atha kubwera konkuno mamunayo tidzacheza bwinobwino asaope ndimakhala dekha.

Follow and share βœ…

03/06/2026

Hey upendo Tangipangileniko post nkhani yangayi anthu andithandinze maganizo munthune pandekha ndikulephela kupenza answer am pregnant for 7 months abambowa Ntchito apagwila koma palibe chomwe amapanga care about our future akapenza ndalama amapanga ma plan pa iwo wokha ndiyeno ankandikakaminza kupita kumuzi chonsecho nditawawunza k*ti agule malata omwe anasala ndi njerwa anandilalatila osati pang'ono koma ndekha ndinagula Malo ndizina zofunikila nyumba bc ndinachivomerenza kumalawi ndinakana kupita nanga ndikafikila pati komaso iwowo ndine palibe sogolo lililonse lomwe ndikhonza kudalila loko ndiyeno ndinakana Lalo akundilembela massage alikuntchito ati ndidzikakhala ndinzanga nyumbayi sakwanisa kulipila alindizochita zambili ndiyeno pamenepo ndidziti chani ineyo ndatopa nanzo saname bola ajanakhala k*t samagwila Ntchito koma ayindithu ndithu Ntchito amagwila yabwinonso . Ndinveken chigoba mukapisita mundikodole thanks

HelloNdikulira amuna anga 😭😭😭😭😭😭. Anasanduka mbalame ya chiwiri, amati akupita ku Lilongwe kwa mai awo, ife ndili ku Chi...
03/06/2026

Hello
Ndikulira amuna anga 😭😭😭😭😭😭. Anasanduka mbalame ya chiwiri, amati akupita ku Lilongwe kwa mai awo, ife ndili ku Chitipa koma mpaka pano sakuziwika k*ti ali k*ti.
Mai awo ndawaimbira lero koma ak*ti sanafike ku Lilongwe 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭.
Chonde ndithandizeni, mwina alipo omwe awona mbalame yachilendo ikuyakhuleni. Momwe amanyamuka, ananyamula chikwama cha black ndipo amati afika ku Lilongwe lachiwiri usiku. Kuno ku nyumba ananyamuka 8 za usiku koma amati ikamafika 12 usiku akhala atafika ku Lilongwe.
Ndili ndi nkhawa. Ndine woyembekezera ndipo sindikudziwa ngati anachita ngozi kapena anakumana ndi mavuto ena.
Chonde number musaikepo. Amuna anga amakonda zamankhwala kwambiri. Ndinawauza k*ti bwanji osangoyenda pa bus 🚌 koma anakana, ati ndalama alibe chifukwa ma bus akudula.

Hello,Kwa zaka 26, bambo athu akhala akusunga mwana wa sister wawo mwachinsinsi m’chipinda. Koma sitinkadziwa k*ti chuma...
02/06/2026

Hello,
Kwa zaka 26, bambo athu akhala akusunga mwana wa sister wawo mwachinsinsi m’chipinda. Koma sitinkadziwa k*ti chuma chomwe takhala tikusangalala nacho, kuphatikizapo ma lorry 🚚 ndi nyumba zambiri, chinachokera kwa mwana ameneyu.
Ife tili ana 6 ndipo tonse takulira pa chuma chimenechi osadziwa zomwe zinali kumbuyo kwake.
Chandibweretsa pano ndi zomwe zachitika posachedwapa. Bambo athu anasandutsa mwana wa sister wawoyo kukhala ngati kapolo ndipo amamusunga m’chipinda momwe amati amapezeramo ndalama.
Tinayamba kudziwa zimenezi pamene mwana wa sister wawoyo anamenya bambo athu nkhonya. Atangomenyedwa, bambo athu anangokhala tsiku limodzi ndipo anayamba kudwala. Akudwala anayamba kuulula zinthu zambiri, kuphatikizapo k*ti mwana wa sister wawoyo sanamwalire monga momwe anthu ambiri ankakhulupirira. M’malo mwake, anamutenga ndi kumusunga kwa zaka zonsezi, ndipo ankamugwiritsa ntchito pa zinthu zomwe zimabweretsa chuma.
Zimenezi ndi zowawa kwambiri chifukwa mayi a mwanayo anasokonezeka maganizo chifukwa cha chisoni chotaya mwana yemwe anali yekhayo.
Tsopano bambo athu akudwala kwambiri. Lero kunabwera anthu a church kudzawapempherera koma thanzi lawo silikusintha. Kuyambira pamene anamenyedwa nkhonya, mlomo wawo unapotozeka ndipo amalankhula movuta moti mawu awo ambiri sakumveka bwino.
Banja lathu likufuna anthu amene angatithandize k*ti bambo athu apeze chithandizo choyenera komanso k*ti cousin wathu, amene wakhala akukhala m’mikhalidwe imeneyi kwa zaka zambiri, nayenso athandizidwe ndi kubwezeretsedwa ku moyo wabwinobwino.
Kwa zaka zonsezi sitinkadziwa k*ti m’chipinda cha bambo athu munali munthu amene amamusunga mwachinsinsi. Zonsezi zatipweteka kwambiri. Mayi athu anamwalira chaka chatha, ndipo mayi a mwanayo nawonso anasokonezeka maganizo chifukwa cha zomwe zinachitika.
Chonde musunge nkhaniyi mwachinsinsi chifukwa ndife anthu odziwika bwino m’tauni muno.

Hello,Kodi mwamuna pakati pa mkazi wake ndi amayi ake, ndani amene ayenera kumugulira galimoto koyamba?Ndikufunsa chifuk...
02/06/2026

Hello,
Kodi mwamuna pakati pa mkazi wake ndi amayi ake, ndani amene ayenera kumugulira galimoto koyamba?
Ndikufunsa chifukwa mwamuna wanga wasankha kugulira amayi ake ang'ono galimoto m'malo moyamba kugulira ine monga mkazi wake.
Chimene chikundipweteka kwambiri n’chak*ti si amayi ake omubereka. Amayi ake anamwalira ali ndi zaka 5, ndipo analeredwa ndi amayi ake ang'ono. Tsopano wapita kukawagulira galimoto chifukwa chofuna kuwathokoza chifukwa chomulera.
Ine monga mkazi wake, ndamuberekera ana awiri aamuna okongola, ndipo ndimaganiza k*ti akanayamba kundisangalatsa ine. Kunena zoona, ndakhumudwa kwambiri moti ndabwerera kwa amayi anga chifukwa mtima wanga wasweka.
Ndikungoganiza k*ti akanagulira amayi anga ndiye ndikanamvetsa bwino chifukwa iwo ndi amene anandibereka.
Kodi inu mukuganiza k*ti zimene wachitazi zik*tanthauza k*ti alibe chikondi ndi ine, kapena kungoti akungoyamikira munthu amene anamlera? πŸ’”πŸ˜­

Hello,sindimaziwa k*ti mwamuna wanga amasanduka fisi usiku ndipo makolo anga akundikakamiza k*ti ndingopilira zakubanja ...
31/05/2026

Hello,
sindimaziwa k*ti mwamuna wanga amasanduka fisi usiku ndipo makolo anga akundikakamiza k*ti ndingopilira zakubanja ndizachinsinsi bola ndikukhala bwino kusiyana ndik*ti ndibwereko ku banja chifukwa iwo alibe ndalama zobweza kwa mwamuna pa zomwe wapanga kwa makolo anga ndi inenso.
Ndinkafuna mwamuna wa chuma ndipo Ambuye adandipatsa mwamuna ndili ku college, wachuma ndipo amandipanga spoil kwambiri. Zonse ankandichitira. Makolo anga anawamangira nyumba ku Zomba ndipo anaika magetsi zonse.
Tikapita ku nyumba kwake amangondikhutulira ndalama ndipo makolo anga pano akudya nyama pakhomo, akukhala bwino chifukwa cha ndalama za mwamuna wanga. Ndili ku college ndimavala zovala zapamwamba kwambiri as well as ma handbags anga ambiri amandigulira kunja akapita.
Ndili pa college ndimawona kuchedwa k*ti ndimange banja. Pano ndili ku banja, tinapanga ukwati mu December koma ndimakhala odabwa k*ti every midnight mwamuna wanga amachoka ku chipinda mwina for an hour asanakabwere. Ndimangoganiza k*ti ali pa internet kulankhula ndi ma customer ake za business.
Izi zakhala zikuchitika usiku uliwonse mpaka mwezi unowo kumayambiliro ndinaganiza zopanga check k*ti amatani. Atachoka kuchipinda ndinamlondola koma samadziwa. Kenako ndinawona akuvula sapato ndikusanduka fisi. Ndinajambula photo ndipo ndinabwerera ku bed.
The following day zinachitikanso ndipo ndinajambula pic ndikupita ku nyumba kwa makolo anga ndikawawonetsa ndikuwafotokozera momwe zinthu zikhalira, k*ti munthu wabwino yemwe ndimaganiza k*ti ndi mngelo, usiku amasanduka fisi.
Makolo anga ndinawauza k*ti basi ndichoke ngakhale ndili ndi mimba koma anakana. Ati sangakwanitse kubweza ndalama zonse zomwe bamboyo adalowola komanso zabwino zomwe awachitira. Moti anandiuza k*ti ndibwerere ku banja komweko, ati limenelo ndilo banja. M’banja umasunga zinsinsi.
Ndili pano ku banja koma sindikusangalala. Mwamuna wanga yemwe ndimakonda kwambiri amasanduka fisi, ndipo makolo ak*ti ndisachoke. Ndili ndi zaka 25 ndipo mwamuna wanga ali ndi zaka 47. Tikukhala bwino kwambiri. Ali ndi ana awiri kuchokera kwa mkazi woyamba amene anamwalira, anawo ali ku school ndipo amandikonda kwambiri chifukwa ndinalonjeza kuwapatsa chikondi ngati ana anga.
Koma ndikaganiza zoti amasanduka fisi usiku ndimangofuna nditachoka, koma makolo akukana.

31/05/2026

Hello
Nkazi wanga wandipha ine kuno ku Bangwe😭😭😭😭😭😭
Nkazi wanga amasunga chisisi cha nzake osandiuza k*ti ali ndi edzi and ine ndinamufusila mpaka ndakhala ndikudyamo kwa miyezi iwiri😭😭😭😭😭😭
Lero ndipo ndapeza k*ti nkazi wanga ali ndima botolo ama ARV mmanja so ndamufusa zukhala bwanji ndipomwe amanena k*ti nzakeyo anazasungitsa kwa nkazi wanga ati samafuna k*ti mwamuna yomwe anabwera ku nyumba kwake aziwe zoti akumwa😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Koma ngati ndingozipha .ndili pano mutu sukuyenda. Nzawoyo angoziwana miyezi ingapo yapitayo monga nkazi olo kundifotokozelapo k*ti nzawoyo akumwa mankhwala 😭😭😭😭😭😭
Ndichite bwanji abale, nkazi sakuziwa k*ti nzakeyo ndimagona naye.

Address

Durbanville
Cape Town

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Upendo Tv posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share