Luanar fm

Luanar fm The Voice that Matters - Live on 99.6/99.8 MHz
Your station for agriculture, development, education, innovation & entertainment.

Pali chiyembekezo choti chiwerengelo cha fodya yemwe akukanidwa pansika chitsika potsatira zokambirana zomwe bungwe lomw...
29/04/2026

Pali chiyembekezo choti chiwerengelo cha fodya yemwe akukanidwa pansika chitsika potsatira zokambirana zomwe bungwe lomwe limaona za ulimi wa fodya mdziko muno la To***co Commission (TC) likuchita ndi kampani zogula fodya komanso unduna wa zamalimidwe.

Malingana ndi kalata yomwe bungweli latulutsa, mbali zitatuzi zikhala zikuunikira zomwe zikuchititsa kuti mlingo ochuluka wa fodya udzikanidwa pa nsika ndikupeza mayankho oti akomere mbali zonse.

Ma belo a fodya okwana 95 pa 100 aliwonse akumabwenzedwa pa nsika kamba ka zifukwa zosiyasiyana ndipo izi zakwiyitsa alimi omwe anaopsyeza kuti achita zionetsero kamba ka nkhaniyi. Masiku apitawa, bungweli linakumana ndi ogula komanso alimi a fodya komwe mwa zina anagwirizana zoimitsa lingaliro lochita zionetserozi.

Bungwe la TC lati lidziwitsa alimi afodya za zotsatira za zokambiranazi mawa lachinayi pa 30 April.

Wolemba: Kenneth Luciano

Mgwirizano wa zaka zitatu omwe oimba nyimbo za uzimu, Theresa Phondo anali nawo ndi bank ya Standard tsopano wafika kuma...
23/04/2026

Mgwirizano wa zaka zitatu omwe oimba nyimbo za uzimu, Theresa Phondo anali nawo ndi bank ya Standard tsopano wafika kumapeto.

Polemba pa tsamba lake la mchezo la Facebook, Phondo wati kugwira ntchito ndi bank ya Standard kwakhala chinthu cha mtengo wapatali kwambiri pa ulendo wake wa maimbidwe ndipo kwake ndikuyamika kamba ka chikhulupiliro chomwe bank’yi inali nacho pa iye.

“Ndine othokoza kwambiri pa zomwe bankiyi yandichitira makamaka pondikhulupilira komanso kundikankhira chitsogolo nthawi zonse. Ndigwiritsa ntchito zinthu zomwe ndaphunzira mu nthawi imeneyi pamene ndikupitilira ndi ulendo wanga pa nkhani zoimbaimba,” Phondo walemba motero.

Phondo, yemwe anaimbapo mu band ya Zathu m’mbuyomu, ndi m’modzi mwa akatswiri omwe akuchita bwino kwambiri pa maimbidwe m’dziko muno, ndipo posachedwapa watulutsa nyimbo yotchedwa No Gwede yomwe anthu ambiri akukondwa nayo.

Wolemba: Kenneth Luciano
Chithunzi: Theresa Phondo

Bungwe la Malawi Energy Regulatory Authority (MERA) lachenjeza eni malo omwetsera mafuta kuti adzalandira chilango ngati...
22/04/2026

Bungwe la Malawi Energy Regulatory Authority (MERA) lachenjeza eni malo omwetsera mafuta kuti adzalandira chilango ngati atapezeka akusunga mafuta mwadala pomwe vuto la kusowa kwa mafutawa lakula m'dziko muno.

Izi ndi malingana ndi kalata yomwe bungweli latulutsa lero yomwe yasainidwa ndi yemwe akugwilizira ofesi ya mkulu wa bungweli a Dan Chinthambi.

Kalatayi mwa zina, yati onse omwe apezeke akuchita m’chitidwewu, omwe ndi otsutsana ndi malamulo, adzalandidwa ziphaso zochitira malonda, kulipira ndalama kapena kumangidwa kumene.

Wolemba: Kenneth Luciano

Akatswiri apakanthawi ododa chikopa monga Kinnah Phiri komanso Peterkins Kaira ali nawo pamwambo omwe team ya LUANAR MIT...
19/04/2026

Akatswiri apakanthawi ododa chikopa monga Kinnah Phiri komanso Peterkins Kaira ali nawo pamwambo omwe team ya LUANAR MITUNDU FC ikukhazikitsa jersey yomwe itagwiritse ntchito season ino ya FDH Bank Premiership yomwe ikuyamba pa 25 mwezi uno.

Mwambowu ukuchitikira ku hotela ya Malville Boutique mu nzinda wa Lilongwe ndipo ena mwa omwe afikanso pa mwambowu ndi a Vice Chancellor a sukulu ya ukachenjede ya LUANAR, Professor Emmanuel Kaunda komanso akuluakulu aku unduna wa zamasewero komanso ku bungwe la SULOM.

17/04/2026

LUANAR FM-Nkhani za masewero.

Matimu awiri odziwika bwino m'dziko muno a Mighty Wanderers ndi FCB Nyasa Big Bullets akuyembekezeka kuchotsana chimbenene mu mpikisano wa Charity Shield mawa loweruka pabwalo la zamasewero la Bingu National Stadium mu mzinda wa Lilongwe.🏟️

Manoma ndi Maule akukumana koyamba chaka chino pomwenso kwatsala sabata imodzi kuti ligi yaikulu mdziko muno ya FDH Premiership iyambe.

Masapota amatimu awiriwa ayamba kale kutafunirana mawu m'masamba a mchezo ndi malo ena pazayemwe apambane masewerowa.

Wolemba: Taim Jimmy

Full Time.LUANAR FC 1-1 MITUNDU BAPTIST.Mitundu primary school ground.  FC  Baptist FC
16/04/2026

Full Time.

LUANAR FC 1-1 MITUNDU BAPTIST.
Mitundu primary school ground.
FC
Baptist FC

South African opposition politician Julius Malema has been sentenced to five years in prison after being found guilty of...
16/04/2026

South African opposition politician Julius Malema has been sentenced to five years in prison after being found guilty of the illegal possession of a gun and firing it in public.

Malema's lawyer said he would be appealing against the decision to prevent the leader of the Economic Freedom Fighters from being taken away to prison. The length of the sentence could see the 45-year-old being disqualified as an MP.

Standing in court in a dark suit and red tie, Malema showed little emotion as the magistrate read out the sentence.

Last year, he was convicted of five offences, including the unlawful possession of a firearm and ammunition, discharging it in a public space and reckless endangerment.

The charges related to an incident in 2018 when a video emerged showing Malema using a semi-automatic rifle to fire several shots in the air during his party's fifth anniversary celebrations held in the country's Eastern Cape province.

Source: BBC

The Ministry of Health and Sanitation says Dietitians and Nutritionists should strive for a cordial relationship and foc...
16/04/2026

The Ministry of Health and Sanitation says Dietitians and Nutritionists should strive for a cordial relationship and focus on achieving a common goal to ensure quality service delivery in the country’s hospitals.

Deputy Director in the Ministry, Nitha Nayeja made the remarks on Wednesday in Lilongwe during a stakeholder consultation meeting organized by the Lilongwe University of Agriculture and Natural Resources (LUANAR) which sought to gather input for a Degree of Bachelor of Science in Dietetics (Honors) curriculum.

Nayeja said the two professions are key in the fight against malnutrition and they should work together for the benefit of Malawians.

“Government is committed to support dietitians and nutritionists by among others addressing their work needs. We need these sections to be visible in the health sector and work towards championing dietary diversity to fight chronic malnutrition,” she said.

By Kenneth Luciano
Picture: Nitha Nayeja

16/04/2026

It’s Throwback Thursday!

Today we’re taking a trip down memory lane…

What’s that one moment in your life that made you feel so great, so proud, or simply unforgettable?

Drop your memories in the comments let’s relive those beautiful moments together!

15/04/2026

Kodi mwawapatsa moni amzanu lero?

Perekani moni kwa abale ndi alongo mu programme ya Malonje pa LUANAR FM, 99.6 MHz kuyambira nthawi ya 9 koloko mpaka 10 koloko m'mawa uno.

The show is on! My Top 10 with Isaac on Luanar Fm 99.6 & 99.8 Mhz.What songs are you vibing to this week? Let us know.
14/04/2026

The show is on! My Top 10 with Isaac on Luanar Fm 99.6 & 99.8 Mhz.

What songs are you vibing to this week? Let us know.

MALAWI GVT. RELEASES 2026-27 FARM GATE PRICES The Ministry of Agriculture, Irrigation and Water Development has released...
14/04/2026

MALAWI GVT. RELEASES 2026-27 FARM GATE PRICES

The Ministry of Agriculture, Irrigation and Water Development has released minimum farm gate prices for strategic crops for the 2026 and 2027 season.

According to the press release signed by Secretary for Agriculture and Water Development Erica Maganga, Maize, which is Malawi’ s staple food has been pegged at 900 kwacha per kilogram which means a 50 kilogram of maize will be purchased at 45,000 kwacha.

Soya beans will be purchased at 1,700 kwacha, Paddy rice at 1,500, pure beans 3,000 while shelled groundnuts will be purchased at 3,500 kwacha per kilogram, just to mention a few.

The ministry says these prices are with immediate effect and has so far urged all agro-dealers to buy crop commodities at not less than the prices stipulated by the ministry.

By:Taim Jimmy
FM

Address

219
Lilongwe

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Luanar fm posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share

Category