Times 360 Malawi

Times 360 Malawi Times 360 Malawi, the online platform of the award-winning Times Group, Malawi’s only 360 media house
(365)

The Times Group has challenged itself since its humble beginnings in 1895 when it published the inaugural newspapers at Songani in Zomba. This is the only media giant and market leader in newspapers, radio, television, offset printing, courier, publishing, and advertising agency bagging a long list of media awards local and international through investigative and analytic journalism.

26/12/2025

What a Weekend 26 December 2025

26/12/2025

MDYANGU | 26 DECEMBER 2025

26/12/2025

RFP | 26 DECEMBER 2025

  Mwana wamkazi wa zaka zitatu wafa, madzi atamukokolola mu mtsinje wa Nkhadwe mdera la mfumu yayikulu Tengani m'boma la...
26/12/2025



Mwana wamkazi wa zaka zitatu wafa, madzi atamukokolola mu mtsinje wa Nkhadwe mdera la mfumu yayikulu Tengani m'boma la Nsanje, kutsatira mvula yomwe yakhala ikugwa kuyambira dzulo usiku m'bomali.

Potsimikiza za nkhaniyi, mneneli wa khonsolo ya Nsanje a Robert Nayeja ati madzi osefukira akhudza nyumba zokwana 49, ndipo 29 mwa nyumba zomwe zakhudzidwazi zagweratu m'dera la mfumu yayikulu Malemia ndi Tengani, pamene kafukufuku akupitilira kuti apeze m'mene mvulayi yakhudzila madera ena.

A Nayeja ati m'dera la mfumu yayikulu Malemia, madzi osefukira kuchokera mu mitsinje ya Nyamadzere, Ngoni ndi Chimwala akhudza midzi monga Mtemangawa, Ndenguma, Thawalawa, Mbangu, Mwanda ndi Mwasalapa.

"Kwa TA Tengani, nyumba 48 ndizomwe zakhudzidwa ndipo 28 zagweratu. Mtsinje wa Nyamgugu omwe uli kwa TA Mbenje wakhudza midzi monga Tizola, Zilikumunda, Nyang'a, Kalupsya ndi Tambo pamene ma TA ena tikufufudzabe," atero a Nayeja.

Pakadali pano, khonsolo ya Nsanje yapempha anthu omwe akukhala m'madela a chiwopsezo cha madzi osefukira kuti asamukire madela okwela.

Kum'mawaku, anthu amavutika kudutsa pa malo ena otchedwa Mayere mu msewu wa M1, pakati pa Bangula ndi Nsanje pamene madzi osefukira amadutsila pamwamba pa msewuwo.

Wolemba Innocent Kalikokha

  Business mogul and owner of Ngom's Oil in Liwonde, Elias Ngomano, has launched a football and netball tournament aimed...
26/12/2025



Business mogul and owner of Ngom's Oil in Liwonde, Elias Ngomano, has launched a football and netball tournament aimed at raising awareness about security issues in Machinga District.

Speaking at the launch event, which featured matches between Machinga Police and Liwonde Police teams, Ngomano emphasized the critical role security plays in national development. He explained that the tournament is designed to attract community members so they can be sensitized to these important issues.

Ngomano, who also serves as chairperson for Machinga Community Policing, added that the initiative is a way of giving back to his customers and the community during the festive season.

Meanwhile, Traditional Authority Nkula welcomed the awareness campaign, noting that it comes at a crucial time when incidents of crime often increase during the festive period.

In the football match, the Machinga Police team defeated Liwonde Police 5-4 in a penalty shootout.

Reported by Blessings Tambala.

 Bungwe la Musicians Union of Malawi (Mum) lati banja lawoyimba komanso aluso mdziko muno lili ndi chisoni chachikulu ku...
26/12/2025



Bungwe la Musicians Union of Malawi (Mum) lati banja lawoyimba komanso aluso mdziko muno lili ndi chisoni chachikulu kutsatira imfa ya mambembala asanu agulu la The Hive lomwe limaimba ndiwoyimba wodziwika bwino Eli Njuchi.

Mamembala asanuwa womwe amwalira kutsatira ngozi ya galimoto m'boma la Ntcheu lachisanu pomwe amapita kokayimba ku Lilongwe ndi Elivacy Myaba yemwe amayimba mawu, Vincent Mkwinda ( Artist Liason/Tour Manager), Junior Kapengule (Pianist)
Raphael Chitsonga( Drummer) ndi MacFarlen Banda( Lead Guitarist).

Mkulu wa bungweli a Vita Chirwa ati aluso athyoka kamba kakutaya anthu asanuwa womwe anati anali ndi luso lakuya.

Aluso wosiyanasiyana akupereka uthenga wawo wokhumudwa kamba ka imfa ya anthu asanuwa.

Kutsatira imfa ya anthu asanuwa, phwando lomwe Eli Njuchi anakonza la The Hive Experience ku Bingu International Convention Centre mu mzinda wa Lilongwe loweluka layimitsidwa.

Wolemba Jimmy Chazama ndi Sam Banda Jnr

26/12/2025

EVENING NEWS | 26 DECEMBER 2025

  Blessings to You!You and your family are invited to be our special guests. Let's be together as we end the year and st...
26/12/2025


Blessings to You!
You and your family are invited to be our special guests. Let's be together as we end the year and start a brand new one in one night! Come just as you are.
Do not miss this crossover for anything.

  Apolisi m'boma la Dowa amanga abambo awiri kaamba kowaganizira kuti anapha a Gift Kanyoza a zaka 32 omwe amachokera mm...
26/12/2025



Apolisi m'boma la Dowa amanga abambo awiri kaamba kowaganizira kuti anapha a Gift Kanyoza a zaka 32 omwe amachokera mmudzi mwa Misi m'dera la mfumu yayikulu Msakambewa ya m'bomali.

Mneneri wa polisi ya Dowa a Alice Sitima, wati awiriwa amangidwa lero pa 26 December 2025 kutsatira kafukufuku wa polisi pa imfa ya malemuwa usiku wa pa 25 December.

A sitima, ati oganizilidwawa ndi a Witness Nkhoma a zaka 22 ndi a Chisomo Paul a zaka 25 ndipo onsewa amachokera mmudzi mwa Chinkhota ya m'boma lomweli la Dowa.

Malingana ndi Sitima oganizilidwawa anamenya a Kanyoza kaamba koti amawaganizira kuti amafuna kuwabera nsapato yomwe anali atangogula kumene pamalo ena omwela mowa.

Apolisi ya Dowa atalandira uthengawu anathamangira kumalo angoziwo komwe anapeza kuti malemuwa anamwalira kaamba kakumenyedwa kwambiri mthupi lawo.

Wolemba: Mphatso M'bang'ombe

  Nthambi yoona za nyengo m'dziko muno ya Department of Climate Change and Metiorogical Services yati m'madera ambiri ak...
26/12/2025



Nthambi yoona za nyengo m'dziko muno ya Department of Climate Change and Metiorogical Services yati m'madera ambiri akumpoto ndi ochepa am'chigawo chapakati ndi kumwera akhala akulandira mvula.

Nthambiyi yati mvulayi ikhala ikugwa yamphamvu madera ambiri akumpoto kuyambira mawa loweluka pa 27 December 2025.

Ndipo yati chiopsezo chakusefukira kwa madzi ndichokwera maka m'madera akumpoto komwe mvula idzigwa yamphamvu.

Wolemba Mphatso M'bang'ombe

26/12/2025

NKHANI MADZULO | 26 DECEMBER 2025

  Community involvement and empowerment has been singled out as crucial for national development.This has come out durin...
26/12/2025



Community involvement and empowerment has been singled out as crucial for national development.

This has come out during the Fruits of Mdeka (FOM) Annual general meeting (AGM) which is held at Namikasi Secondary School in Blantyre district.

Speaking as guest of honour Rabecca Ngalande, a retired midwife says when the community is empowered, they will take the initiative as their own and they have the responsibility to look after every project in their area.

FOM President Alfred Butao has commended the members of the group for their commitment saying since its establishment in 2019 they have made a good progress.

“Apart from strengthening relations amongst the people coming from Traditional Authority Chigalu we managed to support learners, elderly people, procure some wheelchairs for the people with disabilities and involved in many development projects in the area,” he said.

Reported by Gift Sitima

Address

Scott Road, Ginnery Corner, P/Bag 39
Blantyre
312200

Opening Hours

Monday 07:30 - 17:00
Tuesday 07:30 - 17:00
Wednesday 07:30 - 17:00
Thursday 07:30 - 17:00
Friday 07:30 - 17:00
Saturday 09:00 - 12:00

Telephone

+265887005791

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Times 360 Malawi posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Times 360 Malawi:

Share