Calvary Family Church Radio FM

Calvary Family Church Radio FM Liwu lokupatsani chiyembekezo

Yemwe akuimilila chipani cha UTM Ngati phungu wa dera la Zingwangwa Soche anaponya voti yake Ku namasimba ward mderali.
16/09/2025

Yemwe akuimilila chipani cha UTM Ngati phungu wa dera la Zingwangwa Soche anaponya voti yake Ku namasimba ward mderali.

Pulezidenti wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera yemwenso ndi mtsogoleri wachipani Cha Malawi Congress party wafika pa male...
16/09/2025

Pulezidenti wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera yemwenso ndi mtsogoleri wachipani Cha Malawi Congress party wafika pa malembo F P school boma la Lilongwe kuzaponya voti yawo

Iye ndi Mayi akunyumba kwawo ayima panzele monga ngati aliyense akuchitira

wolemba Eve Maselenga

anthu akudikila modekha kuti aponye voti ngakhale kuli dzuwa komanso kutentha pa malo ovotela a St Pius ku nkololosa mun...
16/09/2025

anthu akudikila modekha kuti aponye voti ngakhale kuli dzuwa komanso kutentha pa malo ovotela a St Pius ku nkololosa munzinda wa Blantyre.

pa malo oponyela a manja mu nzinda wa Blantyre anthu oponya voti akumaunikidwa chala kapena ka pepala kovotela kenaka ak...
16/09/2025

pa malo oponyela a manja mu nzinda wa Blantyre anthu oponya voti akumaunikidwa chala kapena ka pepala kovotela kenaka akumapitanso Pena pomwe ogwira ntchito akumawachonga mu buku la anthu oponya voti.

muchithunzichi ogwira ntchito ku bungwe la chisankho kuunika oponya voti.

Zina mwazinthuzi pa Malo oponyela voti m'dera la Chirimba.
16/09/2025

Zina mwazinthuzi pa Malo oponyela voti m'dera la Chirimba.

kuli bata ndi chitetezo pamalo oponyela voti pa sukulu ya manja m'dera la Zingwangwa Soche.
16/09/2025

kuli bata ndi chitetezo pamalo oponyela voti pa sukulu ya manja m'dera la Zingwangwa Soche.

16/09/2025

Anthu analawila mwaunyinji pa sukulu ya manja mu m'dera la Zingwangwa Soche.

Mmodzi mwa omwe akuimira ngati khansala mu chipani cha UTM ku dera la Bangwe Namiyango Elipher Mvula Banda ati ndi okonz...
12/09/2025

Mmodzi mwa omwe akuimira ngati khansala mu chipani cha UTM ku dera la Bangwe Namiyango Elipher Mvula Banda ati ndi okonzeka kutukula derali ngati angapatsidwe mpata.

A Mvula Banda omwe ndi aulumali wa kayendedwe ati anthu asayang'anire ulumali omwe ali nawo koma mfundo zimene zitukule dera la Bangwe Namiyango.

Iwo anapitiliza kupempha anthu kusintha maganizo omawayang'anira pansi anthu aulumali ponena kuti munthu wina aliyense ali ndi kuthekera kopanga zinthu.

wolemba Chaulea Mwale

The Malawi Electoral Commission has begun dispatching ballot papers to constituencies in preparation for the upcoming el...
10/09/2025

The Malawi Electoral Commission has begun dispatching ballot papers to constituencies in preparation for the upcoming elections scheduled for September 16.

MEC Chairperson, Justice Annabel Mtalimanja, confirmed the development on Tuesday, September 9, when she oversaw the process at a secure warehouse at Kamuzu International Airport in Lilongwe. She emphasized that security remains a top priority to safeguard the voting materials.

“We are starting with Chitipa and Karonga, Rumphi and Mzuzu, as well as Nsanje and Chikwawa, Mulanje and Phalombe, because the plan is to begin with areas that are hard to reach and farthest,” said Mtalimanja.

She added that all logistics had been carefully arranged: “Vehicles have been fully serviced, we have ensured that there is enough fuel, and the vehicles will be tracked. We want to assure the public that the materials are under heavy security provided by the Malawi Defense Force and Malawi Police Service.”

According to MEC, the dispatch is expected to be completed by Thursday, September 11. From there, the ballot papers will be distributed to polling centers between September 13 and 14.

Meanwhile, candidates across the country are intensifying their campaigns as they look to cement their chances of winning in their respective positions.

By Eve Tabitha Maselenga (CFC Radio)

Unduna wa za malonda wati nthawi yakwana kuti anthu mdziko muno azigwiritsa ntchito njira zamakono pochita malonda.Mmodz...
08/09/2025

Unduna wa za malonda wati nthawi yakwana kuti anthu mdziko muno azigwiritsa ntchito njira zamakono pochita malonda.

Mmodzi mwa akuluakulu kuchokera ku undunawu wa za malonda Ezron Chirambo wati kugwiritsa ntchito Internet popanga malonda ndi njira ya bwino imene anthu makono kugwiritsa ntchito.

A Chirambo anena izi lolemba mu mzinda wa Blantyre pamapeto a mkumano ophunzitsa anthu ochita malonda kudziwa njira zamakono za malonda.

Ku mkumanowu kunali anthu osiyana siyana kuchokera ku unduna wa za malonda, unduna wa za chuma, komanso ma bungwe oyendetsa ntchito za malonda.

Wolemba:Chaulea Mwale

A Ben Phiri ati mwa zinthu zina zomwe aphunzira ngati chipani atatuluka m'boma ndi monga kuipa kuika ma number plate a g...
08/09/2025

A Ben Phiri ati mwa zinthu zina zomwe aphunzira ngati chipani atatuluka m'boma ndi monga kuipa kuika ma number plate a galimoto olemba "Ana a dad".

Iwo ati izi sizizachitikanso akalowa m'boma pa 17 poti izi zinali zolakwika.

A Ben Phiri omwe ndiwokopa anthu kuchipanichi akulankhula Ku msonkhano wa atolankhani omwe chipanichi chikuchititsa mu nzinda wa Blantyre.

A Phiri atinso chipani cha DPP aza. Chizachepetsa mdipiti wa galimoto zomwe zimapelekeza mtsogoleri wa dziko

Mmawu awo mkulu wa komiti ya amayi, Mary Navitcha wati chipanichi chaphunziranso zolakwika zomwe chipani cholamula Cha MCP chachita ndipo akhala akukonza zolakwika zonse pamodzi.

Poonjezera, mneneri wachipanichi Shadreck Namalomba wati chipanichi chili ndi chikhulupulilo chonse kuti apambana pa chisankho cha pa 16 September.

CFC radio BLANTYRE (Eve Tabitha Maselenga)

We want to assure the nation that maranantha Academy will return to number one, Dr Kaonga says.Maranatha Academy chairpe...
05/09/2025

We want to assure the nation that maranantha Academy will return to number one, Dr Kaonga says.

Maranatha Academy chairperson Dr Ernest Kaonga says the school has maintained a ninety nine percent pass rate with top students scoring eight points.

Speaking at a media conference in Blantyre, Kaonga said the highest performing student scored eight points a point more than the national highest who got seven.

"Well since 2017 maranantha Academy has had highest performing students who have scored the first or second highest points. This year we have the second highest scoring student, bit next year we will be back on top, I want to assure the nation," He said.

Address

Kapeni Road
Blantyre

Telephone

+265881281579

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Calvary Family Church Radio FM posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share

Category