Angaliba Online

Angaliba Online Media House

 Zatsimikizika tsopano kuti timu ya Manchester United isewelanawo mu mpikisano  wa UEFA Champions League itagonjesa timu...
04/05/2026



Zatsimikizika tsopano kuti timu ya Manchester United isewelanawo mu mpikisano wa UEFA Champions League itagonjesa timu ya Liverpool masana a lamulungu pa 3 May 2026 pa bwalo la Old Trafford Ku Mangalande.

Izi zadza pamene timuyi yakhala zaka zochuluka chiseweleleni mu mpikisanowu potsatila kusachita bwino.

Pakadali pano timuyi ili pa nambala yachitatu ndi mapoints okwana 64, kutsatira kugonjesa Liverpool yi ndizigoli zitatu kwa ziwiri m'masewera omwe anali opatsa chidwi.

Masewerowa asanachitike mphuzitsi wakale watimuyi Sir Alex Ferguson anagwa koma atawapima ku kuchipatala madotolo atsimikiza kuti akupeza bwino.

Date: 03/05/2026
Wolemba: Promise Peter

  03/05/2026The founder of Salvation for All Ministries International, Apostle Clifford Kawinga, urged traditional leade...
03/05/2026

03/05/2026

The founder of Salvation for All Ministries International, Apostle Clifford Kawinga, urged traditional leaders to love one another in their communities and trust in God, not charms, at a gathering organized by the ministry at Namiwawa Secondary School in Blantyre.

Apostle Kawinga emphasized church-traditional leader partnerships for community development and spiritual growth.

Blantyre Mayor Jomo Osman thanked Kawinga, calling it a first in Malawi's history, and promised culture preservation and bias-free development with chiefs.

Senior Chief Kumtaja also thanked Kawinga and pledged to work with churches, avoiding favoritism.

The event brought together over 420 leaders to promote unity and collaboration.

Salvation for All Ministries International has reached 10 million people with God’s word since 2006 through various initiatives like Hope Field Initiative, food distribution, Water and sanitation programs just to mention a few

(Reporter: Madalitso Pendame)

03/05/2026

2026 MARIATHON LUNCH -RADIO Radio Maria Malawi, MANGOCH MAIN STUDIO

  Mpingo wa Zambezi Evangelical Church pansi pa Mitsidi Synod walangiza makolo kuti azimasukirana ndi ana awo achitsikan...
03/05/2026



Mpingo wa Zambezi Evangelical Church pansi pa Mitsidi Synod walangiza makolo kuti azimasukirana ndi ana awo achitsikana pamavuto omwe akukumana nawo.

Dr Joyce Makokola omwe ndi m'modzi mwa akuluakulu oyang'anira zaumoyo m'boma la Ntcheu anena izi pamene anali mulendo olemekezeka pamwambo otsekera msonkhano wa atsikana achichepele ampingowu pa school ya pulaimale ya New Era.

A Makokola ati pazikhala kumasukirana pakati pa ana achitsika komanso makolo ngati njira imodzi yothetsa mchitidwe ozimangilila omwe wachuluka m'bomali.

Mulembi wankulu mumpingo wa Zambezi Evangelical Church Mitsidi Synod, Rev Robert Yandula ati mpingo wawo ukutenga mbali kupeleka uphungu wabwino kwa achinyamata kuti azitha kupanga ziganizo mwaiwo okha. Iwo alonjeza kuti mpingo wawo waika ndondomeko yolipilila atsikana kusukulu zaukachenjede omwe ali ndivuto lazachuma ngati njira imodzi yolimbikitsa maphunziro mu mpingowu.

Mkulu woyang'anira atsikana mumpingowu,a Makhalidwe Huwani anati unali msonkhano wopambana omwe atsikana opitilila chikwi (1000)anatenga mbali kuyambila lachisanu pa 1 May 2026 mpaka lelo pa 3 May. Nsonkhanowu ati upeleka magolomera ku gululi kuti maphunzirowa sanapite pachabe.

Wolemba: Francis Gunda
(Ntcheu)

03/05/26

  The Zambezi Evangelical Church National Girls’ Brigade Conference is wrapping up today in Ntcheu District under the th...
03/05/2026



The Zambezi Evangelical Church National Girls’ Brigade Conference is wrapping up today in Ntcheu District under the theme“Stepping Into Purpose.”

The three-day conference, which opened Friday, May 1, has drawn more than 1,500 girls under 18 from ZEC congregations across Malawi. Over 500 officers are also attending to mentor the participants.

National Chairperson for Girls Brigade in ZEC, Lieutenant Dorothy Gumbo, is leading the event. Lieutenant Reverend Jiya will deliver the closing sermon.

Guest of honor Doctor Joyce Makokola headlines the list of invited officials. Others include Ntcheu District Council Chairperson Jumbe Mambo, the District Commissioner, and Senior Chief Kwataine.

The conference kicked off with a march from Zambezi Evangelical Church to the New Bus Depot before returning to New Era Primary School campus, the main venue for activities.

Reported by Francis Gunda
(Ntcheu)

 Happy world press freedom Day
03/05/2026


Happy world press freedom Day

 Anthu am'mudzi wa Ngalande anagwidwa tsemwe pamene  munthu ndi msuweni wake onse amaikidwa m'manda lelo kwa mfumu yaiku...
03/05/2026


Anthu am'mudzi wa Ngalande anagwidwa tsemwe pamene munthu ndi msuweni wake onse amaikidwa m'manda lelo kwa mfumu yaikulu Njolomole m'boma la Ntcheu.

Malingana ndi yemwe anaimira akubanja a Clement Wingolo ati malemuwa ndi a Dayton Sinkileya omwe amwalila pachipatala chachikulu cha Ntcheu pamene anali ndi vuto lakuonongeka kwa chiwindi komanso a Lunes Mazuwa omwe amwalilila kunyumba ndi nthenda yosanza basi.

A Wingolo ati pasanathe phindi zokwanira khumi ndi zisanu(15 minutes) analandila uthenga wa maliro awiriwa motsogozana la chisanu pa 1 May 2026.Iwo izi zazizimutsa kubanja kwawo ndipo sakumvetsa za imfayi.

M'mawu ake m'busa wa mpingo wa Seventh Day Adventist mchigawo cha Mphate, a Friddy Pachanya ati imfa yotele ikhale phunziro kwa aliyese kuti tisiye machimo omwe angatilepheletse kudzapulumuka patsiku lachiweluzo.

A Lunes Mazuwa amwalila alindizaka 69 komanso Dayton Sinkileya amwalila ali ndi zaka 67 zakubadwa.

Wolemba : Francis Gunda
(Ntcheu)

   Press Freedom Day  ournalists in Malawi have been challenged to move beyond traditional reporting and embrace solutio...
03/05/2026


Press Freedom Day

ournalists in Malawi have been challenged to move beyond traditional reporting and embrace solution driven journalism as a tool for national development.

Speaking during a World Press Freedom Day panel discussion in Salima, MISA Malawi Chairperson Golden Matonga said the media has a critical role in highlighting the everyday struggles faced by ordinary citizens, many of whom still lack access to basic services.

Matonga noted that while these challenges persist, the voices of affected communities are often not adequately amplified. He urged journalists to use their platforms to bring such issues to the forefront and push for meaningful change.

He further emphasized the need for media practitioners to focus on reporting that not only exposes problems but also promotes practical solutions that can improve people’s lives.

The panel discussion, supported by the Malawi Energy Regulatory Authority (MERA), is also providing journalists with insights into the institution’s operations, including fuel regulation and broader issues within the energy sector.

By : Pemphero Suya

  JOMO WAPEPESA.Kutsatila mkukumwe wa anthu utaikapo mlomo pa zomwe mfumu ya nzinda wa Blantyre Isaac Jomo Osman anachit...
02/05/2026



JOMO WAPEPESA.

Kutsatila mkukumwe wa anthu utaikapo mlomo pa zomwe mfumu ya nzinda wa Blantyre Isaac Jomo Osman anachita pomenya anthu makofi, mfumuyi yabwela poyera tsopano ndi Kupepesa.

Ngakhale kuti mfumuyi kum'mawa inatulutsa kanema oti sangapepese, pano atulutsa kalata yopepesa pa Khalidwe lomwe anaonetsa.

Malingana ndi mfumuyi, iwo ndi okonzeka kupitilila kukhalilana bwino ndi anthu a mdela lao.

02/05/26

  02/05/2026Nduna yoona zofalitsa nkhani a Shadrick Namalomba ati boma ndi lozipereka pogwila ntchito limodzi ndi nyumba...
02/05/2026

02/05/2026

Nduna yoona zofalitsa nkhani a Shadrick Namalomba ati boma ndi lozipereka pogwila ntchito limodzi ndi nyumba zofalitsa mauthenga zing'ono-zing'ono za dziko muno.

A Namalomba ayankhula izi pomwe anali mlendo olemekezeka pa mwambo okhazikitsa Mariathon ku Radio Maria Malawi.

Iwo akwanisa kuthandiza nawo
Ndipo apempha anthu ena andale kuti azitenga nawo gawo pa ntchito yothandidza ku zipembezo komanso kukondana wina ndi nzake.

Poyankhula kumbali yawo Mkulu oyendesa Radio Maria Malawi father Joseph Kimu ati cholinga chokhazikitsa ndondomekoyi mkufuna kupeza ndalama zokwana 60 Million Kwacha zomwe zithandizile kuyendetsa wailesiyi.

Father Kimu ati iwo ali ndi masomphenya ofuna kuthana ndi ngongole zomwe pakadali pano ali nazo komanso kuti azitha kulipila omwe amawathandizila kugwila ntchito.

Father Kimu apempha boma kuti liwathandize kumbali ya chuma Kaamba koti wailesi yawo sipanga malonda pokhapokha akhale kuti malondawo ndi okhuzana ndi matenda kapena chisankho.

Mwambowu watsegulilidwa lero ndipo ukuyembekezeleka kuzatsekedwa pa 2 August chaka chino.

Ndalama yomwe yatoleledwa pa mwambowu ndi yopitilila 20 Million Kwacha .

(Olemba- Madalitso Pendame-Mangochi)

02/05/2026



Bankrupt Spirit Airlines is preparing to shut down operations around 0700 GMT Saturday after rescue talks collapsed, sources say, as soaring jet fuel costs linked to the US-Israel war on Iran derail its recovery, Reuters reports.

02/05/2026


Malawi's Yao Paramount Chief Sultan Kawinga urges electorates in Machinga Mikoko Constituency to campaign peacefully and gracefully accept defeat when the byelections are held in June

Address

Ginnery Corner, Opposite NBS Bank
Blantyre

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Angaliba Online posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Angaliba Online:

Share

Category