VOMI News 247

VOMI News 247 VOMI News 247 is Malawi's leading social media platform and Television station based in Dublin Ireland

🚨 𝗕π—₯π—˜π—”π—žπ—œπ—‘π—š: Mtogoleri wa North Korea Kim Jong-un wavomera kuti ayamba kuonetsa Premier League m'dziko lawo koma pakhala ...
13/11/2025

🚨 𝗕π—₯π—˜π—”π—žπ—œπ—‘π—š: Mtogoleri wa North Korea Kim Jong-un wavomera kuti ayamba kuonetsa Premier League m'dziko lawo koma pakhala malire:

β€’ samaonetsa ma game live, azipanga edit Kaye asanaonetse.

β€’ Azichotsa footage yomwe paoneka ma player a South Korea. Ma player ngati Kim Ji-soo (Brentford) and Hwang Hee-chan (Wolves).

β€’ Game izikhala 60 minutes osati 90 minutes.

β€’ Mawu achizungu amene aoneka Ku stadium azibisidwa ndi zithunzi za chi Korea

β€’ Adzichotsa chili chonse chomwe chaonetsa mathanyula

CONGRATULATIONS LEAH MALEKANOAs she is now Public Relations Officer for the Ministry of Foreign Affairs.Surely Vomi News...
13/11/2025

CONGRATULATIONS LEAH MALEKANO

As she is now Public Relations Officer for the Ministry of Foreign Affairs.

Surely Vomi News 247 reporters are next as our patrons Henzo and Arbeto will be taking over ministerial positions soon.

Koma mukusevana ngati chakudyatu
13/11/2025

Koma mukusevana ngati chakudyatu

Thupi la malemu a Gertrude Gondwe tsopano lafika ku tchalitchi cha St Andrews CCAP mu mzinda wa Mzuzu komwe kukhale mwam...
13/11/2025

Thupi la malemu a Gertrude Gondwe tsopano lafika ku tchalitchi cha St Andrews CCAP mu mzinda wa Mzuzu komwe kukhale mwambo wa mapemphero.

Malemuwa anali mkazi wa yemwe anakhalapo nduna ya za chuma mu ulamuliro wa Bingu wa Mutharika Goodall Gondwe

Mabungwe a CDEDI ndi Lost History Foundation lero akupeleka kalata kunyumba ya malamulo yopempha aphungu kuti akambirane...
13/11/2025

Mabungwe a CDEDI ndi Lost History Foundation lero akupeleka kalata kunyumba ya malamulo yopempha aphungu kuti akambirane zokhazikitsa lamulo lovomeleza aphunguwa kuchita zokambirana zawo mu chichewa.

Kwa anzathu okufa ndi imodzi inde inu a Betting Juga kapena kuti Gambling.Nzanu uyu walowa m'manda ndi ma ticket ake oku...
13/11/2025

Kwa anzathu okufa ndi imodzi inde inu a Betting Juga kapena kuti Gambling.

Nzanu uyu walowa m'manda ndi ma ticket ake okufa ndi imodzi atadyetsa ndalama zake zonse ndatitu zonse.

Maliro tilira koma komabeta mosamara Bet Responsibly

This is one Bashir Al Bashir on his assessment of the plane that crashed in Thungwa Chikangawa Forest.He says Ndegeyi in...
13/11/2025

This is one Bashir Al Bashir on his assessment of the plane that crashed in Thungwa Chikangawa Forest.

He says Ndegeyi inagwa at exactly 1 hour. Osatinso 1 hour and 2 seconds, 1 hour basi. Do you know why?

Akuti kunali bad weather ya chifunga. From my experience, chifunga chimakhala chambiri at the opening of the day, chimapepuka kukamacha in most cast cases, tsikuli ananyamuka kuli chifunga, how were they able to track the Mz-LL route without deviation around 7-8 am and fail to use the proper route pobwelera kumapedzeka angodzungulira ngati aledzera, same pilots, same craft.

Why did the president hold the information of the missing plane mpaka madzulo mma 2 o'clock, ndege yosowa 10.am, what was his reason?

Ndege yoti iri ndi mafuta a 2 hours only, why did the president instruct army commander to give him information only after 4 hours?

Where in Chikangawa kuli nkhalango yokhwitima yoti anthu angakanine kuyenda, army officers for that matter? Where, why did the commander lie to us kuti kuli nkhalango yokhwitima?

Why, was Chilima's body found somewhere isolated when obviously he was seating close to his bodyguards, why was his body alone and not close to the plane.

Inde ngozi does destroy zovala, how was his his jacket out of his body, as tight the belt, lamba wamchiuno anavuka bwanji?

Nchifukwa ninji wa MCP anakanizidwa kukwera ndege, you can't lie to me kuti Dr. Shanil Muluzi and others were more senior to Chimwendo on protocol, never, and don't lie to me kuti Chilima anawakaniza, he flew the previous days to Korea with Sam Kawale and Kunkuyu in the same plane sanawakanize imeneyo bwanji?

Where is the guard of the tower that the plane fell close to, alikuti, can someone get that one and we hear from him what he knows.

Ndege inagwera pa fumbi why does it have that high impact and why sinayake.

In my opinion, there is no proper investigation that answered most critical questions outside these, some even more technical. Report ya Sundi ija unali uzereza wa anyamata amugafa trying to be clever and think all of us are fools.

Mzimayi uyu amupeza ali mbulanda atagonekedwa pafupi ndi nyumba yina yake ku Sekampaneng Unit 7 ku North west province, ...
13/11/2025

Mzimayi uyu amupeza ali mbulanda atagonekedwa pafupi ndi nyumba yina yake ku Sekampaneng Unit 7 ku North west province, South Africa malingana ndima report akuti nzimayiyu anali ndi umuna wambiri komanso watupa mphechepeche zomwe zikuonetsa kuti wagwililidwa ndi anthu ochuluka. Anthu achifundo ndiomwe anamumveka zovala zomwe zinali chapafupi ndi iye. Ndipo amutula ku police

Ngakhale kuti amusiya ndi moyo koma Munthuyu sakulankhula komaso sali bwino sakudziwa komwe ali komanso chomwe chamuchitikira umu ndi mmene akumawaphera azimayi ku Joni mmhu Ambuye alowelerepo basiπŸ™

Apolisi ku Ntchisi usiku uno aphulitsa utsi okhetsa misonzi pofuna kubalalitsa ophunzira omwe amafuna  kuthana ndi munth...
12/11/2025

Apolisi ku Ntchisi usiku uno aphulitsa utsi okhetsa misonzi pofuna kubalalitsa ophunzira omwe amafuna kuthana ndi munthu wina yemwe akuti anathawira kuchipinda chogona anyamata pa sukulu ya Sekondale ya Ntchisi pomuganizira kuti anakaba m'mudzi ozungulira otchedwa Chiwembe.

M'neneri pa polisi ya Ntchisi Salomy Zgambo watsimikiza za nkhaniyi.

Malinga ndi ophunzira omwe tayankhula nawo, iwo amafuna kuthana ndi yemwe akuganizilidwa kuti ndi mbavayo kamba koti dzana katundu wa ophunzirawa monga zovala zinabedwa.

Zina ukamva πŸ’” 😭Ophunzira uyu James ankakhulupirira kuti kusala kudya kwambiri kwa masiku 40 kungathandize banja lake kut...
12/11/2025

Zina ukamva πŸ’” 😭
Ophunzira uyu James ankakhulupirira kuti kusala kudya kwambiri kwa masiku 40 kungathandize banja lake kuthana ndi mavuto awoβ€”koma kufuna kutsanzira Yesu kunatsala pang’ono kutaya moyo wake.

Iyi ndi nkhani yozama kwambiri yokhudza chikhulupiriro ndi malire.

JAMES , anatsimikiza mtima kuthandiza banja lake panthaši yazovuta. Anayamba kukhala ndi nthawi yayitali yopemphera komanso kusala kudya, pokhulupirira kuti ndi yankho la zovuta zawo. Anakwanitsa kusala kudya masiku 40 usana ndi usiku. Kumeneko ndi kudzipereka kodabwitsa.😒

Komabe, pa tsiku la 41, zinthu zidalakwika kwambiri. Thupi lake linafowoka, ndipo anathamangira naye kuchipatala kuti akalandire chithandizo .

Mnzakeyo anatsimikiza kuti James adachitapo kanthu chifukwa cha zovuta zomwe banja lake lakhala likukumana nalo posachedwa. Mwatsoka JAMES watisiya sopano πŸ’”πŸ’”

12/11/2025

Akabaza kusambitsa mzawo chifukwa ma kasitomala amamudandaula fungo.

ZINA UKAMVAMakolo a mwanayu ndi akuno ku Malawi  koma amakhala ku South Africa ndiye akuti munthu wina anampatsa poison ...
12/11/2025

ZINA UKAMVA

Makolo a mwanayu ndi akuno ku Malawi koma amakhala ku South Africa ndiye akuti munthu wina anampatsa poison mwanayu ndiye mwana anayamba kulira ndi m'mimba ndipo tsiku lomwelo anamwalira.

Atamuyeza apeza kuti anadyetsedwa mankhwala... Zikumveka kuti amzawo a mayi ake omwe amawasungira mangawa ndi omwe apanga chipongwecho kuti awakhaulitse

Address

24 Belvedere Place Flat 1, Phibsboro, Dublin 7
Mountjoy

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when VOMI News 247 posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to VOMI News 247:

Share