Capital FM Malawi

Capital FM Malawi Malawi's number one urban News, Business and Hit Music station.
(1)

Escape Ordinary Radio🎙️
Advertise with us: +265886274444
96.4 & 96.6 FM
Stream: bit.ly/3OvGNVn
Instagram: capitalfmmw
X
WhatsApp: bit.ly/3W4rRSW
YouTube: https://www.youtube.com/
Capital FM is a privately owned Adult Contemporary English Radio Station that was launched 29th March 1999. Capital FM was the second commercial station to be launched and now

boasts majority listener-ship amongst the bi-lingual urban population. We are affiliated with the British Broadcasting Corporation (BBC World) and Voice of America (VOA)
We value civic responsibility and seek to give the people of Malawi a voice by providing quality broadcast news, information and entertainment programming that will assist them to speak out for better services and good governance.

17/09/2025



Unofficial results for presidential elections in Karonga Songwe Constituency:
1- Arthur P. Mutharika 8,479
2-Lazarus Chakwera 2,592
3- Dalitso Kabambe 633


17/09/2025



Zipani za MCP ndi DPP zikusinthana mawu pa momwe chisankho chachikulu chikuyendera, pomwe zonse zikhulupilira kuti zapambana.

Poyankhula pa misankhano ya olemba nkhani ku Lilongwe, zipanizi zikudzudzulana kaamba koyima pa chulu, chilichonse nkumazitamandira kuti chachita bwino.

Mwa chitsanzo, Jessie Kabwila wa MCP akuti DPP ili patsogolo kukhulupirira kuti mtsogoleri wake, Peter Mutharika wapambana, ngakhale kuti bungwe la MEC silinalengeze zotsatira.

Koma poyankhapo, DPP kudzera mwa mneneri wake, Shadric Namalomba yati ikutsatira zotsatira zosatsimikizika poonjezera kuti ndi zodabwitsa kuti MCP ikukhulupiriranso kuti yachita bwino.

Pothirirapo ndemanga, oyankhulapo pa nkhani za ulamuliro ndi ndale, Andrew Kaponya wa ku sukulu ya ukachenjede ya MUBAS, akuti sizodabwitsa kuti zipanizi zikuyankhulana motere.

Kaponya, Komabe, wachenjeza zipanizi kuti zipewe kuzilengeza zokha kuti zopambana kufikira bungwe la MEC lilengeze.

17/09/2025



Aspiring members of Ighembe ward have expressed dissatification over MEC's decision to hold by-elections in the ward, following omission of some candidates from the ballot paper.

Margret Mwakalinga whose name was missing on the ballot paper says the decision has come at a wrong time when she has already spent more resources preparing for the ongoing electoral period.

She added that she does not have enough resources to participate for fresh elections, therefore she is calling for MEC to reconsider, saying that this puts her on the verge of not doing well.

People's Party aspiring ward councilor, Moshi Fundi whose name was on the ballot paper, said this is MEC's fault therefore, the decision is not fair to them and it will be hard to gather resources for the by-elections.

However, an independent aspirant for the ward, Adrian Masimbi said he has positively welcomed the decision and is ready to contest again, even if it means pulling more resources

By Winkly Mwaulambo

17/09/2025




Malingana ndi Sameer Suleman, chipani chawo cha DPP ndichodabwa ndi zomwe wanena mneneri wa chipani cholamula cha Malawi Congress MCP, pomwe anauza olemba nkhani kuti chipani chawo. chawina kale,

Iye wati ndizodabwitsa kuti akuluakulu a chipani cha MCP akuwoneka kuti apeza kale zotsatira za chisankho pomwe bungwe la MEC silinayambe kulengeza.

Powonjezera izi, Ben Phiri wayamikira a chitetezo a Malawi Defence Force MDF, kaamba kopeleka chitetezo chokwima kuchoka pa tsiku lovota kufika lero.

Iye wati pakufunika kuti zofuna za anthu pachisankhochi zilemekezeke.


     Chipani. Ha Democratic Progressive DPP chikuchititsa mkumano wa olemba nkhani Ku Lilongwe.Mkumanowu ukutsogodzedwa ...
17/09/2025




Chipani. Ha Democratic Progressive DPP chikuchititsa mkumano wa olemba nkhani Ku Lilongwe.

Mkumanowu ukutsogodzedwa ndi mkulu wofalitsa nkhani ku chipanIchi, Shadreck Namalomba, komanso Sameer Suleman, Alfred Gangata ndi Ben Phiri.

17/09/2025



Malingana ndi bungwe loyendetsa chisankho MEC, Malo otsatirawa alandila zotsatira kuchokara Ku Madera awo:

Chitipa
Salima
Mzuzu City
Mangochi
Balaka
Machinga
Chiladzuru
Neno
Lutchenza


17/09/2025





Pakadalipano, bungwe la MEC lati chisankho cha makhansala ku Ighembe ward ku Karonga, achiimitsa kaamba ka mavuto awiri omwenso anakhudza anthu awiri omwe amapikisana nawo pa mpandowu.

Awiriwa ndi Adrian Masimbi komanso Margret Mwakalinga.


17/09/2025



Unofficial results from 13 out of 24 polling centers for the presidential elections in Kasungu Municipality Constituency.

Joyce Banda PP 55
Banda Thokozani indipendent 18
Bandawe Akwame AAA 35
Chakwera Lazarus MCP 5235
Chibambo Kamuzu indipendent 11
Chilungo James independent 7
Chipojola Felix independent 3
Kabambe Dalitso UTM 521
Muluzi Atupere UDF 131
Peter Mutharika DPP 4645
Mvula Phunziro indipendent 8
Mwenefumbo Tumpale NDP 1
Nankhumwa Kondwani PDP 2
Sauti Jordan P*P 2
Smart Swira indipendent 0
Tobias Milward indipendent 3
Usi Micheal 45

By Saulos Nyirenda

  Ntchito yoika pamodzi zotsatira zosatsimikizika za dera la ku nzambwe m'boma la Mchinji tsopano yatha.Pakadali pano og...
17/09/2025




Ntchito yoika pamodzi zotsatira zosatsimikizika za dera la ku nzambwe m'boma la Mchinji tsopano yatha.

Pakadali pano ogwira ntchito ku MEC ndi oyimilira omwe akupikisana nawo pachisankhochi akudikira zotsatira zakuderali komwe anthu aponya voti yawo m'malo okwana 17.

Anthu okwana 29,000 ndiomwe analembetsa ku dera la kunzambwe m'bomali.

Wolemba: Emmanuel Chawula

17/09/2025




Bungwe loyendetsa chisankho la Malawi Electoral Commission MEC, lati zotsatira za chisankho chomwe chinachitika dzulo zikuwelengedwabe.

Malingana ndi wapampando wa bungweli Annabel Mtalimanja, ntchito yonyamula katundu ovotera ikupitilira m'madera ena pomwe kwina ntchitoyi yatha.

Pakadalipano, Mtalimanja wapempha atsogoleri adzipani zosiyanasiyana kuti alewe kudzilengeza okha ngati owina koma adikile kuti bungwe la MEC lidzalengeze.

Iye wati kudzilengeza wekha ngati owina ndi Mlandu ndipo malamulo agwira ntchito.


17/09/2025



Adindo m'boma la Blantyre ati vuto la netiweki likuchedwetsa ntchito yotumiza zotsatira za chisankho kuchokera mmadera a aphungu, kupita ku malo olandilira zotsatira za chisankho m'boma lonse ku HHI.

Mkulu oyang'anira za chisankho m'boma la Blantyre yemwenso ndi bwanamkubwa wa bomalo a Alex Mdooko watsimikiza za nkhaniyi poyankhula ndi olemba nkhani ku malowa.

Pamene nthawi imakwana cha mma 10 koloko mmawa uno, zotsatira zochuluka zinali zitafika mmalo olandilira zotsatira a madela a aphungu.

Mdooko wati m'madera akumidzi kwa m'boma la Blantyre kuli malo oponyera voti okwana 164.

     Posachedwapa, akuluaku a bungwe la Malawi Electoral Commission MEC, akhale akuchititsa mkumano wa olemba nkhani ku ...
17/09/2025




Posachedwapa, akuluaku a bungwe la Malawi Electoral Commission MEC, akhale akuchititsa mkumano wa olemba nkhani ku malo olandilira zotsatira za chisankho (main tally Centre)


Address

Namiwawa
Blantyre
PRIVATEBAG437,CHICHIRIBLANTYRE3.

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Capital FM Malawi posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Capital FM Malawi:

Share

Category

Capital FM Malawi

Malawi's #1 urban News, Business and Hit Music station launched in 1999. Capital FM is a privately owned radio station which broadcasts in English and Chichewa and aims to give the people of Malawi a voice, by providing quality broadcast news, information and entertainment programming that will assist them to speak out for better services and good governance. Capital FM boasts majority listenership amongst the bi-lingual urban population, particularly with decision makers. Our partners include the British Broadcasting Corporation (BBC World) and Voice of America (VOA).