Uncle Chi Sold It

Uncle Chi Sold It Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from Uncle Chi Sold It, mchinji, Lilongwe.

Ndife andagwira tipatseni malo anuwo tikugulitsileni
Kapena mukufuna kugura phone or laptop kapena chili chosecho mukufuna kugula kapena kugulitsa tipezeni ife tikutandizani pa mtengo wapang'ono

BREAKING NEWSMA NEEDY STUDENTS FEES AYIMVERA FUNGO CHAKA CHINO KU MA UNIVERSITY.Ophunzira a sukulu zaukachenjede ochoker...
21/08/2026

BREAKING NEWS

MA NEEDY STUDENTS FEES AYIMVERA FUNGO CHAKA CHINO KU MA UNIVERSITY.

Ophunzira a sukulu zaukachenjede ochokera m'makomo osaukitsitsa pafupifupi 14,000 akuyenera kudzipezera okha komwe apeze school fees chifukwa boma lawataya paliponse.

Izi ndi malingama ndi bungwe lopeleka ngongole kwa ophunzirawa la Higher Education Student's Loans and Grants Board(HESLGB) lomwe lalengeza lero m'boma la Salima kuti latenga ophunzira okwana 33,254 okha basi mwa ophunzira 46,386 omwe analembera bungweli kupempha ngongole yama phunziro.

Izi zikuchitika boma litakweza school fees m'ma universities a boma ndi 100% kuchoka pa K650,000 kufika pa K1,300,000 pa chaka.

Iziso ndizosemphana ndi zomwe nduna ya zamaphunziro a Bright Msaka anauza mtundu wa a Malawi kuti asadandaule popeza needy student aliyese yemwe anapanga apply loan ku loans board atengedwa pofuna kuti asamve ululu wakukwezedwa kwa school fees.

BOLA CHAKWERA YEMWE UJA, A MALAWI PA 16 SEPTEMBER TINAYAMWA TONDE!!!

BREAKING NEWSHON AIDA MCHENGA,MP WABWELERA KU CHIPANI CHA MCPPhungu wanyumba ya malamulo wa Dowa West constituency yemwe...
09/05/2026

BREAKING NEWS

HON AIDA MCHENGA,MP WABWELERA KU CHIPANI CHA MCP

Phungu wanyumba ya malamulo wa Dowa West constituency yemwe anapamba pa zisankho za chaka chatha ngati phungu woyima payekha (INDEPENDENT),Wolemekezeka AIDA MCHENGA walengeza zobwelera ku chipani cha Malawi Congress Party(MCP).

Iye wati kuyambila lero ndi phungu wachipani cha MCP ndipo wapanga chiganizochi atafusa nzeru kwa anthu akudera lake omwe amutsimikizira kuti iwo ndi anthu achipani cha MCP kotero apitilize kugwira ntchito ndi chipanichi popeza ngodya zake ndi zomwe iwo amakhulupilira.

Kubwelera kwa aphungu omwe anapambana ngati oyima paokha kuchipani cha Malawi Congress Party, ndichitsimikizo chakuti a Malawi ali ndi chikhulupiliro mwa utsogoleri wachipanichi ndi nsanamira zake.

Leading South African opposition figure Julius Malema has called on President Cyril Ramaphosa to resign after the Consti...
08/05/2026

Leading South African opposition figure Julius Malema has called on President Cyril Ramaphosa to resign after the Constitutional Court ruled that parliament had violated the constitution by blocking moves to impeach him in 2022.

TNM mtopora
07/05/2026

TNM mtopora

Dziko la Ghana ladandaula ku bungwe la African Union (AU) za nkhaza zomwe nzika za m’maiko ena a mu Africa, kuphatikizap...
07/05/2026

Dziko la Ghana ladandaula ku bungwe la African Union (AU) za nkhaza zomwe nzika za m’maiko ena a mu Africa, kuphatikizapo a ku Ghana, akukumana nazo ku South Africa.

Nkhaniyi ikutsatira dandaulo lochokera kwa a anthu ena a ku Ghana omwe akukhala komanso kuchita malonda ku South Africa, omwe akuti akuzunzidwa, komanso kuopsezedwa pa nthawi yomwe nzika zina za dziko la South Africa zikuchita zionetsero m’dzikolo.

Dziko la Ghana tsopano likupempha bungwe la AU kuti lilowererepo pofuna kuteteza nzika za m’maiko a mu Africa zomwe zili m’maiko ena a bungweli, komanso kuonetsetsa kuti mkanganowu usafike poyipa.

"We Are Giving Nigerians And Ghana 24 Hours Ultimatum To Leave South Africa, We're Going To Closed Their Shops If They R...
06/05/2026

"We Are Giving Nigerians And Ghana 24 Hours Ultimatum To Leave South Africa, We're Going To Closed Their Shops If They Refused To Leave."– Phakel Declares.

The leader of Operation Dudula, Phakel, revealed that Nigerians and Ghanaians living in South Africa have been given a 24-hour ultimatum to close all their shops and leave the country. According to him, they are marching to Durban and shutting down all shops owned by black foreigners.
Phakel also urged the South African government to begin paying them R1 million monthly, claiming they have no skills, no jobs, and no means of survival.

M’boma la Mchinji, m’mudzi wa Kang’amba, anthu agwidwa tsembwe komanso mantha bambo  Robiam Mikisoni apezeka atamwalira,...
05/05/2026

M’boma la Mchinji, m’mudzi wa Kang’amba, anthu agwidwa tsembwe komanso mantha bambo Robiam Mikisoni apezeka atamwalira, pomwe akuganiziridwa kuti adachita kudzipha.

kafukufuku waonetsa kuti panali kusamvana pakati pa iwo ndi mkazi wawo pa nkhani yogulitsa mbeu, pomwe a Mikisoni amati ankachita zimenezi popanda kufotokozera mkaziyo. Kusamvanaku kunakula mpaka mkaziyo kuchoka panyumba n’kupita kukakhala kwa makolo ake masabata awiri apitawa.

Koma mkaziyo atabwerera kunyumba m’mawa wa lero, anapeza mwamuna wake atamwalira.

Pakali pano apolisi akufufuza kuti apeze chimwe chadzetsa imfa.

Ngati mukukumana ndi mavuto a m’banja kapena maganizo, kufunafuna thandizo kungakhale njira yabwino yothanirana nawo.

ngati mukudziwa kalikose pazomwe zinachitika pangozi yomwe inapha achilima imabani number imeneyo
05/05/2026

ngati mukudziwa kalikose pazomwe zinachitika pangozi yomwe inapha achilima imabani number imeneyo

Address

Mchinji
Lilongwe

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Uncle Chi Sold It posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Shortcuts

Share