Peter Nkhoma

Peter Nkhoma Content creator

17/09/2026

Imfa ya Kasambala ikuoneka kuti inali nyambo yofuna Chilima, watelo Nkosi.

Zikuoneka kuti imfa ya Ralph Kasambala inali nyambo yofuna kukola Chilima, koma ndizodandaulitsa kuti akubanja la Kasamb...
17/09/2026

Zikuoneka kuti imfa ya Ralph Kasambala inali nyambo yofuna kukola Chilima, koma ndizodandaulitsa kuti akubanja la Kasambala akukana kuti pachitike kafukufuku.

Kodi ine nditapha mwana wanga boma lingalephele kundifufuza chifukwa ndimwana wanga? Koma machitidwe ake akakhala amenewa titha tonse mwina tsiku lina muzangomvanso kuti Nkosi wafa, wamaliza motelo Nkosi.

17/09/2026

Ndine amene ndinathandizila kuti ndege ija ipezeke koma ndine odandaula kuti sanandiitane kumaliro olo amodzi.

Ndine adandaula kuti sindinaitanidwe kumaliro aliwonse awanthu omwe anafa pandege aja.Ndinapangitsa kuti ndege ija ipeze...
17/09/2026

Ndine adandaula kuti sindinaitanidwe kumaliro aliwonse awanthu omwe anafa pandege aja.

Ndinapangitsa kuti ndege ija ipezeke ndine koma olo maliro amodzi sindinaitanidwe, watelo Nkosi

Mboni yalero ikungosakaniza nkhan, ayambe iyi asiye akatelo adumphile ina, mwachidule mboni iyiyi ndiye aaaa madzi enien...
17/09/2026

Mboni yalero ikungosakaniza nkhan, ayambe iyi asiye akatelo adumphile ina, mwachidule mboni iyiyi ndiye aaaa madzi enieni.

Inu mukumumva bwanji Nkosi?

17/09/2026

Mr Nkosi kupelekela umboni wazomwe anaona pa 10 June 2024.

Felix Njawala writes ✍️ Kodi ma guy a MCP mumandinena kuti mutu wanga ndiwaukulu, tinene kuti Dedza Kasina wakewu ndiwau...
17/09/2026

Felix Njawala writes ✍️

Kodi ma guy a MCP mumandinena kuti mutu wanga ndiwaukulu, tinene kuti Dedza Kasina wakewu ndiwaung'ono?

17/09/2026

Akubwelatu lero kuzapelekela umboni wake ofunika kusunga bundle yokwanila.

Bola tisamvenso ena akunena kuti ameneyo wadya ndalama, izi anayankhula ngozi itangochitika kumene.

Saulos Chilima anachita kuphedwa ndipo zimenezo sindimakaika, pangatalike bwanji anthu omwe anaona zimenezi azabwela poy...
17/09/2026

Saulos Chilima anachita kuphedwa ndipo zimenezo sindimakaika, pangatalike bwanji anthu omwe anaona zimenezi azabwela poyela ndikuuza dziko, anatelo Bon Kalindo miyezi 8 yapitayo.

Mawu anu ndi otani kwa DC Kalindo?

Lero kulinso ntchito ku parliament pamene kukubwela Mr Nkosi ndi anthu ena, Mr Nkosi ndi mkulu uja anaoneka pa Zodiak ak...
17/09/2026

Lero kulinso ntchito ku parliament pamene kukubwela Mr Nkosi ndi anthu ena, Mr Nkosi ndi mkulu uja anaoneka pa Zodiak akufotokoza mmene zinakhalila.

Address

Cape Town
6900

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Peter Nkhoma posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Peter Nkhoma:

Shortcuts

Share