Nyungwe Community Radio

Nyungwe Community Radio Nyungwe Community Radio serves as a powerful advocacy platform promoting social and economic change among over 300,000 people of Chikwawa District.

This includes addressing gender based violence and mitigating against environmental degradation.

Nyungwe FM SportsMayi wa fuko lino Gertrude Mutharika wafika pa bwalo la ndenge la Kamuzu mu mzinda wa Lilongwe komwe at...
19/08/2026

Nyungwe FM Sports

Mayi wa fuko lino Gertrude Mutharika wafika pa bwalo la ndenge la Kamuzu mu mzinda wa Lilongwe komwe atsogolere kulandira timu ya Scorchers pa ulendo wake ochokera ku mpikisano wa WAFCON komwe inathera pa nambala yachiwiri.

Ku bwalori kwafikanso anthu osiyanasiyana okonda mpira kuphatikizapo nduna yowona za masewero Alfred Gangata ndi nduna zina zochuluka.

Timuyi ikuyembekezereka kufika nthawi ya 15:30.

Wolemba : Robert malenga

19/08/2026

Mabungwe omwe siaboma komanso nthambi yomenyera ufulu wa maphunziro pa boma m'boma la Chikwawa, adandaula ndi zotsatira za mayeso a sitandade 8 komanso folomu 2 ponena kuti ophunzira sadachite bwino kwenikweni

Malingana ndi mkulu wa bungwe la Khalanimaso Youth, a John Josiki limodzi mwa mabungwewa ati nzomvetsa chisoni kuti Chikwawa ngati boma lakanika kukhonzetsa ana kupita ku sukulu za sekondale za dziko, m'malo mwake zakwanitsa kukhonzetsa za pa boma

Iwo ati gwero la izi ndi kusowa chidwi kwa makolo kulimbikitsa ana awo maphunziro, adindo owoona maphunziro ndi eni ophunzira zomwe mkulu wa nthambi yomenyera ufulu wa za maphunziro pa boma m'boma la Chikwawa la District Education Network (DEN) , a Francis Storey agwirizana ndi mabungwewa

Wolemba : Jaison Chiyembekezo

Nyungwe FM NewsMalawi’s Second Vice President Enock Kanzingeni Chihana has left King Shaka International Airport in Durb...
18/08/2026

Nyungwe FM News

Malawi’s Second Vice President Enock Kanzingeni Chihana has left King Shaka International Airport in Durban for OR Tambo International Airport in Johannesburg after leading Malawi’s delegation to the 46th SADC Heads of State and Government Summit.

Chihana, who was delegated by President Arthur Peter Mutharika, was seen off by Malawi’s High Commissioner to South Africa Stella Ndau and KwaZulu-Natal MEC for Social Development Mbali Shinga, among others.

He inspected a Guard of Honour mounted by the South African Army before departing Durban. Chihana is expected to connect to Bakili Muluzi International Airport on Thursday, August 20, 2026.

The delegation included Foreign Affairs and International Cooperation Minister George Chaponda, Defence Minister Feston Kaupa, Principal Secretary for Defence Gift Dulla and Head of Communication in the Second Vice President’s Office Kelvin Mposa Tchali, among others.

Author: Robert Benson Malenga

Nyungwe FM

the voice of the valley

Hakainde Hichilema has been officially declared President elect!Congratulations Bally 👏
18/08/2026

Hakainde Hichilema has been officially declared President elect!

Congratulations Bally 👏

16/08/2026

45 minutes gone

MALAWI 0- CAMEROON 3

  FM Zamasewero Timu ya mpira wamiyendo koma osewera ake ali azimayi ya dziko la Malawi yafika ndime yomaliza ya CAF Wom...
12/08/2026

FM Zamasewero

Timu ya mpira wamiyendo koma osewera ake ali azimayi ya dziko la Malawi yafika ndime yomaliza ya CAF Women’s Africa Cup of Nations kutsatira chipambano chawo ndi Algeria 3-1.

Scorchers yapeza chipambanochi ndi zigoli kuchokera kwa Tabitha Chawinga, yemwe wagoletsa zigoli ziwiri, ndi chimodzi cha Temwa Chawinga.

Scorchers tsopano ikuyembekezera kukumana ndi Morocco, kapena Cameroon omwe akuyembekezereka kusewera posachedwapa.

Wolemba Prosper Phiri

  FM
08/08/2026

FM

  FM Nkhani Abale kuphatikiza wena akufuna kwabwino asonkhana ku Chileka mmudzi wa M'banda munzinda wa Blantyre  komwe n...
08/08/2026

FM Nkhani

Abale kuphatikiza wena akufuna kwabwino asonkhana ku Chileka mmudzi wa M'banda munzinda wa Blantyre komwe ndikumudzi kwawo kwa Mkulu wa Nyumba yaboma yowulutsila mawu mdziko muno ya MBC, Brian Banda, komwe akulilira Maliro.

a Banda amwalira loweluka atadwala kwa kanthawi kochepa pa Chipatala cha Mwayiwathu.

Mukugwira kwawo kwa ntchito a Banda, anagwilapo ku Capital Radio, Times Group ndipo amwalira akugwila ngati Mkulu wa MBC.

Thupi la Brian Banda, likuyembekezeleka kulowa m’manda Lolemba, pa 10 August 2026.

Wolemba Prosper Phiri
Zithunzi Mercy Zamawa

  FM Nkhani Mtsogoleri wadziko lino Peter Muthalika wati ndokhudzika ndi imfa ya Mkulu wa Nyumba yaboma yowulutsila mawu...
08/08/2026

FM Nkhani

Mtsogoleri wadziko lino Peter Muthalika wati ndokhudzika ndi imfa ya Mkulu wa Nyumba yaboma yowulutsila mawu ya MBC, Brian Banda.

Muchikalata Chomwe mtsogoleriyu watulutsa posachedwa p***a chati iwo komaso Mayi wadziko lino Getrude Muthalika, ndokhudzika ndi imfayi ponena kuti a Banda anali Mtolankhani yemwe amagwila ntchito yake mwa ukadaulo yemwe wakhala akuthandiza Boma mmagawo osiyanasiyana.

Mtsogoleri wadziko linoyu wapepesa akubania, amzake ndi ena onse okhudzidwa kuti Mulungu awafungate munthawi yowawitsayi.

Wolemba Prosper Phiri

  Thupi la Mkulu wa Nyumba yaboma yowulutsila mawu ya MBC, Brian Banda, likuyembekezeleka kulowa m’manda Lolemba, pa 10 ...
08/08/2026



Thupi la Mkulu wa Nyumba yaboma yowulutsila mawu ya MBC, Brian Banda, likuyembekezeleka kulowa m’manda Lolemba, pa 10 August 2026, mmudzi wa M’banda ku Chileka munzinda wa Blantyre.

Source: Times Group

Address

Chikwawa

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Nyungwe Community Radio posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Shortcuts

Share