28/05/2026
Monga mwachikonzero pakusala masiku awiri okha kuti Makapwa Medicals ichitise mwambo wawo wokhazikisa chimbale chotchedwa "KODI LALEMBEDWA"?
Cha nyimbo zomvera komaso zoonera.
Pa 31 May 2026 tiyeni tikapezeke ku Naperi Seventh Day Baptist church munzinda wa Blantyre.
Tithandizire kukweza maimbidwe mumpingo wanthu wa Seventh Day Baptist pogula chimbalechi.
Mtengo pakhomo ndi ulere..
...... inuyo mukangogula chimbalechi basi.
Tiyeni tonse tikapezeke kumeneko
Kodi inuu zabwino zipose apa!?