Peter Nkhoma

Peter Nkhoma Content creator
(2)

04/09/2025

Kusinthasintha boma kumapangitsa kuti dziko lisatukuke, ndipo ife monga azitumiki a Mulungu tikunena kuti boma la Chakwela lipitilila chifukwanso latisamalila ife azitumiki potipatsa ngongole zochuluka kwambili zomwe maboma ena sanatichitile.

04/09/2025

Kafukufuku amene wachitika wanena zoona ndithu ndipo zoti a Chakwela ndi otchuka ndizoona ndithu koma sanatchuke pazinthu zabwino, mmene watchukila Chakwela ndi chimodzimodzi ndi satana kutchuka ndizoipa zokhazokha, akutelo akuluwa.

04/09/2025

Kafukufuku amene wachitikayi ndiwabodza MCP singaluze ayi zimenezo ndiye muiwale, ndipo achewa tilipo ambili mutidziwa pa 16 September pano, watelo mkuluyi.

04/09/2025

Nicholas Dausi kuyamikila president Chakwela kamba komanga stadium ku Mwanza.

04/09/2025

Shadow MP wachipani cha MCP yemwe akuimila ku Mwanza west Maureen Chitsulo kuyankhula pamwambo omwe unaliko lero otsekulila Mwanza stadium, imenenso yasinthidwa kuchoka pa Mwanza stadium mkukhala Joyce Chitsulo stadium.

From Mwanza stadium to Joyce Chitsulo stadium, President Lazarus Chakwela wati stadium yomwe yamangidwa ku Mwanza tsopan...
04/09/2025

From Mwanza stadium to Joyce Chitsulo stadium,

President Lazarus Chakwela wati stadium yomwe yamangidwa ku Mwanza tsopano izitchedwa Joyce Chitsulo stadium pofuna kulemekeza ntchito zomwe anagwila.

Kafukufuku amene wachitika waonetsa kuti  anthu 41 pa 100 alionse adzavotela Peter Muthalika pamene anthu 31 pa 100 alio...
04/09/2025

Kafukufuku amene wachitika waonetsa kuti anthu 41 pa 100 alionse adzavotela Peter Muthalika pamene anthu 31 pa 100 alionse adzavotela Lazarus Chakwela

Kafukufuku amene wachitika waonetsa kuti Lazarus Chakwela ndiye mtsogoleri amene akudziwika kwambili kuposa aliyense pac...
04/09/2025

Kafukufuku amene wachitika waonetsa kuti Lazarus Chakwela ndiye mtsogoleri amene akudziwika kwambili kuposa aliyense pachisankho chimenechi.

03/09/2025

Part 2 yanyamata amene anabedwa atangobadwa kumene pachipatala cha Queens ku Blantyre mkupezeka ali ndi dzaka 29, mayi ake akufokotokza mmene zinakhalila.

Azimayi kumasamala mukabeleka kumene.

03/09/2025

Azimayi kumasamala mwana akangobadwa kumene kuchipatala, mayi awa anabeledwa mwana mkunamizidwa kuti wamwalila koma anapezeka patatha dzaka 29.

02/09/2025

Mkuluyi kuchokela kwa Msundwe akuti MCP idutsa kamodzi ndi kamodzi ndipo zipani zina zisapuse kuti kukhala chibweleza, komanso akuti anthu omwe akumapita misonkho ya DPP angofuna kukawaona a Muthalika.

Inu maganizo anu ndiotani?

02/09/2025

Chipani cha DPP chiwina kamodzi ndi kamodzi chifukwa anthu akupita okha kumsonkhano komanso sakulandilako maheu, akutelo akuluwa.

Address

Cape Town

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Peter Nkhoma posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share