29/05/2020
Ambuye kodi mwandiiwala
Awe anali mau anyamata wina Yemwe anapemphera mosweka mtima kwa Nuking pomudandaulira zavuto lomwe anali nalo iye anapemphera kwa nthawi yaitali km samaona kusitha chilichonse kenako anapempha ndikt Ambuye mwandiiwala pamene anangomaliza kulakhula mau amenewa anaona maso mphenya mphamvu ya Yehova kumenyana ndiyasatana apa ndipamene anazindikira kt Mulungu ali naye ndipo akuyenera kupemphera kwambiri.
Kutheka inuso muliemunyengo yotere mwapemphera mayakho sakubwela ena mwafika pozilakhulira nokha kt zoti kwa Mulungu kuli mayakho ndakaika. Km ayi musatope pakt pamene nzeru zathu zatha ndipamene za Yehova zimayambira iye amaziwa zonse zimene mwamupempha musatope pakt mayakho anu sabwelala momwe mukufunila ngati muzatopa pempherani kt mulandile zolinga zanu Ambuye akudaliseni osaiwala kupanga share