Daily Bible Verses With Prophet Oswald Chizala

Daily Bible Verses With Prophet Oswald Chizala THIS PAGE IS SPECIFICALLY FOR GOD'S KINGDOM ADVANCEMENT THROUGH BIBLE TEACHINGS
(1)

20/09/2025

Pray with me πŸ•―οΈ
Almighty Father,
Remove from me spirit of fear and anxiety,
Give me the spirit of faith and boldness.
Break every power of all negative words spoken against my soul
-Ps. 109:20 πŸ›
And Meet me at the points of my needs by Your riches in Jesus Name. πŸ™πŸΏπŸ›πŸ”₯πŸ”₯

Hallelujah πŸ™πŸ™

FM on πŸŽ™οΈπŸŽ€πŸ™

ZIZINDIKILO 9 ZIMENE MUDZADZIWE KUTI ASATANIC KAPENA AFITI ANAKUGWILANI PA MOYO WANU NDIPO AKUUSEWELESA 1,kumakhalila mo...
20/09/2025

ZIZINDIKILO 9 ZIMENE MUDZADZIWE KUTI ASATANIC KAPENA AFITI ANAKUGWILANI PA MOYO WANU

NDIPO AKUUSEWELESA

1,kumakhalila moyo okhumudwa ,kukwiya kwiya
=muthu opephela okondedwa sumayenela kumakhalila kumakhumudwa ndi zozizila zomwe ayi

2,kusapita chitsogolo mu zithu zanu
=dziwani kuti afiti ndi ASATANIC ndi maukulu oyipa amene sasangalala muthu akamapita chitsogolo koma kubwelela mmbuyo ,moti ngati zithu zanu sizikusitha
=kaya banja lanu kaya business yanu kaya tchito chigwilileni koma popanda chochita ayi alipo adakupondelezani

3,kumakhalila kulota joka,,nyau,,kugonedwa,,kulephela kuwoloka mtsinje kulephela kukwela phili,,kumadyesedwa kutulo kulota mzungu,,kulota mkango,kulota milamba ndi zina zotelo dziwani kuti alipo ASATANIC kapena afiti anagwila moyo wanu

4,makhalila kukumana ndi matsoka pa moyo wanu mwina gogole pa moyo ,Anthu kuwabweleka ndalaama koma osakupasa, zimakhala kuti satana akugwila moyo wako

5,kumakhalila kudedwa pa zifukwa zoti zosakwanila komaso kusakondeledwa pa malo

6,kufooka mu umoyo wa pephelo pa moyo wako ,kumakhalila pa phoni 6 to 6 pa phoni njala yose yamau AMULUNGU osamawafuna ayi

7,kumakhalila muthu KUBUNYULA akazi ndi amuna ena mwa Anthu mumakonda kunena kuti ine nde banja ayi ,mudziwa kuti mukufuna kuti muzikhalila kumabunyula

8,akazi wako kapena mwamuna wako sumakhala naye ndi chilakolako koma mkazi wakunja kapena mwamuna wakunja ,ichi ndi chizindikilo kuti pa iweyo ziwanda zasatana zikujoyapo pa moyo wako

9,kusakhala ndi moyo osavomekeza nyengo zimene ukudusamo komaso kusafuna kuphuzitsidwa liuma kapena thota ,,ana asatana safuna kutsutsidwa koma kaka pa zithu zoti alibe nazo umboni

KUTI MUTULUKEMO PANGANI IZI

1acolit 3v16 akuti kodi simudziwa kuti muli kachisi wa MULUNGU ndipo mzimu woyela agonela mwa inuyo??

aheber 12v29 MULUNGU ndiye moto onyekesa

dziwani kuti pamene pamaphikidwa nyama ,,kuti nyama inja muyike pa moto or galuyo atakhala wamisala koma chapamoto sachikhudza

Ziwani kuti ngati mungakhazikike pamaso pa Mulungu M'choonadi Mulungu adzaika moto pa inu ndipo satana sadzakufikirani

Aheberi 12:29

Satana amapita pomwe palibe moto wa Mulungu

AMBUYE AKUDALITSENI NONSE πŸ™

AMEN

20/09/2025
20/09/2025

MUMASULIDWE MANJA MWA SATANA.

MASALIMO 125:2

Monga mapiri azinga Yerusalemu, momwemo Yehova azinga anthu ake, kuyambira tsopano kufikira nthawi zonse.

Okondedwa mumadziwa kuti sit onse amene muzintchitomu or pa ma business timadalira pephelo? mudziwe kuti ambiri amadalira nyanga , ndipo akaona kuti inu zikukuyenderani sakondwa koma kulingalira zokuphani kuti akhalepo ndi iwo .

Lingankhale banja alipo wina alikwa asing'anga kuti akulandeni mwinanso ena munalandidwa kale , ndipo pano akupanga zoti akupheni chifukwa akuopa kuti antha kubwelelanso manja mwanu.

Lelo ndikupephera kuti kumwamwa kutumize chitetezo chochuluka kuti nyanga zawo zisagwile ntchito.

Amene munapangidwa kale chipongwe, kulandidwa Okondedwa, kukulodzani ku ntchito or pa business yanu lelo ndikulamula angelo amulungu kuti afike pa moyo wanu ndikusulutsa za mankhwala zilizonse .

Musanze, ena muzibibe , ena zituluke munthukuta ndi ena mumisonzi mdzina la Yesu khiristu Nazareth mwamasulidwaπŸ™πŸ™πŸŽ™οΈ

19/09/2025

MALOTO AWONETSERA KUTI MPHAMVU ZA UFITI ZIKULIMBANA NAWE

Ufiti ndi chipangidzo cha uzimu chomwe chimagwiritsidwa ntchito pofuna kuononga miyoyo ya anthu
(Malingaliro, Zokhumba komaso Machitidwe a zinthu)

1.KULOTA ZOCHITITSA MANTHA KAPENA KUMAKHALA NDI MANTHA USIKU.

Tamvetserani loto lirilonse lomwe limakupatsani ndikubweretsa mantha pamoyo wanu silabwino ndilochokera ku mphamvu za ufiti.
2 Timoteo1:7
Mulungu sanatipatse Mzimu wa mantha;koma waMphamvu,wachikondi komaso kudziretsa.

Mantha amachokera kwa satana osati kwa Mulungu.
Tiripo wena timaopa even kugona tokha mnyumba usiku nkhani mantha.
Munthu wotere akusowekera Mamasulidwe amphamvu kwambiri.

2.KULOTA UKUMIRA M'MADZI

Abale ndi alongo musiyanitse kumira m'madzi ndi kuwoloka apa tikukamba za kumira m'madzi
(tsinje,nyanja,dam, swimming pool etc)

Zimatanthaudza kuti alipo amene amakutambira kuti tsogolo lako lisapite patali(Stagnation)

Nthawi zambiri anthu olota maloto otere zinthu zawo sizimapita patali;
kupedza ntchito posakhalitsa yatha, kuyamba business posakhalitsa yaduka,kupedza banja from nowhere latha.

Ngati mumalota maloto otere mukusowekera kukumana ndi Mtumiki wosata zamaloto akuthandidzeni Mamasulidwe.

3.KULOTA UKUDZUDZIKA M'MALOTO
KAPENA KULOTA UTAKODWA

Kulota utasowa mtendere,usakupedza zabwino m'maloto,utachedwa ku sukulu kapena kudzochitika za kumalotoko.

Zimatanthaudza kuti mavuto omwe ukukumana nawo m'moyowu alipo wina wake amane amapangitsa kudzera mu ufiti.

Ndipo Munthu wotere zinthu zake zimakhala zochedwetsedwa;
Azako onse anapedza banja iwe ayi ndithu,

Azako ambiri anamanga manyumba iwe olo Chitseko ulibe.

Mzimu wa kuchedwetsedwa,kudzudzika komaso kusapita patali.

Ukusowekera Mamasulidwe amphamvu kwambiri.

4.KULOTA NJOKA

kulota ukuthamangitsidwa ndi njoka,
njoka itakuloma,njoka italowa mnyumba.

Zimaimilira kuberedwa ndi kulandidwa ulemelero ndi tsogolo lako kudzera mu ufiti
Genesis 3:23-24

Munthu wotere amayenda kwambiri m'moyo wangongole komaso kusagwira bwino ntchito kwa ndalama zomwe amapedza pamoyo wake.

Mamasulidwe akufunikira pa iwe.

5.KUWOMBEREDWA KAPENA KUBAIDWA M'MALOTO N'KUTULUTSA MAGAZI

Zimatanthaudza kuti wina wake wakulodza ndi nyanga pofuna kukupha kapena pofuna kupha china chake m'moyo mwako.

Tisaiwale kuti moyo wa Munthu ndi Nyama uli mu mwazi.
Genesis 9:5

Munthu wotere amakonda kumva kufooka pena kumadzimva kulemedwa komaso umamva fungo lonyasa ukakhala.

Ukusowekera Mamasulidwe, machiritso komaso chitetedzo.

6.KULOTA NJUCHI ITAKULUMA KAPENA ZIKUKUTHAMANGITSA

Abale ndi alongo tisiyanitse ndikulota uchi kapena njuchi ziri ndi malesa.
Apa tikukamba njuchi zikukuluma kapena zikukuthamangitsa.

Zimatanthaudza kuti akumidima kudzera mu ufiti akusata moyo wako ngati njuchizo zikukuthamangitsa koma ngati njuchi yakuluma zimatanthaudza kuti akuyika ziwanda zoti zizikupanikitsa pa moyo wako.

Munthu wotere matenda sachoka pamoyo wake komaso sakhala ndi thanzi losangalatsa.

Ukumane ndi Mtumiki akuthandidze mumapemphero a Mamasulidwe.

7.KULOTA MAKOSWE

Kulota makoswe akudya zovala zako, akukuthamangitsa, atakusautsa mnyumba mwako ndi zina zotero.

Zimatanthaudza kuti akumidima kudzera mu ufiti alodza ndikuba chisomo chako cha zachuma.

Iweyo za Chuma zako sizilongosoka kufikira utamasulidwa.

NOTE:Vuto lirilonse lomwe linayambira kumaloto kupemphera opanda kuphwasula malotowo siziyendapo.

Nchifukwa chake ndimalimbikitsa kukumana ndi Mtumiki amene amasata za maloto ngati vutolo lidayamba mutalota maloto ena ake.

kaya malotowo simuwakumbukira koma pedzani Mtumiki amene zamalotozi amadzisata.

NDATI MUKUFUNA THANDIDZO LAPADERA KOMASO KUMASULIRA MALOTO

TILANKHULENI PA πŸ‘‡

WhatsApp or call
(+265) 992 275 595

CHIDZIWITSO

Pepani kamba kochurukidwa sindimakwanitsa kuyankha funso lanu pa comment box or message ya ku inbox kwa page yathuyi ofuna thandidzo muimbe kapena mundilembere ku WhatsApp

AMBUYE AKUDALITSENI NONSE

ZIKOMO KWAMBIRI

AMEN πŸ™

19/09/2025

Mulungu akuchitirani zomwe maso anu sanaonepo,makutu sanamvepo ingakhale mmitima ya anthu sizinavumbulitsidwepo mdzina la Yesu
πŸ”₯

18/09/2025

Osataya mtima, palibe yemwe anadutsa munyengo zowawa nkufera momwemo.
-Palibe anadutsa munyengo osatulukamo
-Palibe anadutsa munyengo zowawa moyo wake onse.


-Ngakhale Yobu anatuluka mudzowawa( matenda ndi umphawi komanso zitonzo)
-Ngakhale Abraham ndi Sarah anatuluka mu zowawa(kusabereka)
-Ngkhale Mose ndi ana aMulungu, anatuluka mu zowawa( ukapolo)
-Ngakhale Esitere ndi ana a Mulungu aja, anatuluka mu zowawa ( ma attack komanso zitonzo)
-Ngakhale Daniel anatulukamo mu dzenje la Mikango
-Ngakhale anyamata aja, anatulukamo mu ng'anjo ya moto


-Nyengozi ndi zakanthawi chabe
-Kunja kumawalanso
________________
MASALIMO 118:13
"Kundikankha anandikankha ndipo ndikanagwa ,koma Yehova anandigwiritsitsa"
___________________

18/09/2025

CHONDE OSABISALA MULUNGU AKUKUFUNANI KUMENE MWABISALAKO.

Ndipo anamva mau A Yehova Mulungu akuyenda yenda munda nthawi ya madzulo ndipo anabisala Adamu ndi kazi wake pamaso pa Yehova Mulungu pakati pa mitengo ya munda Genesis 3:8-10.

Adamu ndi kazi wake anabisala pamene Yehova amayenda yenda munda wa edeni koma mau amamva koma anasakha kubisala.

Lero Yehova akuitana aliyense kukayenda naye tsiku ndi tsiku koma inu mwasakha kubisala kusafuna kumva mau AMulungu.

Mulungu akukuitana kumene mwabisalako
Mwabisala kumiseche,
Mwabisala kuchigololo
Mwabisala UFITI
Mwabisala kupsa mtima
Mwabisala KUBUNYULA
Mwabisala kusakhulupirika kwa mwamuna Wanu ndi kazi wanu .
Mwabisala mu JUNGA
Mwabisala mowa ndi CHAMBA
Mwabisala kunama
Mwabisala mu utabwali
Mwabisala muchinyengo.

Kulikonse kumene wabisala tulukanikoni Mulungu akukuitanani Mulape machimo ndikuyamba moyo watsopano.

Mulungu akufuna aziyakhula nanu tsiku ndi tsiku powerenga mau ake ndikuwasunga.

Lapani Machimo mulandire chisomo cha Ambuye wathu Yesu khristu popeza akubwera posachedwa.

Lolani mphamvu ya Mzimu oyera ikhale nanu

Mtendere wa Ambuye wathu Yesu khristu ukhale name

Hallelujah πŸ™ anthu Amulungu πŸ™πŸ™

FM on πŸŽ™οΈπŸŽ€

18/09/2025

πŸ“– β€œWeeping may endure for a night, but joy comes in the morning.” (Ps. 30:5)

πŸ“– β€œThe Lord will make you the head, not the tail; above only and not beneath.” (Deut. 28:13)

πŸ“– β€œWho knows if perhaps you were made queen for such a time as this?” (Esther 4:14)

πŸ“– β€œGod demonstrates His love for us in this: while we were still sinners, Christ died for us.” (Rom. 5:8)

πŸ“– β€œI praise You, for I am fearfully and wonderfully made.” (Ps. 139:14)

Rise up, your season is here! πŸŒΈβ€οΈβ€πŸ©ΉπŸ”₯🌷❀️🫢🏿

FM on πŸŽ€πŸŽ™οΈ

17/09/2025

Nyengo yi sinafike kudzakuonongani koma kudzaonetsera ukulu wa Mulungu pa moyo wanu.

Lero lino Yehova azionetsere yekha chimene Iye ali pa moyo wanu m'dzina la Yesu Khristu.

FM on πŸŽ€πŸŽ™οΈ

WERENGANIKO IZI✍️✍️✍️Ndizoonadi kuti malingana ndi malamulo a Mpira, yemwe amamakidwa kwambiri ndi amene ali ndi mpira.K...
17/09/2025

WERENGANIKO IZI✍️✍️✍️

Ndizoonadi kuti malingana ndi malamulo a Mpira, yemwe amamakidwa kwambiri ndi amene ali ndi mpira.

Komansotu mudziwe kuti Si yemwe ali ndi mpira yekha yemwe amamakidwa komanso yemwe ali ndi kuthekera koti akhonza kumwetsa zigoli ndikuthandizira kuti ena agoletse.

Chimodzimodzi mu zopempherazi; Satana amalimbana ndi yemwe ali opempheranso kwambiri kapena yemwe ali ndi Chisomo chachikulu
( kaya ndi zachuma, utumiki etc)

Komanso satana amatha kulimbana nanu akaona kuti muli ndi kuthekera koti kutsogoloku, m***a kudzabooleza.

Choncho dziwani izi:
-Satana salimbana ndi Kape
(Munthu yemwe Sali ndi Influence mu uzimu)
-Satana salimbana ndi munthu opanda tsogolo( oti atha kudzabooleza.

NB:
Ngati mukukumana ndi nkhondo zochuluka ndiye kuti sindinu munthu wamba mu dziko la uzimu.
CHOFUNIKIRA
Wonjezerani moto wa pemphero.
(Yemwe akumakidwa amayenera kulimbikabe mpakana atapeza mwati wa chigoli)
____________________________
1 AKOLINTO 16:9
"Khomo lalikulu landitsegukira koma pali zambiri zonditchinga."

AMEN

GOLIATI AFE LEROLIAROMA 8:18Goliati wina aliyense ali ndi Davide wake.Ndikuti vuto lililonse liri ndi mathero ake.Inu pa...
16/09/2025

GOLIATI AFE LEROLI

AROMA 8:18

Goliati wina aliyense ali ndi Davide wake.

Ndikuti vuto lililonse liri ndi mathero ake.

Inu palibe vuto lamuyaya nchifukwa chake chirichonse chiri ndi expire date.

Kusabereka kukakumana ndi Yesu Khristu kumatha.

Kusaona kukakumana ndi Mfumu ya mafumu osaona amaona.

Ngongole ikakumana Messiah umakhulukidwa.

Palibe nthenda yomwe inayamba yaima pamalo pomwe pamapedzeka M'chiritsi wa chiritsi Yesu Khristu.

Umphawi ndi usiwa kungokumana ndi Bwana wa mabwana Yesu Khristu zimagonja zokha.

Mulandu wako ukamupatsa Loya wa ma loya Yesu Khristu ndizija anthu amatulutsidwa ku police cell pamulandu woti azawo akuseva jele 10 years.

Kusowa kwa banja kukakumana ndi Mamuna wa mtanda munthu banja lodala amalipedza mosavutikira.

Vutolo likumane ndi Yesu Khristu wa ku Nazareti

AMEN πŸ™

Ngati mukufuna thandidzo la uzimu kapena pemphero lapadera ndi Kumasulira maloto

Tilankhuleni pa πŸ‘‡
WhatsApp or call
(+265) 992 275 595

Hallelujah πŸ™

Address

Blantyre

Telephone

+265887096964

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Daily Bible Verses With Prophet Oswald Chizala posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Daily Bible Verses With Prophet Oswald Chizala:

Share