Strong Vision

TANZANIA President wa dziko la Tanzania Samia Suluhu akhalapo yekha pa ballot paper ngati presidential candidate wa zisa...
14/10/2025

TANZANIA

President wa dziko la Tanzania Samia Suluhu akhalapo yekha pa ballot paper ngati presidential candidate wa zisankho zomwe zikufuna zichitike pa 29 October mdziko la Tanzania.

Ak*ti zili chonchi kaamba zipani zotsutsa boma zonse zathawa kumeneko komaso ambili aphedwa, ena apenga misala komaso anthu ena ochuluka amangidwa.

13/10/2025

in Africa when a pastor wants a vehicle, we will contribute for him but when one of members want a vehicle we will pray for him..."receiveee !!"

Pali mphekesera k*ti Mtsogoleri wadziko lino proffessor Arthur Peter Mutharika wasankha a Sameer Suleiman ngati yemwe ak...
12/10/2025

Pali mphekesera k*ti Mtsogoleri wadziko lino proffessor Arthur Peter Mutharika wasankha a Sameer Suleiman ngati yemwe akuyenera kunkhala speaker wa nyumba ya malamulo ku choka ku chipanichi.

Nyumba ya Malamulo yikuyenera kukumana ndi kuvota yemwe ankhoza k*tenga udindowu.

"Video yomwe ikuyendayenda pa social media, anandipanga screen record nthawi yomwe anandiimbira hone pa 10 August.Anali ...
12/10/2025

"Video yomwe ikuyendayenda pa social media, anandipanga screen record nthawi yomwe anandiimbira hone pa 10 August.

Anali boyfriend wanga nde ndinamukhulupilira, atandiimbira phone ndinamuuza k*ti ndikuyimbirabe ndikukasamba, then he said odi tiwone basitu, bwanganduuuuu beans.

Amati kuli show ku South Africa nde anati andiike pa list k*ti ndikaimbe, then ineyo poyamba ndimamuyankha za mwano, then he said usaiwale ndili ndi stuff yako, basitu mpamene waivunga pammbalambanda."

Watero Morale The Rapper pa Mikozi Network kwinaku akulira.

From InboxPlease ndithandizeni maganizo"Posachedwapa, ndakhala ndikuvutika. Zimandipweteka kuona mwana wanga wamkazi wa ...
12/10/2025

From Inbox

Please ndithandizeni maganizo

"Posachedwapa, ndakhala ndikuvutika. Zimandipweteka kuona mwana wanga wamkazi wa zaka 6 akuchitiridwa nkhanza ndi mkazi wanga watsopano tsiku lililonse, koma ndimadziona k*ti ndilibe mphamvu zomuletsa.

Nthawi iliyonse akamachitira mwana wanga wamkazi motere, amandiumiriza k*ti ndisalowelere nawo. Ndikudziwa k*ti sindine tate wabwino wa mwana wanga komabe ndimakondanso kwambiri mkazi wanga.

Amandimvetsetsa m'njira zomwe palibe wina aliyense, ngakhale mkazi wanga womwalirayo sadakwanilitsepo.

Ndakhala ndikuwapempha mobwerezabwereza ndikuchonderera banja la malemu mkazi wanga k*ti atenge mwana wanga wamkazi k*ti akakhale nawo. Ndinalonjezanso k*ti ndidzamutumizira ndalama pafupipafupi k*ti azisamalira komanso zosowa zake. Komabe, amaumirira k*ti azikhala ndi ine, ponena k*ti akuyenera kukondedwa ndi abambo ake ndipo sakufuna kumulanda.

Tsopano ndimadzimva kukhala wokanidwa. Ndakhala ndikumuchonderera mkazi wanga kangapo ngati angapeze njira yolandirira mwana wanga, koma amaumirira k*ti ndimupezere malo ena okhala chifukwa sadakonzekere kukhala naye m'nyumba imodzi mwana wangayo .

Pakadali pano ndikuvutika komanso sindikudziwa choti ndichite. Kunena zoona, sindikufuna k*taya mkazi wanga, amene amandikonda komaso amandimvetsetsa mozama chifukwa cha mwana wanga wamkazi.

Ndikudziwa k*ti ndiyenera kukhala bambo woteteza mwana wanga, koma ndiyeneranso kusangalala. . Ndine mnyamata wazaka 49 yemwe ndikufunanso kukhala ndi chibwenzi chokoma. Komanso mkaziyu ali ndi pakati( mimba yanga ) Kunena zowona, ndimamva chisoni kwambiri ndi mwana wanga, koma ndatayika kwathunthu.

Ndipange bwanj k*ti mwana wanga akhale otetezedwa kwa mkazi wanga komaso k*t ndisasiyane ndimkazi wanga

Please help me 💔😭

Ak*ti anamutumizira ndalama yomangisila mmutu ndi Transport  Kuti akumane Saturday koma Sanapiteko.Nde lero mwamuna yo w...
12/10/2025

Ak*ti anamutumizira ndalama yomangisila mmutu ndi Transport Kuti akumane Saturday koma Sanapiteko.

Nde lero mwamuna yo wangolawilirako yekha nkukatenga zakezo

 .   ndi upcoming Female artist. Ndikuziwa ambri mwainu simukumuziwa 'YES' But as i said k*ti She is a Female upcoming a...
12/10/2025

.

ndi upcoming Female artist. Ndikuziwa ambri mwainu simukumuziwa 'YES' But as i said k*ti She is a Female upcoming artist nde simungamuziwe nonse..

Tsiku ngati lero pa 12 October mu chaka cha 2021 ku masana, oyimba yu anapanga post ku Page yake zodandaula oyimba wina wa chambba cha Gospel yemwe ankafuna Kuti azipanga naye Chisembwele.

She posted this

"Most of you guys mwakhala mukundifusa kt sindipanga macollabo ndima artist akuluakulu chifukwa chani? Ena mumafusa kt ndilibe manager chifukwa chani?

It all started in 2020 nditatulutsa nyimbo yanga yoyambilila pa made on monday.. Ma artist akuluakulu ena anandibigger, kundilimbikisa k*ti ndizipusha.. Fast foward, mu 2021 ndinatulusa nyimbo inaso pa made on mondayso and this time around ku twitter kwanga ndikomwe kunayaka moto.. I could get a lot of random messages from strange men, asking for my number, ena ati we should be friends, ena kumati afuna azindipanga manage.. To my surprise anthu ofuna kundipanga manage aja amapezeka kt akundifusa zinthu zosemphana ndiza music and then ndinangozituluka k*ti sindizakhalaso ndi manager..

Nthawi yomwe ndinatulusa nyimbo yanga yachiwiriyo ndinapangidwa follow ndima artist akulu akulu ambiri pa twitter and anandibiggerso pamenepaja.. Nde kunali pressure ma message kudzadza ku twitter ndi whatsapp..

Ma artist akuluakulu angapo anandihalla kumati we should work.. I was really excited poona izi... Artist wina wa gospel anandihalla kundiuza k*ti afunitsitsa titayimba nyimbo limodzi and i asked him kt nde ikhala gospel, do you think it will work cz timayimba zinthu zosiyana and ma fans ako sangafille k*ti uyimbe zaiinezi and he was like okay, chabwino sitiyimba bt i'll be supporting you cz ndaona kt uli ndi tsogolo...

I was very excited and sindinakhulupilire.. We used to be texting patalipatali and tsiku lina anangondiuza kt ndufuna ndik*tumizile ndalama urecorde nyimbo plus ujambulise video koma we should be f*cking buddies.. Ndinamuuza kt sindingakwanise and anakwiya nkundiuza kt i should clear the conversations and send him a screenshot... Ine ndinadeleterdi kenako sanandi-Blocker mmoti kucheza kunathela pomwepo

WOPHUNZIRA WA CHAKA CHOMALIZA KU UNIMA WAMWALIRAInnocent Mwase, ophunzira wa chaka chotsiliza ku University of Malawi (U...
12/10/2025

WOPHUNZIRA WA CHAKA CHOMALIZA KU UNIMA WAMWALIRA

Innocent Mwase, ophunzira wa chaka chotsiliza ku University of Malawi (UNIMA) wamwalira dzuro ku Zomba ndipo sanadwale wangogwa.

Iye wafikitsa chiwelengero cha ophunzira pafupifupi 78 a sukulu za ukachenjede omwe amwalira mdziko muno mukanthawi kochepa.

Kumvenji Lamba, wothandizira kuyendetsa sukulu ya UNIMA atsikimiza izi ndipo apepesa akubanja ndi anthu onse okhudzidwa.

Mwase amachita maphunziro Bachelor of Arts in Political Sciences.

May his Soul Rest in peace 💔

Nana wabweranso❤️
12/10/2025

Nana wabweranso❤️

11/10/2025

Ndilibe UFA nde ndangoti Neba Lero mgaiwa sindkuufuna gaileko Ufa oyera Ndidyeko Lero, iye Ati bweletsan mgaiwawo tisithane 💔😭

Chipani cha DPP chadzudzula a Noel Lipipa komanso a Kamlepo Kalua kamba konena k*ti omwe anatumidwa ndi Chipani kukaumil...
11/10/2025

Chipani cha DPP chadzudzula a Noel Lipipa komanso a Kamlepo Kalua kamba konena k*ti omwe anatumidwa ndi Chipani kukaumiliza a George Kasakula k*ti apepese ndi anyamata a DPP ndipo akuyenera kulandira chilango

Kalata yomwe mneneri wa Chipanichi a Shadreck Namalomba atulutsa yati Chipanichi sichinatume aliyense kuchita izi ndipo sikoyenera k*ti mamembala a Chipanichi adzilowerera pa zinthu zomwe sidzikuwakhuza koma zikukhuza dzina la Chipani

Kalatayo yaoophseza k*ti awiriwa apepese ndipo aliyense olowerera nkhani za Chipani popanda kudutsira ku nthambi yazofalitsa nkhani adzalandira chilango.

Nkono mukuona wo  ndiwa mayi Vanessa omwe anatulutsira mwana wawo wa miyezi isanu ndi iwiri (7) pawindo k*ti ampulumuse ...
11/10/2025

Nkono mukuona wo ndiwa mayi Vanessa omwe anatulutsira mwana wawo wa miyezi isanu ndi iwiri (7) pawindo k*ti ampulumuse thawi yomwe nyumba amakhala itayaka Moto mwazizi.

Iwo ak*ti atangozindikila zoti nyumba yawo ikuyaka moto choyambilira anaganizila pomwe panali mwana wawo.
amafuna mwana wawo asafe chifukwa cha utsi. Mwachisomo cha mulungu odzimitsa moto (fire fighters) anatukila mwachangu atalandila uthenga wazizizi'wu ndipo anakwanitsa kupulimutsanso mayi wo..

God bless all women chikondi chanu ndichokwanira

Address

31 Ikatali
Blantyre
7100

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Strong Vision posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Strong Vision:

Share