09/08/2026
Anthu okwiya komanso a chibale a malemu Olipa Aluveta Nanthambwe akumba manda pa nkhonde la nyumba ya Daniel Zimpita yemwe akumuganizira kuti wapha mayiyo.
Malinga ndi Sitima apolisi ndi a chipatala apempha mafumu ndi adzukulu kuti akakumbe mandawo malo ena.
Pomwe izi zikuchitika Zimpita akusungidwa ndi Polisi ndipo akawonekela ku bwalo la milandu.
Wolemba:Mathews Benard