M-Feja

M-Feja no sweet without sweat.

Bambo yemwe amangozowika ndi dzina loti Jamaica wadulidwa dzanja ku Karonga ndi mwini ndalama yemwe anabwerekesa ndalama...
07/03/2026

Bambo yemwe amangozowika ndi dzina loti Jamaica wadulidwa dzanja ku Karonga ndi mwini ndalama yemwe anabwerekesa ndalamazi, mkuluyu waona izi atalephera kubweza ngongole yokwanira K25 million yomwe anamubwereka odula mkonoyu.

Muchithunzimo udulidwa mkono ndi odula dzanjayu.

🚨 Triple Murder ku Joe Slovo, Milnerton 🚨Kuphedwa  kwa anthu atatu kukufufuzidwa kutsatira kuwombera pakona ya Omarombo ...
22/02/2026

🚨 Triple Murder ku Joe Slovo, Milnerton 🚨

Kuphedwa kwa anthu atatu kukufufuzidwa kutsatira kuwombera pakona ya Omarombo Street ndi Freedom Way ku Joe Slovo, Milnerton, Cape Town.

Apolisi adapeza Toyota Avanza yasiliva yomwe ili ndi zipolopolo zingapo pamalopo. Mkati mwa galimotoyo, matupi aakazi awiri achikulire adapezeka ndipo adanenedwa kuti amwalira. Pafupi ndi mamita ochepa, mtembo wa mwamuna wazaka 36 unapezekanso.

Cholinga cha chiwembuchi sichikudziwikabe, ndipo kafukufuku akupitilira.

nako Ku parliament wina wachigwesa chake chopuma 🤣🤣🤣Malawi eeeeh tikapuma kumwamba
20/02/2026

nako Ku parliament wina wachigwesa chake chopuma 🤣🤣🤣Malawi eeeeh tikapuma kumwamba

20/02/2026

Anthu tikukumana nazo mmaderamu..njuchi kumvuta kufuna munthu asayikidwe eeeh🙌🙌🙌

NKHANI YA CHISONI 😭 💔Bambo wachikuda mukumuonayu dzina lake ndi Calvin M***a wazaka 33 ,mzunguyo dzina lake ndi Adriaan ...
20/02/2026

NKHANI YA CHISONI 😭 💔

Bambo wachikuda mukumuonayu dzina lake ndi Calvin M***a wazaka 33 ,mzunguyo dzina lake ndi Adriaan Van Tonder wazaka 71.

Calvin ndi Adrienne amapanga rent pa yard imodzi ku Eloff, Mpumalanga. Chifukwa cha vuto lamadzi lomwe lili ku Eloff ko, a landlord anawayikila Jojo tank kuti azithandizika madzi akasiya. Ndiye akuti Jojo tank inali ndi ma pipe awili ina yopita mu room ya Calvin ina yopita mu room ya Adriaan,koma tankyi inayikidwa ku side ya room ya Adriaan.

Ndiye akuti tsiku lina Adriaan anadula pipe yamadzi yopita mnyumba mwa Calvin, zomwe zinampangitsa Calvin kuwauza a landlord. A landlord analamura kuti Adriaan abwezeletse pipe ija. Ndiye akuti Calvin anadzapita ku shop kukagura zinthu, tsiku lake lomwelo koma pobwelera anapeza kuti Adriaan wachotsanso pipe ija, ndipo mnyumba mwake mulibe madzi.

Akuti apa mpamene Calvin ananyamuka ndi mwana, wake wa 9 years kukalumikiza pipe ija. Akuti ali mkati molumikiza pipe ija mpamenetu mkangano unabuka pakati pa azibambo awiliwa. Akuti Adriaan mpamene anatenga mfuti mkumuombela Calvin kambiri mbiri ndipo anamwalira pamaso pa mwana wake (mnyamata) wa 9 years. 😭 😭 😭 Mwana uja anayamba kukuwa ndipo mayi ake anabwela kumupeza Calvin waombeledwa. Akuti Adriaan ataona mkazi wa Calvin akulira anayamba kumuopsyezanso kuti nayenso amupha. Koma mkaziyo anakwanitsa kuyimbila apolisi ndipo Adriaan anamangidwa. Ndipo anakaonekela ku court lachiwiwili lathali pa 17 February ku Mpumalanga .

Zomvetsa chisoni kuti mwana wa 9 years anaonelera kuphedwa kwa bambo ake, ndipo ndi zinthu zoti zimpanga traumatise moyo wake onse. 💔 😭 Komanso mkazi wa Calvin ndi oyembekezela. Ku South Africa ka nkhani pang'ono amaona kuti solution ndikupha eeish. Dziko la usatana ili. Munthu wazaka 71,zachidziwikile akafela kundende komko.

Koma Theba 😭💔Ndauzidwa kuti M'malawi zanthu wamwalira ataomberedwa ndi mfuti ku fisantekraal South Africa mamawa wa lero...
19/02/2026

Koma Theba 😭💔

Ndauzidwa kuti M'malawi zanthu wamwalira ataomberedwa ndi mfuti ku fisantekraal South Africa mamawa wa lero

Dzina lake ndi Ishmael Koma malingana ndimalipoti adawa akuti analowa gulu lama gangsters ndye gulu lawo linakapha anthu agulu Lina ndye anabwela kuzabweza chifukwa adawa amphedwa ndi Malawi amachokera b0ma nkhokatoka akuti 😭😭😢

Rest in peace... Koma Pena zopeweka tizipewa kuno koyenda amalawi. .zomwe timachita kumalawi kubweletsa kuno ndi ifa ndinthu .

Agalu olusa a mtundu wa Pitbull sabata yatha adaluma ndikupha garden boy kapena kuti ogwira ntchito ku garden ya mzungu ...
19/02/2026

Agalu olusa a mtundu wa Pitbull sabata yatha adaluma ndikupha garden boy kapena kuti ogwira ntchito ku garden ya mzungu ku Durban ndipo dzulo agalu amtundu omweu wa Pitbull alumaso garden boy wa nzungu ku Balista ku KZN mpaka kumuvulaza modetsa nkhawa mwayi sanafe wangovulala.

Nkhaniyi akuyiphiphilitsa chifukwa anthu omwe alumidwawo ndiobwera koma please tiyeni tikhale osamalitsa tikamapita ku ntchito mmanyumba azungu komwe kuli agalu amtundu uwu izi ndi zilombo zoopsa sizimamva stop it olo mwini wake ali apo..ndye kuwona agalu awa better kumauzilatu abwanawo aziwatsekela until mutamaliza ntchto

Remember agalu omwewa analuma mpaka kumupha mwini wake ku Mitchell’s plain Cape Town

SOUTH AFRICA:🇿🇦A police Ku south Africa agwira mwana wa former president malemu Robert Mugabe, kamba kowombera wantchito...
19/02/2026

SOUTH AFRICA:🇿🇦

A police Ku south Africa agwira mwana wa former president malemu Robert Mugabe, kamba kowombera wantchito wake yemwe ndi garden boy, kunyumba yeke yomwe ili ku Johannesburgn kudela lotchedwa Hyde park.

Ndipo garden boy yemwe wa womberedwayo a police anayitanisa ambulance msanga ndipo athamangira naye kuchipatala koma panopa sitikudziwa kuti amuwombela malo ati komanso panopa sitinamve lipoti lililonse akuchipatala momwe alili munthu owombeledwayo.

ZACHISONIWamwalira Ali mu njira kuchoka ku Malawi kupita ku South Africa. Sanadwale komanso sadachite ngozi. Adangogwa b...
19/02/2026

ZACHISONI

Wamwalira Ali mu njira kuchoka ku Malawi kupita ku South Africa. Sanadwale komanso sadachite ngozi. Adangogwa basi imfa kukhala yomweyo.

18/02/2026

Boys will be boys, and another reason why women live longer than men 😮😳🤣

Memory kamange Waphedwa ku lilongwe😭  😭 Memory anasowa pa 11 feburary chaku mamawa mbali ya ku lilongwe TTC ndipo lero a...
17/02/2026

Memory kamange Waphedwa ku lilongwe😭 😭

Memory anasowa pa 11 feburary chaku mamawa mbali ya ku lilongwe TTC ndipo lero apolice agwira anthu ena omwe Apezeka ndi phone ya Memory, ndipo anthuwo avomera kuti adamuphadi tsikanayu.

Pakadali pano sizikudziwika kuti thupi la tsikanayu anthuwa adali ponya kuti ndipo anthu omwe adapha tsikanayu akuti ndiochokera kwa mgona. Aaaah malawi iwe 💔 😭 iwe malawi wanga wayiii💔 😭

Source:Hastings Msosa ゚viralシalシ ゚viralシalシ

MalawiChikwawa ChichewaChikwawa - Osasewera ndi Amalawi Madolowa anapeza galimoto yamalilo nkuikamo coffin koma amathawi...
16/02/2026

Malawi

Chikwawa
Chichewa

Chikwawa - Osasewera ndi Amalawi
Madolowa anapeza galimoto yamalilo nkuikamo coffin koma amathawisa matumba amakala. Anapakila matumba amakala ambiri mbiri nkumaoneka ngati Malilo kupusisa apolice. Boys inaikamo olila, Azimai anyimbo

English language
You can't believe this ! Yes it's happening in Malawi

So these are charcoal smugglers. They faked a funeral convoy this morning and even purchased a coffin and yet the vehicles had carried hundreds and hundreds of charcoal. Unfortunately Chikwawa police has managed to foil the plan. They even hired some women to be crying on top of their voices when ever they see police men

Source : Times 360

Address

Cape Town
7441

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when M-Feja posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to M-Feja:

Share