Mpebros TV

Mpebros TV Mpebros TV is Independent media TV which its aim is to proclaim the gospel of our Lord Jesus Christ

12/10/2025

BUNDA CHITHANGATO KUIMBA
NYIMBO YA MUTU WAMSONKHANO PA GAWO LA ULALIKI

12/10/2025

UKU KUNALI KUIMBA BUNDA FUTURE BAPTIST MEN CHOIR
TITLE YA NYIMBO-FUNSA

12/10/2025

NTHAWI YA CHOPEREKA CHA DLC KOMANSO KUKWANGULA GAWO LA CHIWIRI LA SABATA SUKULU

12/10/2025

Gawo La chiwiri la sabata sukulu la pa 11 OCTOBER 2025 Bunda SDB

12/10/2025

SABATA SCHOOL YA DZULO PA 11 OCTOBER 2025 KU MSONKHANO WAMISASA FROM BUNDA SDB

11/10/2025

CHITHANGATO WOMEN'S CHOIR SINGING AT MAKAPWA SDB CHURCH DURING 2025 ANNUAL GENERAL CONFERENCE

MA PHOTOS APA 11 OCTOBER 2025 FROM BUNDA SDB SHOWING MOMWE MSONKHANO WAMISASA UKUYENDERA
11/10/2025

MA PHOTOS APA 11 OCTOBER 2025 FROM BUNDA SDB
SHOWING MOMWE MSONKHANO WAMISASA UKUYENDERA

Chikalata chomwe chalembedwa ndi omwe akonza dongosolo lothandiza abusa a Seventh Day Baptist Malawi yonse mu chuma kudz...
09/10/2025

Chikalata chomwe chalembedwa ndi omwe akonza dongosolo lothandiza abusa a Seventh Day Baptist Malawi yonse mu chuma kudzera m'mayimbidwe.
Chikalatachi chalembedwa ndicholinga chofuna kudziwitsa akhristu a mpingowu kuti aziwe zofunikira pokonzekera za chochitikachi.

Mpingo wa Seventh Day Baptist uli ndimwambo wa maimbidwe pa 2 November, 2025 ndipo uzachitikira pa Naperi SDB church mu ...
02/10/2025

Mpingo wa Seventh Day Baptist uli ndimwambo wa maimbidwe pa 2 November, 2025 ndipo uzachitikira pa Naperi SDB church mu mnzinda wa Blantyre, ndipo uzayamba 1 koloko masana. Mwambowu ukutchedwa "Tiwagwire Dzanja Music Concert". Ndipo cholinga cha mwambowu ndichofuna kuthandiza Abusa a mpingowu muno m'malawi ndi ndalama yomwe izapezeke pa mwambo umenewu, pa ndalama zomwe zizatoleredwe pa tsikuli ngati fundraising.
Pocheza ndi mmozi yemwe akuyendesa Mwambowu yemwenso ndi mmozi wa oyimba yemwe azapezeke pa tsikuli Fredrick Sulani anati pamene anthu akukonzekera kuzapezeka pa mwambowu akuyenera kuzabweretsa ndalama yokwana K5,000 ngati chopereka pa tsikulo ndipo Kwa omwe sadzakwanitsa kufika akupemphedwanso kuti atha kudzangotumiza chopereka chawo. Ndipo anayankhulapo kuti Magulu oyimba osiyanasiyana a achinyamata, amayi komanso abambo akupemphedwa kudzatenga nawo mbali.
Kumapeto kwake anapereka uthenga wonena kuti kwa amene angafune kudziwa zambiri atha kuyimba pa manambala omwe ali pa poster yo ndi kuyankhula ndi Fredrick Sulani kapena Associate Pastor Blessings Mpezeni Kapenanso a Malumbo Mkandawire pa 0999230175.

Mpebros TV ikhala ikukonzekera kuti ikapezekanso Ku mwambowu pa tsiku limeneli

27/09/2025

27 SEPTEMBER 2025
THESE GUYS HAVE A TALENT,I DIDN'T EXPECT KUTI ANGAIMBE CHONCHI🙌

25/09/2025

Anyamatawa koma anaimba moikapo mtima, Alandile ulemu wawo.
Kumva kukoma nyimboyi ngati ndili kale pa khomo la kumwamba
Alleleyaaaaaaa!!!!!!!

23/09/2025

MA HIGHLIGHTS A KU KASINJE MUSIC SABBATH 😁🙌
A VIDEO CLIP OF A SONG TITLED:PEACE BE STILL

Address

Mbayani
Blantyre
981762775

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Mpebros TV posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Mpebros TV:

Share

Category