Daily Bible Verses With Prophet Oswald Chizala

Daily Bible Verses With Prophet Oswald Chizala THIS PAGE IS SPECIFICALLY FOR GOD'S KINGDOM ADVANCEMENT THROUGH BIBLE TEACHINGS
(1)

25/08/2025

Musiyeni Mulungu akhale Mulungu pakuti chochitikacho chachitika.πŸ™

Ngati Mulungu analemba kuti
Mudzakhara pa banja
Mudzapeza ntchito
Mudzayamba business
Mudzabereka mwana

Zidzakwanilitsidwa ngakhare okuponderezani atachuluka

Mulungu amakonda aliyese,

God loves you so much πŸ’―βœ…βœ…πŸ’―βœ…πŸ™

25/08/2025

🌺 Pakuti monga thupi lopanda mzimu lili lakufa, koteronso Chikhulupiliro chopanda ntchito chili chakufa.πŸ™
✝️ Yakobo 2 v26 πŸ“–.

is so good to me πŸ’―πŸ’―βœ…βœ…

Si onse omwe amatiAmbuye Ambuye akalowa mu ufumu wa Mulungu koma iwo ochita chifuniro cha MulunguMateyu 7:21Tikuti si on...
25/08/2025

Si onse omwe amati
Ambuye Ambuye akalowa mu ufumu wa Mulungu koma iwo ochita chifuniro cha Mulungu
Mateyu 7:21

Tikuti si onse omwe amanyakulq Bible ndi azitumiki a Mulungu ebawa atumidwa ndi satana kufuna kusocheletsa osankhidwa ndi Mulungu

Kumasamala tiri mumasiku otsiridza

Hallelujah πŸ™

IYI MWAWERENGA KALE?MIKA 7:5Moyo uno pali anthu ena omwe ngakhale titawa kakamira koma azachokabe pa moyo wathu.Zindikir...
25/08/2025

IYI MWAWERENGA KALE?
MIKA 7:5

Moyo uno pali anthu ena omwe ngakhale titawa kakamira koma azachokabe pa moyo wathu.

Zindikirani ichi pali anthu ena omwe timalumikizana nawo kuti angotitengera kuchipambano chathu osati kukhala nawo moyo onse ndiye phunzirani kuvomeleza anthu ena akamalekana nanu pomwe ena amakhala anthu osafunika pa moyo wathu.

Mulungu amalora kuti apite cholinga asatchinge m'daliso wathu.
Loti mmene analekana ndi Abraham Mulungu anamudalitsa Abraham koposa poyamba, pali anthu ena omwe amatilepheretsa kulandira m'daliso pa moyo wathu chonde aloreni apite ndithu πŸ™πŸ™πŸ™

Hallelujah πŸ™πŸ‘

Talembani kuti satana ndakukana ndine wa Yesu KhristuAchite manyazi pakuti alibe gawo pa moyo wanuHallelujah πŸ™
24/08/2025

Talembani kuti satana ndakukana ndine wa Yesu Khristu

Achite manyazi pakuti alibe gawo pa moyo wanu

Hallelujah πŸ™

Konzekera kulandira mayankho a zija wakhala ukupemphelera zaka zonseziPakuti Mulungu wakonzeka kuyankha mapemphero akoAM...
24/08/2025

Konzekera kulandira mayankho a zija wakhala ukupemphelera zaka zonsezi

Pakuti Mulungu wakonzeka kuyankha mapemphero ako

AMEN

Yesaya : 41 :10-10 10. Tsono usaope, pakuti Ine ndili nawe; usataye mtima chifukwa Ine ndine Mulungu wako. Ndidzakupatsa...
24/08/2025

Yesaya : 41 :10-10
10. Tsono usaope, pakuti Ine ndili nawe; usataye mtima chifukwa Ine ndine Mulungu wako. Ndidzakupatsa mphamvu ndipo ndidzakuthandiza, ndidzakutchinjiriza ndi dzanja langa lamanja logonjetsa.

Zomwe munalephera CHAKA chatha yesaniso chaka Chino.

Zomwe munalephera mwezi wantha yesaniso mwezi Uno.

Zomwe munalephera week yatha yesaniso week yino .

Zomwe munalephera dzulo yesaniso Lero ,ndipo

Zomwe mwalephera ora yathayi yesaniso panopa .Ambuye Ali mbari yanu ndipo sazakusiyani nokha ayi.Osataya mtima siku lina zizayenda.

is so good to me πŸ’―βœ…πŸ’―βœ…

24/08/2025

David needed one stone to silence Goliath, Hannah needed one son to silence Peninah, and this year, may God give u ONE testimony to silence your enemies...πŸ”₯πŸ”₯πŸ”₯πŸ’ƒπŸ’ƒπŸ›‘οΈπŸ™πŸΏ

is so good to me πŸ’―βœ…πŸ’―βœ…

24/08/2025

For a better morning, talk to God fist. πŸ•―οΈβ€β€πŸ”₯⛓️‍πŸ’₯

For a better night, talk to God last.πŸ€—β€β€πŸ”₯πŸ”₯πŸ•―οΈ

For a better life, talk to God everyday. β˜¦οΈπŸ›πŸ«€πŸ€—

is so good to me πŸ’―πŸ’―βœ…βœ…

24/08/2025

Moyo wanu sudzakhala chimodzimodzi ngati mumvera ndikuchita mau a Mulungu
Deuteronomy 28:1-13

AMEN

Ngati mukufuna thandidzo la uzimu kapena pemphero la padera ndi Kumasulira maloto
Tilankhuleni πŸ‘‡

WhatsApp or call
(+265)0992275595

24/08/2025

Abale ndi alongo nthawi yatha tiyeni tilape zenizeni tingadzasale pamkwatulo Yesu Khristu akubwera posachedwa

Nokha mukuona zidzindikiro za kutha kwa nthawi:
Mavalidwe achilendo, mametedwe achilendo, ana osamvera makolo, mavuto a za chuma, njala, mbiri za nkhondo ndi zina zotero
MATEYU 24:1-24

AMEN

NTHAWI YATHA

23/08/2025

Prayer for Protection Against Car Accidents & the Spirit of Untimely Death πŸ™πŸ½πŸ§Žβ€β™€οΈπŸ“–βœοΈπŸ•ŠοΈπŸ€

Heavenly Father,
In the mighty name of Jesus, I thank You for the gift of life today. Lord, I worship You because You are my Shield, my Refuge, and my Deliverer. Your Word says in Psalm 91:11 that You will give Your angels charge over me to keep me in all my ways, and I stand on that promise right now. Father, I give You all the glory because You are my Protector on every road I travel, whether near or far.πŸŒΊπŸ™πŸΏπŸ€²πŸΏβ€οΈβ€οΈπŸŒ·

is so good to me πŸ’―πŸ’―πŸ’―βœ…βœ…

Address

Blantyre

Telephone

+265887096964

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Daily Bible Verses With Prophet Oswald Chizala posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Daily Bible Verses With Prophet Oswald Chizala:

Share