The Beast.

The Beast. News + entertainment

Boma silikucheza bwino.
20/01/2026

Boma silikucheza bwino.

24/12/2025

Bwalo lamilandu lati lipereka chigamulopa pempho la belo, pa nkhani ija ya a Richard chimwendo kudzera pa makina a email.

Mkanemamu ndi ma lawyer ambalionse ziwiri a Dziko ndi andianthu Malunda komaso a Khwima Mchizi.

24/12/2025



Woyimira a Richard Chimwendo Banda pa milandu a George Jivason Kadzipatike apempha bwalo la milandu kuti lipereke belo kwa Chimwendo, chifukwa a Chimwendowa ndi phungu wa nyumba ya malamulo komanso ali udindo osamala anthu ena ndiso ntchito zamalonda zosiyanasiyana ndipo ati a Chimwendo sangathawe.

Iwo atiso a Chimwendo adakadzipereka okha ku polisi atanva kuti apolisiwa akuwasakasaka, zomwe ati zikutsindika chilungamo ndi kukhulupirika kwawo pa nkhaniyi.

A Kadzipatike alonjezaso kuti a Chimwendo sasokoneza kafukufuku kapena umboni uliwose wa nkhaniyi ngati bwaloli lipereka belo lero.

Achimwendo sanawonekereso lero kubwalo lamilanduli.

The Beast.

  Bwalo la milandu mu mzinda wa Lilongwe lero lipitirira kunva pempho la belo pa mlandu wa mlembi m'chipani cha Malawi C...
24/12/2025



Bwalo la milandu mu mzinda wa Lilongwe lero lipitirira kunva pempho la belo pa mlandu wa mlembi m'chipani cha Malawi Congress (MCP) a Richard Chimwendo Banda.

A Chimwendo Banda, adawamanga pa 12 December, 2025, pa mlandu owaganizira kuti adafuna kupha munthu mchaka cha 2021.

19/12/2025

Ambiri atsekera ku ntchito lero, koma ena akunyinyirika, eti basi holiday sakuifunaso.

19/12/2025

A George Jivason Kadzipatike, lawyer wa a Richard Chimwendo Banda, kufotokozapo momwe zinthu ziriri kuchipatala komwe a Chimwendo akulandira thandizo, atangotuluka m'bwalo lamilandu lero.

A Chimwendo Banda akuwazenga mlandu ofuna kupha munthu, omwe akuti adaupalamula mchaka cha 2021.

06/12/2025

Eeeeee genius😁

  M'neneri wa boma a Shandreck Namalomba ati a Malawi azigula thumba la Chimanga lolemera ma kilogram 50 pa mtengo wa 45...
13/11/2025



M'neneri wa boma a Shandreck Namalomba ati a Malawi azigula thumba la Chimanga lolemera ma kilogram 50 pa mtengo wa 45 thousand kwacha posachedwapa.

A Namalomba amayankhapo pa mphekesera yoti m'gwirizano wamalonda a chimanga pakati pa dziko la Malawi ndi Zambia wasokonekera, kamba koti dziko lino sirinapereke ndalama zina za chimanga chomwe dziko lino lagula ku Zambia.

Iwo atiuza kuti mphekeserayo ndibodza lamkunkhuniza, kamba koti chimangacho chiri mu mnjira panopa kubwera mdziko muno.

Iwo atsindika kuti tsopano thumba lachimanga lolemera makirogiramu 50 litsika mtengo mpaka K45,000 chimangachi chikafika.

13/11/2025

2025 Summer Gospel Concert

 Environmental activist Mathwes Malata has implored the Democratic Progressive Party (DPP) administration to consider en...
01/11/2025



Environmental activist Mathwes Malata has implored the Democratic Progressive Party (DPP) administration to consider environmental conservation among its prime concerns if the country is to decisively eradicate the persistent impacts of climate change.

In an interview, Malata regarded the environment as a driver and enabler of the national economy and food security; hence, there is a need to preserve it.

He said the government should commit to enforcing environmental conservation laws, declarations, and policies, stating that this will enable a favorable environment for economic growth and food security.

Additionally, Malata warned that neglecting this issue could lead to economic and development stagnation as well as food challenges emanating from climatic shocks.

GENUINE RECITAL,  ⚠ LONG POSTOn the sidelines of my recent career, I was deployed to a certain location that was geograp...
23/10/2025

GENUINE RECITAL, ⚠ LONG POST

On the sidelines of my recent career, I was deployed to a certain location that was geographically disadvantaged, and I served in a specific position after entering into a short-term agreement with one of the government departments.

It was fieldwork, moving from place to place, creating new moments and acquaintances. The work itself demanded more engagement with citizens, having a dialogue of about 5 to 8 minutes per client.

Then, boom! Two guys showed up looking for a service from me. They loved me so much for my noise and my friendly demeanor towards everyone. Physically, they were brawny, strapping men, and I honestly enjoyed their company as I served them one by one.
However, as a journalist, I started to deeply observe these two men who, at the time, seemed to be enjoying my lies in conversations that suited the environment well. I could tell that those sweet lies I kept telling them brought relief and put smiles on their faces, as they couldn't believe that someone as strange as I was kept shaking hands, calling them "cheif, madala, bro," and having such long conversations in that manner.

Then something pushed me to explore the best immediate way I could become a confidante to the two muscular boys while aiming to extract the burden I was suspicious of throughout our conversation. Yes, I looked young, and indeed I was.

I brought up a monetary subject, discussing investments while carefully ensuring that everything aligns with the village setup. Thus, when I realized that I would advance my agenda, one guy started spouting unsalable words: "Amwene, mumadziwa, inuyotu muli-bohboh, mukudya zindalama zabwino, ifeyo ayi-tu." At that moment, I realized that the two guys were surviving in pain. He continued, "Timagwira ntchito pa farm inayake kumtundaku, koma eeee amwene, ng'ombe ikutiko, sifeyo man mmmmhu!" Before he could finish, the other guy gasped for air; I knew that something heated would be said.

"Amwene abwana athu ndioyipa kwambiri, tikungogwirira mavuto nanga titani." I asked if their boss was a citizen. One guy responded, "Amakhala ku 47 uku wakomkuno tee, amabwera kumatipeza chonchimu, ndiye amatikalipira ngati ana." Then I took time asking about their working conditions and environment itself. " iiiih Chief, Timamwa madzi pa chithaphwitu penapake, mjigo kulibe uku, pomwepo timamwetsaposo ng'ombe za ku Farm-ku, kuliso nkhumba, nkhuku, mbuzi ndi a bakha tose timapita kumweko."

I was shocked. I realized that the two fathers couldn't just be heartbroken like that by exaggerating a situation. The journalism aspect started to convince me that I could do something. Fortunately, their map to the farm seemed to be a stone's throw from the place we were. I asked them if we could go together and witness the situation the next day afternoon. They, without thinking twice, nodded in agreement to my request, "tipite amwene mukaone, inuyotu sumungamwe, olo kusambapo m'manja sizingateke muonekeramu?"

It's too long; to be continued.

NOTE: This is a genuine recital, logically presented, and attached to the narrative are real pictures of subjects.

Khonsolo yamzinda wa Lilongwe yati tsopano iyamba kulimbikitsa lamulo lokakamiza eni galimoto zonse zonyamula katundu ok...
27/08/2025

Khonsolo yamzinda wa Lilongwe yati tsopano iyamba kulimbikitsa lamulo lokakamiza eni galimoto zonse zonyamula katundu okwana kapena kuposera matani khumi ndi asanu (15), kutenga chilolezo cholowera mu mzipata za m'zindawu kuchokera ku khonsoloyi asanalowe mu mzindawu nthawi ya usiku.

Mumkalata yomwe khosoloyi yatulutsa, izitu ndi molingana ndi mphamvu zomwe khonsoloyi ili nazo zapansewu zomwe cholinga chake ndikupereka chitetezo mu mzindawu, kwa oyendetsa galimoto.

Eni galimotozi ati akuyenera kumatenga chilolezocho masana kapena chakumadzulo ku ofesi zakhonsoloyi a Chidzanja nthawi yoti alowe mu mzindawu isanakwane.

Malinga ndi mkulu wa khonsoloyi Dr. Macloud Kadam'manja Galimoto zonse zomwe zichepsye izi azizilanda ndi kuzitsekera, komanso eni ake azipereka chindapusa mogwirizana ndi malamulo.

Address

Lilongwe

Telephone

+265991113334

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when The Beast. posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share