24/11/2025
Bwalo lalikulu loweruza milandu mawa pa 25 November 2025 likuyembekezeka kumva ngati kuli nkoyenera kupereka chiletso choletsa mzikiti wa Kachanga ku chileka m'boma la Blantyre kupanga adhan.
Sukulu ya Kalibu academy ndi yomwe inapempha chiletsocho ponena k*ti kuyitanira anthu ku mapempheroko kukumadzetsa mphokoso lomwe likumasokoneza ntchito ya maphunziro pa sukulupo.
Oweruza milandu Justice Tembo ndi yemwe amvelere mlanduwu.