Asokonezi

Asokonezi Person who likes kucheza

02/11/2025

BLANTYRE🇲🇼

*WOLEMBA MR PRESIDEÑT*

*RIP CHITIMBE*

*Kaswiri odziwika bwino poimba nyimba za chimalawi Collins Chitimbe watisiya usiku wathawa*.

Malingana ndi akubanja komanso ma report omwe Mpira Sports yapeza ndikulanda akuti a Collins Chitimbe yemwe ndi brother wawo wa Innocent Chitimbe yemwenso ndi kaswiri oimba komanso kulengezera mpira pa wailesi ija ya Mtiveni Radio akuti brother wawo wangodwala kwa masiku ochepa atapezeka ndi nthenda ija ya sugar.

Collins Chitimbe atisiya usiku wathawa kuchipatala chachikulu cha malamuro ku makwasa m'boma la Thyolo.

Mauthenga ochuluka akupelekedwa opeleka ulemu osiliza kwamalemuwa.Ife a mpira sports tikupepesa akubanja munyengo yowawitsayi.

02/11/2025

Masewero apakati pa Mighty Wanderers ndi Nyasa Big Bullets awasutha n’kuwayika pa 3:00 pm.

WAGANYU Zikhulupiliro zachuluka pomwe ma team a Wanderers ndi Bullets alowa mu stadium pomwe anyamata omwe avala makaka ...
02/11/2025

WAGANYU



Zikhulupiliro zachuluka pomwe ma team a Wanderers ndi Bullets alowa mu stadium pomwe anyamata omwe avala makaka a team ya Bullets amathila bus ya wanderers zinthu zoone ngat madzi zomwe ena akut ndimikodzo komanso ena kuipaka mafuta ankhumba.
Izii sizinasangalase ochemelela team ya mighty Wanderers omwe anayamba kukangana ndi anzawowa ndipo zinatengela apolice kukhazikisa bata pamalowa.

Pomwe bus ya Bullets imalowa masapota awo anaikumdikila mpaka kukafika pomwe ma player amasikila.

Click to Watch & Join

02/11/2025

Happy birthday to President of Tanzania for elected as a president kachikena. Thanks umatha,anthu anatamanga🏃😅

01/11/2025

Akuti Mnyamata wina amumanga kamba kopha Buffalo🙄,ine ndimangoti Buffalo ndi oimba basitu 🙌
Koma umbuli undipha

30/10/2025





is almighty

*TANZANIA*🇹🇿‼️✊Pamene nzika za dziko la Tanzania zikuponya voti pachisankho chachikulu lero m'dzikolo, mtsogoleri wa dzi...
30/10/2025

*TANZANIA*

🇹🇿‼️✊Pamene nzika za dziko la Tanzania zikuponya voti pachisankho chachikulu lero m'dzikolo, mtsogoleri wa dziko lino Professor Arthur Peter Mutharika wati ali ndi chikhulupiliro kuti nzika ziponya voti mwamtendere.

Professor Mutharika wanena izi mukalata yomwe watulutsa pa 28 October 2025, ngati mkulu woona za ndale, nkhondo ndi chitetezo ku bungwe la SADC.

"SADC ndiyozipereka kuthandiza Tanzania patsiku lachisankho, chikatha chisankho. Kudzera ku nthambi ya SEOM, SADC iwonetsesa zisankho za mtendere ndizokhulupirika", kalatayi yatero.

Padakali pano a Mutharika apempha nzika za Tanzania zomwe zinalembetsa kutuluka mwaunyinji ndikukaponya voti pamene andale awapempha kulemekeza zomwe nzikazo zisankhe.

Pa udindo wa mtsogoleri wa dziko la Tanzania pa chisankhochi, opikisana alipo 17 omwe ndikuphatikizirapo mtsogoleri wa dzikolo Samia Suluhu Hassan wachipani cha Chama Cha Mapinduzi (CCM).

Pogwiritsa ntchito udindo wawo a Mutharika anatuma sipika wakale wa nyumba ya malamulo Richard Msowoya kukayendera zisankhozi mdzikolo.

*🔺️🔺️🔺️🔺️J.J🔺️🔺️🔺️🔺️🔹🔹🔹🔹🔹🔹🔹🔹🔹*
*🔹️🔹POMPOPOMPO🔹*
*⚡⚡📝24HRS⚡⚡*
*⚡⚡📝NEWS⚡⚡*
*⚡⚡📝UPDATE⚡⚡*
*FOLLOW US FOR MORE NEWS*🇲🇼🇲🇼🇲🇼➖➖➖➖➖➖➖➖➖➖➖➖➖

27/10/2025

27/10/2025

24/10/2025

Hahahahaha life nintchonctho🤣🤣🙌

Achikulire akuyendera MG 3... Dereku akuti ndi Pango, ayi fenkis 🤣🙌
24/10/2025

Achikulire akuyendera MG 3... Dereku akuti ndi Pango, ayi fenkis 🤣🙌

24/10/2025

Mlakatuli wathu waku Malawi MERCY MBETA. Video ndie ilipo imenei yangotuluka masiku womwewa. gulani yanu lero pa mtengo wa K2000 yokha basi�

Address

Kasungu

Telephone

+265991099379

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Asokonezi posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Asokonezi:

Share

Category