12/01/2025
Wachiwiri kwa mtsogoleri wachipani cha Democratic Progressive ( DPP) mchigawo chapakati a Alfred Gangata akuyembekezeka kukaonekera kubwalo lamilandu mawa ku Lilongwe komwe akawauze mulandu omwe anapalamula.
Malingana ndi kalata yochokera kubungwe lotolera misonkho la Malawi Revenue Authority, a Gangata anawamanga powaganizira kuti anagwiritsa ntchito kalata zina pamalonda zomwe ndizokaikitsa.
Mmodzi mwa maloya a Gangata a Felix Tambulasi atsimikizira Zodiak Online kuti a Gangata akaonekera kubwalo lamilandu mawa ndipo pambuyo pake akapempha belo.
A Gangata anawamanga Lachisanu ndipo akhala mmanja mwa apolisi mathero a sabata onsewa.
(by Andrew Viano-Lilongwe:01/12/2025)
Royal Majesty Inkosi ya Makhosi M'mbelwa VHis Royal Majesty Ngwenyama Inkosi Ya Makhosi Gomani VHis Majesty King Jigme Khesar Namgyel WangchuckHis Royal Majesty King Zwelibanzi Dalindyebo of AbaThembuFredokissOneAfricaArthur Peter MutharikaDr dalitso kabambe for presidencyDr Dalitso KabambeTimothy MtamboAPPAC - American Pakistani Public Affairs CommitteeHuman Rights WatchUNHCR Southern AfricaMalawi24
The Vice President of the Democratic Progressive Party (DPP) for the central region, Alfred Gangata, is expected to appear in court tomorrow in Lilongwe to face charges related to alleged crimes.
According to a letter from the Malawi Revenue Authority, Gangata was arrested on suspicion of using questionable documents in his business dealings.
One of Gangata’s lawyers, Felix Tambulasi, confirmed that Gangata will appear in court tomorrow, where they plan to apply for bail afterward.
Gangata was arrested on Friday and has been in police custody throughout the weekend.
By Ephraim Mkali Banda