06/07/2022
Ekisodo 20:5 May a Mulungu auk*ti( ndidzalanga ana chifukwa cha Atate awo). Okondedwa nkhani imene Mulungu amamuwuza Mose ndi nkhani imemene anthu timaimva osati mozama kwambiri ayi koma ndi yozama kwambiri.
CHIFUKWA
Izi zik*tanthauza k*ti Ku Chiyuda kwambiri akamati anthu amanena amuna okha ,Okondedwa mukamawelenga pa Ekisodo 14 mupeza k*t amati anthu amene amachoka Ku Aigipto anali anthu 600000 amuna okha okha osaphatikiza akazi
Tamverani amene ndife Manolo timayenela tikhale anthu obadwanso kwatsopano chifukwa Mulungu kudutsila mwaife akupeleka anthu ena amene akhoza kudzatumikilanso dzina la Mulungu. Izi zik*tanthauza k*ti mwana wanu akamwalira inuyo musadatembenuke mtima mwayo akapita Ku chionongeko ,tikunena ana amene asadafike popanga chiganizo okha .Enanso
amati adali oyembekezela pati paja ndikuchoka mbewu imeneyi yukapita kugahena ngati makolo
sadabadwenso kwa tsopano.Ena amati tipemphele chifukwa cha k*ti mwana wanga adafa ndisadatembenuke mtima izi sizoona ayi May a Mulungu amati kwaikika kwa Munthu kufa kamodzi kenako chiweruzilo. Okondedwa tiyeni tikhale ochenjera,tibadwenso kwa tsopano tikapulumuke .Ambuye akudalitseni
sadabadwenso kwa tsop