M-Feja

M-Feja no sweet without sweat.

06/12/2025

Wafika ndi Moto , kubanja kukamvuta zedi😂🙌

*NKHANI YOMVETSA CHISONI*Azipha atazindikira kuti mamuna wake yemwe wakhala ku theba zaka zisanu ali ndi banja linaso ku...
05/12/2025

*NKHANI YOMVETSA CHISONI*

Azipha atazindikira kuti mamuna wake yemwe wakhala ku theba zaka zisanu ali ndi banja linaso ku thebako.

Mzimayiyu dzina lake ndi Monica, iye wakhala akuthandizila mamuna wake pomanga nyumba yomwe imamangidwa pa khomo kwawo kwa mamuna

Koma chachititsa kuti aziphe ndi choti ena atabwela kuchokera ku theba adamuwuza kuti amuna anu adakwatilaso ku theba ndipo ali ndi mwana. Powawidwa mtima adangotenga makhwala ophera tizilombo ndikumwa imfa idali yomweyo

Koma olo zitamvuta maka osamafika size yozimpha men let's be loyal kwa akaz Omwe tachoka nawo pamtali this is sad 😭😭

05/12/2025

Anyamata azanga Ati tizintchuza wayizile zozimangiliraz taonjeza akweni akumtelo😃😃🙌😂 forwarding and follow then U help me

   mwakathithi pa page pano zikachitika mumvela Ku  Mabanja oposa 300 akusowa pokhala pomwe anthu ena avulala nyumba zit...
05/12/2025

mwakathithi pa page pano zikachitika mumvela Ku

Mabanja oposa 300 akusowa pokhala pomwe anthu ena avulala nyumba zitawagwera kutsatira mvula ya mphamvu ndi ya mphepo yomwe yagwa mmadera ozugurila tauni ya Liwonde m'boma la Machinga.

Izi ndi malinga ndi phungu wakunyumba ya Malamulo kudera la Likwenu ku m'bomali a Tulinje Muluzi ndipo iwo apempha boma komanso mabungwe ndi ena akufuna kwabwino kuti athandize mabanja okhudzidwawa ndi chakudya komanso zina zowayenereza mu nyengoyi

Polankhula pomwe amayendera anthuwa, a Muluzi ati alephera kukakhala nawo ku zokambirana zakunyumba ya malamulo dzulo kaamba kokhudzidwa ndi ngoziyi yomwe yaononga zinthu zambiri.

Mvulayi yagwetsa nyumba zochuluka, kusasula midadada ya sukulu komanso kugwetsa ma polo amagetsi a madera omwe azungurila tauni ya Liwonde monga Kaudzu, Chabwera komanso Saiti omwe ali pansi pa mfumu yaikulu Sitola m'boma la Machinga.

Pakadali pano, mkulu wa zamaphunziro m'bomali a Douglas Namikungulu ati masiku akubwerawa, maphunziro akhala ovuta kukwaniritsa m'bomali maka msukulu zomwe zakhudzidwa pamene nvula ikupitirilabe.

📝NEWS UPDATE

Driver wa minibus Taxi wadzipha podzimangilira ku Atteridgevile Mshongo ku South Africa mkazi yemwe anamuonongera ndalam...
05/12/2025

Driver wa minibus Taxi wadzipha podzimangilira ku Atteridgevile Mshongo ku South Africa mkazi yemwe anamuonongera ndalama zambiri atamusiya.

Bamboyu anali ndi mkazi yemwe anamupatsa mimba atangolemba mayeso a form 4 (metric). Mkaziyu atabeleka mwana taxi driver yu anamuuza kuti abwelereso ku school ndipo mkaziyo anayamba school ya udokotala. Adha awa akhala akumulipilira school fees komanso kumamupatsa ndalama zoti azigula zofuna za moyo wake mtsikanayi mpaka Chaka chatha anamaliza nkuyamba ntchito yau dokotala

Nzachisoni kuti mkaziyo atangoyamba ntchito anamusiya mamunayu nkupeza mamuna wina kumati sangakwatirane ndi munthu oyendetsa minibus taxi. Ku whatsaap mkaziyo analemba izi zomwe zinamupweteka taxi driver 🥺😰

“Just because you paid for my studies and helped me find a job doesn’t mean I owe you anything.”

“If you don’t love him anymore, leave him and find someone you’ll love. You have a right to lose interest.”

Gender iyiyi eeeh

Ngat zamvuta kulibwino osabadwsa mwana azimayi😢😢 Mwana uyu anaponyedwa chimbuzi anthu ena odutsa anamuvera mkuyitana ant...
05/12/2025

Ngat zamvuta kulibwino osabadwsa mwana azimayi😢😢

Mwana uyu anaponyedwa chimbuzi anthu ena odutsa anamuvera mkuyitana anthu kuchotsamo apeza ali bwino bwino amutengera ku chipatala tiyeni timfunile mafuno abwino mwini mwanayo sakudziwika

Chonde chonde azimayi amzaga ngati simukufuna kubeleka kalera ndiwa ulele kuchipatala or ikitsani chapa mkono cha zaka 10 kuti musabele mkusiyana mkutenga mimba ndikudzataya mwana ndikulakwa uku ku zuza mzimu amzanu ena akulira usana ndi usiku ku kwela mampili kufuna mwana inu mukutaya azimayi otelemu mulungu akulangeni ndinthu ndikulakwa ku zuza mzimu osalakwa

Please follow, help by forwarding nkhani zochitika in different groups to make this page grow 🙏🙏

04/12/2025

Ichi chipweteka gulu , English version Artist kawawa😄😄😄😃🙌

Secondary up to College wakhala akulipilidwa Fees ndi chibwenzi chake , after kumaliza zonse anakana kukwatilana ndi bwe...
04/12/2025

Secondary up to College wakhala akulipilidwa Fees ndi chibwenzi chake , after kumaliza zonse anakana kukwatilana ndi bwenzi lakelo

Apa ndi uyu wapengayu
Nyo kwa nyoo bas 😄

04/12/2025

ngati muli ndinkhani
zitilowelani Ku inbox tizitumiza pamuz Pano nkhani iliyonse chonde anthu inu ya mdela lilironse .. together we can make this page grow big .Kaya Ku WhatsApp any latest news ndinthu ., 👍💪

04/12/2025

Zisankho zamtima zikuzudzitsa liva .. nyimbo iyi angoyipweteka bas 😄🙌 Koma Loiso iweyo

04/12/2025

CHIMWEMWE WAFERA KU NKHONDO 😭😭😭😭💔💔💔. TILIRE MOTANI AMATA??

Usiku wathawu Chimwemwe wagwidwa akuthira batire mkazi wa mwini ku Dedza nthawi ya 10 o'clock usiku ndipo mamuna wa mkaziyu wagwira yekha ataimbiridwa phone ali ku ntchito,iyeyu ngwa police.
Onerani

Kumapeto kwa nkhaniyi zikuonetsa kuti a Chimwemwe aomberedwa ndi mwini mkaziyu.

Rest in Chimwemwe

Taxi Bosses Shot Dead/ Aombera ndikupha oyang’anira ma taxi ku ThebaAkulu akulu oyang’anira ma minibus taxi aku Alexandr...
03/12/2025

Taxi Bosses Shot Dead/ Aombera ndikupha oyang’anira ma taxi ku Theba

Akulu akulu oyang’anira ma minibus taxi aku Alexandra Taxi association aomberedwa dzulo pa ma robots ali mu galimoto Yao. Izi zachitika ku Midrand Gauteng province dzulo pa 2 December 2025

Ma bwana a taxi association wa anali mu galimoto Yao ndipo anaima ma robots pa ma robots atatseka ndipamene kunatulukira zigawenga zomwe zinali ndi mifuti nkuwaombera awiriwa kambirimbiri ndipo anafera pompo. Awiriwa wina anali wa zaka 53 wina wa zaka 38. Aka sikoyamba ayi ndipo anthu ambiri adandaula chifukwa cha infa za oyang’anira ma minibus taxi ku Johannesburg

Two taxi bosses travelling in Toyota Corolla were gun down in Midrand in Gauteng on Tuesday the 2 of December 2025. A 53 year old and 38 year old members of Alexandra Taxi Association (ATA) were ambushed at a traffic light by heavily armed suspects.The police have launched a manhunt to bring the culprits to book. It is believed that taxi violence in Gauteng has now escalated.

Address

Cape Town
7441

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when M-Feja posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share