Dalitso kachambo

Dalitso kachambo Success come to those who may wait
And chance never come alone we creat😉

17/01/2025

I'm on Instagram as . Install the app to follow my photos and videos.

0 Followers, 33 Following, 1 Posts - See Instagram photos and videos from Dalitso kachambo ()

17/01/2025



Ambali ya boma alephera kubweretsa mboni pa mlandu omwe gavanala wa DPP mchigawo cha kuvuma yemwenso ndi phungu wa nyumba ya malamulo kudera la pakati pa boma la Machinga a Daud Chikwanje akuyankha.

Izi zachititsa kuti oweruza milandu a Maxwell Boaz aimitse mlanduwu kufikira pa 11 mwezi wa mawa.

Mwa zina a Boaz achotsanso chilango cha belo chomwe a Chikwanje adapatsidwa kuti adzikaonekera ku bwalo la milandu lachisanu lirilonse ndipo mmalo mwake a Chikwanje sadziyenderaso beloyi.

Koma poonekera ku bwaloli a Chikwanje aukana mlandu oyankhula mawu omwe ali ndi kuthekera kodzetsa chisokonezo omwe akuzengedwa.

A Chikwanje adamangidwa mwezi wa September kutsatira kanema wina yemwe anaonetsa iwo akuyankhula pa msonkhano wina m'boma la Machinga.

Wolemba Blessings Tambala.

13/01/2025

🔥🔥🔥🔥🔥🔥

12/01/2025

Incase you missed this Arthur Peter MutharikaDemocratic Progressive Party - DPP PRESSHon. Alfred Gangata - DPP Vice President CentreDPP-DEMOCRATIC PROGRESSIVE PARTYHon Kamlepo Kalua

12/01/2025
12/01/2025

His Royal Majesty Ngwenyama Inkosi Ya Makhosi Gomani VHis Royal Majesty Inkosi ya Makhosi M'mbelwa VDemocratic Progressive Party - DPPArthur Peter Mutharika

12/01/2025

🔥🔥🔥🔥akumuopa munthuyiDPP PRESS

 Wachiwiri kwa mtsogoleri wachipani cha Democratic Progressive ( DPP) mchigawo chapakati a Alfred Gangata akuyembekezeka...
12/01/2025


Wachiwiri kwa mtsogoleri wachipani cha Democratic Progressive ( DPP) mchigawo chapakati a Alfred Gangata akuyembekezeka kukaonekera kubwalo lamilandu mawa ku Lilongwe komwe akawauze mulandu omwe anapalamula.

Malingana ndi kalata yochokera kubungwe lotolera misonkho la Malawi Revenue Authority, a Gangata anawamanga powaganizira kuti anagwiritsa ntchito kalata zina pamalonda zomwe ndizokaikitsa.

Mmodzi mwa maloya a Gangata a Felix Tambulasi atsimikizira Zodiak Online kuti a Gangata akaonekera kubwalo lamilandu mawa ndipo pambuyo pake akapempha belo.

A Gangata anawamanga Lachisanu ndipo akhala mmanja mwa apolisi mathero a sabata onsewa.

(by Andrew Viano-Lilongwe:01/12/2025)

Royal Majesty Inkosi ya Makhosi M'mbelwa VHis Royal Majesty Ngwenyama Inkosi Ya Makhosi Gomani VHis Majesty King Jigme Khesar Namgyel WangchuckHis Royal Majesty King Zwelibanzi Dalindyebo of AbaThembuFredokissOneAfricaArthur Peter MutharikaDr dalitso kabambe for presidencyDr Dalitso KabambeTimothy MtamboAPPAC - American Pakistani Public Affairs CommitteeHuman Rights WatchUNHCR Southern AfricaMalawi24




The Vice President of the Democratic Progressive Party (DPP) for the central region, Alfred Gangata, is expected to appear in court tomorrow in Lilongwe to face charges related to alleged crimes.

According to a letter from the Malawi Revenue Authority, Gangata was arrested on suspicion of using questionable documents in his business dealings.

One of Gangata’s lawyers, Felix Tambulasi, confirmed that Gangata will appear in court tomorrow, where they plan to apply for bail afterward.

Gangata was arrested on Friday and has been in police custody throughout the weekend.

By Ephraim Mkali Banda

11/01/2025

Master KG SA MusicNkosazana DaughterHis Majesty King Jigme Khesar Namgyel WangchuckHis Royal Majesty Ngwenyama Inkosi Ya Makhosi Gomani V His Royal Majesty Inkosi ya Makhosi M'mbelwa VHis Royal Majesty King Zwelibanzi Dalindyebo of AbaThembuFredokissOneAfricaCycling Around AfricaAround The WorldArms Around Africa Foundation - AAAF

Address

Mtagaluka Soweto
Mangochi

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Dalitso kachambo posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share