19/04/2024
1 a hebri 2 vs 9 : koma tipenya iye amene anamchepesa pang'ono ndi mngelo ndy Yesu cifukwa ca zowawa zathu .Mulungu walora k*t muduse munyengo cifukwa ca colinga, apa tikumuwona Yesu akucepeswdwa cifukwa ca cholinga ,ine ndikupemphera Mulungu akupambanitsen mu dzina la Yesu christu .Type Amen to receive that grace in Jesus name.