Thokozani Namuku

Thokozani Namuku Hardworker from outskirts of Malawi ,chizukulu Cha amayi Nini

03/02/2025

Mphenzi updates

A Bonface Ofesi sazaka 25 afa ataombedwa ndi mphezi lero m'boma la Ntchisi.

M'neneri pa polisi ya Ntchisi a Salomy Zgambo, ati ngoziyi ya chitika pa mudzi otchedwa Kaphatiye m'bomalo.

Iye wati wati pa nthawiyo, malemuwa amalima m'munda mwao koma mwadzidzi mvula ya mphamvu inayamba komanso kuti pa nthawi yomwe amafuna adzithawa mpheziyo inawamenya ndikuwatentheranso zovala zonse.

Pakadali pano, ofalitsa nkhani pa chipatala chachikulu cha m'bomalo a Frank Kaphaso ati a Bonface afa kamba koti adatenthedwa kwambiri ndi moto wa mpheziyo.

A Bonface, amkachokera pa mudzi wa chimwankhuku ku dera la mfumu yaikulu Malenga m'bomalo.

(by Thokozani Namuku-Ntchisi:02/03/2025)

https://www.fb.com/l/6lp1kJRRRFollow this link to get more original stories which is for fun, education and entertainmen...
03/02/2025

https://www.fb.com/l/6lp1kJRRR

Follow this link to get more original stories which is for fun, education and entertainment

This version of Facebook uses less data and works in all network conditions.

03/02/2025

news

Police in Thyolo have arrested a 44-year-old man, Symon Mitende, on suspicion that he is linked to the death of the Malawi Congress Party (MCP) district official, Zinthenga Banda last week.

South East Police Region spokesperson, Edward Kabango, has confirmed the arrest to Zodiak today, but declined to divulge more on his connection to the murder.

Kabango says they are still on the ground to effect more arrests.

Mitende hails from Mzuwa village in the area of senior chief Nchilamwela in the district.

(by Thokozani Namuku-Thyolo:02/03/25)

page

16_september tikusintha boma ndipo boma lapita kwa Arthur Peter Mutharika
03/02/2025

16_september tikusintha boma ndipo boma lapita kwa Arthur Peter Mutharika

03/02/2025

I'm a hardworking man but in wrong generation and country. Please God sent me anywhere but not in Africa

03/02/2025

Madalitso amachokera kwa Mulungu osati asing'anga

03/02/2025

Patrick Mwaungulu and Lanjesi Nkhoma are they safe in DRC?

03/02/2025

Paja Anduna adati tikalipire 2 billion ku Manchester city ndi Arsenal kuti pa jersey yawo azilembapo Vist Malawi nde kaya zili Pati pano?

03/02/2025

Kodi aja amafuna kidney aja idapezeka?

Address

Lilongwe

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Thokozani Namuku posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share