
28/09/2025
Zikumveka kuti bwana Moses kumkuyu athawa mdziko muno kuthawira ku UK komwe banja lawo limakhala.
Kuthawaku kwachitika a MEC atangolengeza posachedwapa kuti a Peter Muntharika ndi omwe apambana pa chisankho cha u President kutikita a Lazarus Chakwera ndi mavoti osasimbika.
Ngakhale kuti chipani cha MCP chinaima pa chulu ndikumati chaberedwa mavoti ndi chipani Cha DPP Komabe izi sizinaphule kanthu kamba koti a Chakwera anavomereza msanga kugonja kwawo pachisankhochi ndikumufunira zabwino zonse Muntharika.