Angaliba Online

Angaliba Online Media House

Gulu la anthu ochuluka lasonkhana pa bwalo la chonde ku mulanje komwe kuli mwambo wachikhalidwe cha a  lomwe chotchedwa ...
19/10/2025

Gulu la anthu ochuluka lasonkhana pa bwalo la chonde ku mulanje komwe kuli mwambo wachikhalidwe cha a lomwe chotchedwa mulhakho wa Alhomwe , ndipo pali chisangalalo chachikulu pa malowa kudzera mavinidwe osiyanasiya ndi zina zambili.

Wolemba : Ruth kauseni online news

 19/10/2025 mtsogoleri wa dziko lino professor  Authur peter munthalika wati kuyambila pa 1 january chaka cha mawa, suku...
19/10/2025


19/10/2025


mtsogoleri wa dziko lino professor Authur peter munthalika wati kuyambila pa 1 january chaka cha mawa, sukulu zonse za pulaimale komanso sekondale za Boma zikhala za ulere.

A munthalika anena izi lero kwa chonde mu Boma la mulanje ku mwambo wachikhalidwe wa mulakho wa Alhomwe.

A munthalika anapitilira kupempha amalawi kuti adzikhala okondana komanso olimbika pa ntchito posatengera kusiyana maganizo pa ndale kamba koti chitukuko cha dziko lino chalunjika pa umodzi.

(wolemba Laureen Jalasi_Mulanje Chonde)

19/10/2025

President Prof. Mutharika attends Mulhako wa Lhomwe (19 October 2025)

 18/10/2025Mtsogoleri wa dziko lino Professor Arthur Peter Mutharika, Mawa akakhala nawo pa mwambo wa chikhalidwe wa mla...
18/10/2025


18/10/2025

Mtsogoleri wa dziko lino Professor Arthur Peter Mutharika, Mawa akakhala nawo pa mwambo wa chikhalidwe wa mlakho wa Alhomwe kwa Chonde M'boma la Mulanje.

Izi ndi malinga ndi kalata yomwe ofesi ya mtsogoleri wa dziko lino ndi nduna watulutsa ndipo yasainidwa ndi mlembi wankulu ku ofesiyi a Justin Saidi.

(Wolemba: Laureen Jalasi_Blantyre)

18/10/2025

Umu ndi momwe Magule osiyanasiyana akuvinidwa pa bwalo la chonde Ku mulanje kuonetsa kukonzekera kwawo pa mwambo wa a mluhakho wa Alhomwe omwe uchitike mawa pa 19 October 2025.

Wolemba : Ruth kauseni

Umu ndi momwe zilili kwa Chonde m'boma la Mulanje, komwe gulu la anthu likusonkhana pa chikondwerero cha Mulhakho wa Alh...
18/10/2025

Umu ndi momwe zilili kwa Chonde m'boma la Mulanje, komwe gulu la anthu likusonkhana pa chikondwerero cha Mulhakho wa Alhomwe. Anthu akusangalala, kuvina ndi kuyimba nyimbo zachikhalidwe komanso zakudya zachikhalidwe cha alhomwe.

Chikondwererochi chinayamba Lachitatu, ndipo chikuyembekezeka kumalizidwa mawa ndi mtsogoleri wa dziko lino Professor Arthur Peter Mutharika, yemwe akhale m’derali kumalizitsa Mwambowu.

Wolemba: Janet Nkhoma

Lero pa 18 October 2025   Ku mulanje  pa bwalo la  chonde komwe kumachitikira mwambo  wa mhlakho wa mlhomwe wa  kuli gul...
18/10/2025

Lero pa 18 October 2025 Ku mulanje pa bwalo la chonde komwe kumachitikira mwambo wa mhlakho wa mlhomwe wa kuli gulu la anthu ochuluka omwe akukonzekera mwambowu omwe uchitike mawa pa 19 October .

Pamwambowu pakhala magule opitilira 500 amdziko muno komanso 100 akunja kwa dziko lino.ndipo cholinga cha mwambowu ndikuonesa chikhalidwe chawo kudzera mu njira zosiyanasiyana monga malonda ogulitsa zovala zachikhalidwe ,makhwala osiyanasiya monga a chiswabu ,esinat ndi ena ochuluka komanso kuonetsa magule osiyanasiyana.

Ndipo mlendo wamkulu woitanidwa pa mwambowu ndi Mtsogoleri wa dziko lino professor Arthur peter Muthalika .

Wolemba :Ruth kauseni

  Victoria Kingstone ndi anthu ena awiri amene akuimbidwa mlandu ofuna kuchita chipongwe a Roza Fatch Mbilizi atulutsidw...
17/10/2025



Victoria Kingstone ndi anthu ena awiri amene akuimbidwa mlandu ofuna kuchita chipongwe a Roza Fatch Mbilizi atulutsidwa pa belo.

Izi ndi malingana ndi bwalo la milandu la Senior Resident Magistrate m'boma la Mangochi.

Anthu ena amene akuyankha mlanduwu ndi a Sanudi Sande ndi Asiyatu Amani.

Iwo awuzidwa kupereka 500,000 thousand aliyense ngati chikore ndipo akuyembekezeka kuti azikaonekera ku polisi ya Mangochi kawiri pa mwezi ulionse.

Oimila a Kingston pa mlandu a Peter Msungama wati wakhutila kuti bwalori lapeleka belo.

Kingston adzalowanso bwaloli pa 4 November 2025 pomwe mulandu udzakhale ukupitilila.

Kingstone adagonja pa zisankho za phungu m'dela la Mangochi Central ndipo a Roza Mbilizi Fatch ndamene adapambana.

Olemba: Blessings Kaimira.

(Mangochi).

17/10/25.

  Mtsogoleri wa dziko lino Pro Arthur Peter Munthalika wasankha  a George Jaffu kukhala General watsopano wa Malawi Defe...
17/10/2025



Mtsogoleri wa dziko lino Pro Arthur Peter Munthalika wasankha a George Jaffu kukhala General watsopano wa Malawi Defence Force.

Mwambo oika nyota a Jaffu unachitika ku page house m'boma la Mangochi.

Polankhula kwa atolankhani utatha Mwambowu a Jaffu anatsindika za ubwino otukula chitetezo cha dziko posamala miyoyo ya asilikali.

Olemba :Blessings Kaimira.

(Mangochi)

17/10/25.

Apostle Clifford Kawinga of Salvation for All Ministries International has stated that the tour to launch the Hope Field...
17/10/2025

Apostle Clifford Kawinga of Salvation for All Ministries International has stated that the tour to launch the Hope Fields initiative is progressing well.

Speaking on Friday in Thyolo district, under Traditional Authority Mkwethemule, Apostle Kawinga revealed that he has so far reached three districts with the initiative.

He expressed dismay that despite the country's abundant water and land resources, many people rely solely on rain-fed farming.

Apostle Kawinga hoped that with the provision of water pumps, farmers would be able to engage in agricultural activities throughout the year.

Senior Chief Mkwethemule expressed optimism that the solar pumps would lead to bumper harvests and urged farmers to take good care of the donation.

Davison Mandime, representing two clubs, thanked Apostle Kawinga for introducing the initiative in their district, stating that they were happy with the development.

The clubs have received substantial support, including 50 bags of fertilizer, 15 hoes and 10 packets of Maize seeds per club.

The Hope Fields initiative aims to promote food security and sustainable livelihoods in key communities in Machinga, Chiradzulu, and Thyolo districts.

Madalitso Pendame

  Mtsogoleri wa dziko lino Professor Arthur Peter Mutharika kudzera mu mphanvu zomwe alizazo wasakha Roza Fatch Mbilizi ...
17/10/2025



Mtsogoleri wa dziko lino Professor Arthur Peter Mutharika kudzera mu mphanvu zomwe alizazo wasakha Roza Fatch Mbilizi kukhala nduna ya za ulimi ndi chitukuko cha madzi komanso a George Partridge kukhala nduna ya makampani, malonda ndi zokopa alendo.

Izi ndi malinga ndi kalata yomwe Angaliba yaona yosayinidwa ndi mlembi wamkulu mu ofesi ya mtsogoleri wa dziko ndi nduna Dr Justin Adack Saidi atulutsa.

Izi zikutanthauza kuti padakali pano nduna zomwe zasankhidwa zakwana zisanu.

A Munthalika adasankhanso a Joseph Mwanamveka kukhala nduna ya zachuma ndi chitukuko komanso Alfred Gangata kukhala nduna yoona za m'dziko ndipo awiriwa adalumbilitsidwa kale.

Rose Fatch Mbilizi ndi phungu wa nyumba ya malamulo m'dela la Mangochi Central ndipo adapambana atapikisana kwambiri ndi a Victoria Kingstone omwe Padakali pano ali m'manja mwa apolisi. Kingston akuimbidwa mlandu oganizila kupha a Roza Fatch Mbilizi.

Wolemba: Blessings Kaimira.

17/10/25

Farmers across the country are benefiting from the Hope Fields Initiative, launched by Apostle Clifford Kawinga, founder...
16/10/2025

Farmers across the country are benefiting from the Hope Fields Initiative, launched by Apostle Clifford Kawinga, founder of Salvation for All Ministries International.

The initiative targets local farmers, aiming to support their agricultural endeavors.

In an interview with Angaliba News, Apostle Kawinga explained that the initiative is a way to put the Word of God into action. "Jesus Christ teaches us to share what we have, which is why we engage in charity work," he emphasized.

Aisha Mwachande, chairlady of the Mkalo Scheme, expressed gratitude for the initiative, promising that her group would work diligently and utilize the farming tools provided effectively.

In Chiradzulu district, four clubs - Kaanani Farmers Club from Traditional Authority (T/A) Nkalo, Shalomu Farmers Club from T/A Mpunga, Ziyoni Farmers Club from T/A Maoni, and Eden Farmers Club from Senior Group Village Headman Namande - are set to benefit from this initiative. Each club comprises 300 farmers.

The clubs have received substantial support, including 50 bags of fertilizer, 15 hoes, and 10 packets of maize seeds per club.

Additionally, they received 2,000 bags of maize, 1,000 loaves of bread, and 2,000 drinks.

This initiative further expands the reach of Hope Fields, supporting local farmers in their quest for sustainable agricultural practices.

madalitso pendame

Address

Ginnery Corner, Opposite NBS Bank
Blantyre
265

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Angaliba Online posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Angaliba Online:

Share

Category