Capital FM Malawi

Capital FM Malawi Escape Ordinary Radio. 96.4MHz & 96.6MHz Malawi's number one urban News, Business and Hit Music station.
(4)

Capital FM is a privately owned Adult Contemporary English Radio Station that was launched 29th March 1999. Capital FM was the second commercial station to be launched and now boasts majority listener-ship amongst the bi-lingual urban population. We are affiliated with the British Broadcasting Corporation (BBC World) and Voice of America (VOA)
We value civic responsibility and seek to give the peo

ple of Malawi a voice by providing quality broadcast news, information and entertainment programming that will assist them to speak out for better services and good governance.

Timu ya Creck Sporting yalengeza kuti yachotsa ntchito mphunzitsi wamkulu Eliya Kananji, wachiwiri wake Harrison Saidi k...
10/06/2026

Timu ya Creck Sporting yalengeza kuti yachotsa ntchito mphunzitsi wamkulu Eliya Kananji, wachiwiri wake Harrison Saidi komanso wochititsa mafizo Blessings Tembo.

Atatuwa anaimitsidwa pa ntchito masiku apitawa potsatira kusachita bwino kwa timuyi.

Komabe, mu kalata yomwe yatulutsa, timuyi yayamikira aphunzitsiwa chifukwa cha kulimbikira kwawo pantchito ndipo yawafunira zabwino.

Timu ya Creck sinapambanepo masewero aliwonse mu FDH Premiership ndipo iri pansi penipeni pa mndandanda wa matimu mu mpikisanowu ndi ma point awiri okha basi.

Wolemba: Rhodes Msonkho Jr.

In a bid to avoid over supply of volumes of to***co in the next growing season, the To***co Commission intends to limit ...
10/06/2026

In a bid to avoid over supply of volumes of to***co in the next growing season, the To***co Commission intends to limit production.

The Commission's Chief Executive Officer, Evance Chilumpha disclosed this when he appeared before the Parliamentary committee on Industry, Trade and Tourism.


Three people have been arrested in Blantyre for allegedly being found in possession of cannabis sativa without a permit....
10/06/2026

Three people have been arrested in Blantyre for allegedly being found in possession of cannabis sativa without a permit.

The suspects, identified as Loy Chinangwa, 30, Hanif Vasilatosi, 25, and Benard Saiwala, 24, were arrested at Chemusa Township during an intelligence-led operation by officers from Kabula Police Unit.

Blantyre Police Assistant Public Relations Officer Doris Mwitha confirmed the arrests, saying the suspects were allegedly found with loose cannabis sativa weighing about one kilogramme each.

She said the recovered substance has been seized pending examination, while the suspects remain in police custody awaiting court proceedings.

By Noel Mkwaila

10/06/2026

Apolisi m'boma la Ntchisi atsimikiza kuti amanga abambo awiri kaamba koba ndikumenya bambo wazaka 53 Lloyd Banda pomuganizira kuti amafuna kuwabera ndalama powanamiza.

Malingana ndi mneneri wa polisi ya Ntchisi Salomy Zgambo womangidwawa ndi Chikumbutso Kachinaka wazaka, 31 wamudzi mwa Ng'ondora pomwe Tobias Kusowa wazaka 36 wamudzi mwa Kasula onse ochokera kwa mfumu yaikulu Msauka m'bomali.

Iye wati nkhaniyi inachitika pakati pa 7 ndi 8 mwezi uno pomwe Lloyd Banda anapita pa shop ya Kachinaka kukatsatsa mabelo asuga okwana 18 kuti amugule ndipo anagwilizana pamtengo wa K750,000 koma zithu zinavuta pomwe mwini shopuyu anazindikila kuti amagofuna kuwabera pomwe amafuna kutumiza ndalamayi.

Zgambo wati mwini shopuyu m'malo motengera mkuluyu ku polisi anapita naye kunyumba kwake komwe anamanga manja ake komanso kumenya ndikumusiya mchimbudzi mpaka usiku wonse.

"Ndipo pa 8, Banda anamuchotsa kunyumba kwa Kachinaka kupita naye kunyumba kwa Tobias koma atamanga manja onse komanso miyendo ndikukamuyika khola lambuzi."Watero Zgambo.

Zgambo wati apolisi analandila uthenga wokhudza nkhaniyi ndipo anapita kumalowa komwe anapheza ndikumupulumutsa komanso kupita naye kuchipatala cha Ntchisi komwe akulandira thandizo.

Pakadali pano iye wati abambo awiri ali mchitokosi pomwe akuyembekezera kukawonekera ku bwalo lamilandu.

Wolemba: Philord Kamagunda Magalasi

Bwalo la Magistrate m'boma la Nsanje latulutsa pa belo mfumu yaikulu Chimombo yomwe inamangidwa pamulandu okhudzana ndik...
10/06/2026

Bwalo la Magistrate m'boma la Nsanje latulutsa pa belo mfumu yaikulu Chimombo yomwe inamangidwa pamulandu okhudzana ndikuononga katundu (malicious damage).

Haneef Ngundende oweruza milandu ku bwalo la Second Grade Magistrate wapereka chigamulochi pomwe mfumuyi inakaonekera kubwaloli lachitatu masana.

Lusungu Gondwe yemwe amayimira Chimombo pamulanduwu wati ndiokondwa kuti bwalo lamva pempho lawo kuti mfumuyi ituluke pabelo ndipo apempha ambali yaboma kuti afulumizitse mulanduwu.

Mfumu yaikulu Chimombo inamangidwa lachisanu sabata latha poganiziridwa kuti ikukhudzidwa ndikuonongedwa kwa mlatho wakale pamtsinje wa Mchenga Malembo m'bomali Koma mfumuyi ikuukana mulanduwu.

Wolemba: Manford Chirombo

Kampani ya Lainya Electrical Contractors yayamba ntchito yoika magetsi msukulu zisanu  m'boma la Nsanje.Mkulu wa kampani...
10/06/2026

Kampani ya Lainya Electrical Contractors yayamba ntchito yoika magetsi msukulu zisanu m'boma la Nsanje.

Mkulu wa kampani ya Lainya Electrical Contractors McDonald Samuel wauza Capital online kuti ntchitoyi ayigwira msukulu za primary za Nyanjiwa, Mthawira, Chigumukire, Ndiola ndi malo achitukuko cha aphunzitsi (TDC) a Chigumukire m'bomali.

"Tinachiona kuti mchofunika kuti tiike magetsi msukuluzi ndicholinga choti tithandizire pantchito zotukula maphunziro m'boma lino. Ntchitoyi tikuyembekezera kuigwiranso msukulu zina mzigawo zamaphunziro monga za Mpatsa ndi Kaloga mugawo lachiwiri lantchitoyi," watero Samuel.

Mlangizi wazamaphunziro mchigawo cha Chigumukire, Blessings Salagi wayamikira kampaniyi kaamba Kantchitoyi ponena kuti ophunzira msukulu zomwe zipindure ndindondomekoyi tsopano akwanitsa kuwerenga nthawi yausiku zomwe zithandize kutukula maphunziro m'derali.

Kampani ya Lainya Electrical Contractors ikuyembekezeka kugwiritsa ntchito ndalama zokwana 18.6 million Kwacha pogwira ntchitoyi.

Wolemba: Manford Chirombo

Bwalo la Magistrate m'boma la Nsanje latulutsa pa belo mfumu yaikulu Chimombo yomwe inamangidwa pa mulandu okhudzana ndi...
10/06/2026

Bwalo la Magistrate m'boma la Nsanje latulutsa pa belo mfumu yaikulu Chimombo yomwe inamangidwa pa mulandu okhudzana ndikuononga katundu (malicious damage).

Haneef Ngundende, oweruza milandu ku bwalo la Second Grade Magistrate, wapereka chigamulochi pomwe mfumuyi inakaonekera ku bwaloli lachitatu masana.

Lusungu Gondwe yemwe amayimira Chimombo pa mulanduwu wati ndiokondwa kuti bwalo lamva pempho lawo kuti mfumuyi ituluke pabelo ndipo apempha ambali yaboma kuti afulumizitse mulanduwu.

Mfumu yaikulu Chimombo inamangidwa lachisanu sabata latha poganiziridwa kuti ikukhudzidwa ndikuonongedwa kwa mlatho wakale pa mtsinje wa Mchenga Malembo m'bomali Koma mfumuyi ikuukana mulanduwu.

Wolemba: Manford Chirombo


Bwalo la magistrate m'boma la Chikwawa lalamula Francis Kagone wazaka 30 kuti apereke chindapusa cha ndalama zokwana 700...
10/06/2026

Bwalo la magistrate m'boma la Chikwawa lalamula Francis Kagone wazaka 30 kuti apereke chindapusa cha ndalama zokwana 700, 000 kwacha kaamba kopezeka olakwa pa mulandu oyendetsa chipatala opanda chilolezo.

Atakaonekera kubwalo lamilandu lachiwiri, kagone anavomera mulanduwu ndipo anapempha bwalo kuti limuchitire chifundo kaamba koti anavomera kulakwa kwake komanso kuti ndikoyamba kuti iye apalamule mulandu.

Oimira boma pa milandu Enerst Mangwena, naye anapempha bwaloli kuti lipereke chilango chokhwima kwa Kagone poganizira kuti kuyendetsa chipatala opanda chilolezo kungaike chiopsezo chachikulu kumiyoyo ya anthu.

Popereka chigamulo chake, oweruza Annie Chikhadzula, anagwirizana ndi ambali ya boma polamula Kagone kuti apereke chindapusa chandalama zokwana 700,000 kwacha ndipo akalephera akagwire ukaidi wazakwa ziwiri.

Bwaloli lalamulanso kuti mankhwala omwe adalandidwa kwa Kagone aperekedwe kunthambi yaboma yoona zamankhwala ndicholinga choti akaunikidwe bwino.

Wolemba: Manford Chirombo


Kampani ya Lainya Electrical Contractors yayamba ntchito yoika magetsi msukulu zisanu m'boma la Nsanje.Mkulu wa kampaniy...
10/06/2026

Kampani ya Lainya Electrical Contractors yayamba ntchito yoika magetsi msukulu zisanu m'boma la Nsanje.

Mkulu wa kampaniyi McDonald Samuel, wauza Capital online kuti ntchitoyi ayigwira msukulu za primary za Nyanjiwa, Mthawira, Chigumukire, Ndiola ndi malo achitukuko cha aphunzitsi (TDC) a Chigumukire m'bomali.

"Tinachiona kuti mchofunika kuti tiike magetsi msukuluzi ndicholinga choti tithandizire pantchito zotukula maphunziro m'boma lino. Ntchitoyi tikuyembekezera kuigwiranso msukulu zina mzigawo zamaphunziro monga za Mpatsa ndi Kaloga mugawo lachiwiri lantchitoyi," watero Samuel.

Mlangizi wa zamaphunziro mchigawo cha Chigumukire, Blessings Salagi wayamikira kampaniyi kaamba ka ntchitoyi ponena kuti ophunzira msukulu zomwe zipindure ndi ndondomekoyi tsopano akwanitsa kuwerenga nthawi yausiku zomwe zithandize kutukula maphunziro m'derali.

Kampani ya Lainya Electrical Contractors ikuyembekezeka kugwiritsa ntchito ndalama zokwana 18.6 million Kwacha pogwira ntchitoyi.

Wolemba: Manford Chirombo


Human Rights Watch has presented a report to Vice President Jane Ansah highlighting continued attacks and violations aga...
10/06/2026

Human Rights Watch has presented a report to Vice President Jane Ansah highlighting continued attacks and violations against persons with albinism in Malawi.

The report, set to be launched this Friday in Lilongwe, is based on research conducted in nine districts, where over 80 people, including persons with albinism, their families, community leaders, and rights organizations, were interviewed.

The study examined challenges affecting people with albinism, including education, employment, inclusion, and access to social protection programmes.

Speaking after meeting the Vice President, Elizabeth Kamundia, Director of the Disability Rights Division at Human Rights Watch, urged government to fund the National Action Plan on Albinism and address the social and economic exclusion faced by people with albinism.

By Jane Kaonga

Address

P/Bag 437, Chichiri, Blantyre 3
Blantyre

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Capital FM Malawi posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Capital FM Malawi:

Share

Category