16/05/2025
Sad or rather interesting to hear that KEN B WAZAKANENA (what is his real name, anyway) is struggling to register or rather pay school fees at Soche Technical College where he would like to study a technical course.
Fees at Soche Technical College for those selected by Ministry of Labour as day scholars is only k25,000 per term.
And if you are lucky to be selected on General bursary you are covered you only have to pay k5,000 for ID for first term only and k2,000 for all other terms as Students Union Council fee.
The Bursary also covers examination fees which is now k35,000 only for level one.
We aren't judging whether he can afford that or not but we can provide guidance on the bursary to whoever is interested.
Please drop a comment below if you have any questions or call us on 0881232216. Don't send Whatsapp messages or text don't flash.
We can share guidance on that and many issues on TEVET related trainings.
!
Ngati palifunso ATI funse on 0881232216. Calls only
Ken B Wazakena akupempha akufuna kwabwino kuti amupititse ku school. Walemba izi ku inbox 👇
Akometsi, ndakhala ndikuyendera Soche Technical College kuti mwina ndingaphuzileko ntchito za manja poti ma comedy akukanika anthu akungonditukwana. Ndayesetsa kudzithandiza ndekha koma chilichonse ndingachite palibe akundipanga support. Depression ikundiswa.
Ine school inandivuta chifukwa chosowa fees paja ndili ndi Mayi okha. Ndayendera ku Soche kano ka 4 poti ndiza boma ndimayesa ndipeza mwayi koma zikuvuta ndi mkana ndazibweletsa poyera kuti chonde thandizeni ndiphuzire ndikuwona ngati kulakwitsa kwina ndimapangaku ndi umbuli osowa school, koma pa ground ndimayesetsa.
Ndisaname school ndikuyifuna. Ndili ndi zaka 23 koma ku Malawi kuno ndapanga zinthu zoposa nsinkhu wanga even kuthandiza anthu ena kufika pabwino koma ine ndili pompaja. Ndazindikira kuti ikupelewera ndi school ndipo ndikapeza mwayi wa school, ndikhulupilira ndidzachita bwino kwambiri.
Ngati mungathe ikani post kuti ndikufuna kubweleraso ku school koma fees ndiye vuto amene angakonde akangolipila straight ku school yomwe ingapezeke maka maka Soche ineyo ndiziyenda kaya wapansi koma mkalasi ndilowe komanso ndiphunzireko ntchito ya manja.
Choonde ndithandizeni akufuna kwabwino. Give me a chance to go to school and I will do better.
Ken B Wazakena
0991364973