TRUTH MEDIA

TRUTH MEDIA This is the only Official Page of Prophet Oswald Chizala founder and president of Light of Truth International Ministries.
(1)

15/08/2026

MUKALOTA IZI NDIE KUTI MWANYAMULA ZA PAMWAMBA

AMOSI 3:7

By:Prophet Oswald Chizala
15 August, 2026

1.KULOTA UKUYENDETSA GALIMOTO

➡️Munthu woti m'moyo weniweniwu sukwanitsa kuyendetsa galimoto koma M'maloto nkumayendetsa galimoto bwino bwino osaphwanyitsa.

➡️Zimatanthaudza kuti mwa iwe muli utsogoleri womwe udzauyendetsa bwino bwino kwambiri.

➡️Pena zimatanthaudza kuti tsogolo lako liyenda bwino kwambiri.

2.KULOTA UKUPASIDWA NDODO

➡️Zimatanthaudza kuti ndiwe Munthu wa ulamuliro Mwachidule ukhala ndi udindo waukuru pa company, ufumu, utumiki komaso ku mabungwe ndi ku ndale.

➡️Maudindo ake ndi monga VP, president, Senior Chief ndi zina zotero.

3.KULOTA ULI NDI ANTHU APAMWAMBA.

➡️Zimatanthaudza chisomo cha kulumikidzika ndi anthu a pamwamba kwambiri.

➡️Pena zimatanthaudza kuti chomwe chiri mwa anthuwo chirinso mwa iwe.

4.KULOTA UKUPASIDWA MA KEY

➡️Zimatanthaudza kuti wanyamula family yakwanu, wanyamula mtundu wa kwanu, uli ndi ulamuliro pa zachuma koma zinthu zina zofunikira.

➡️Ukwaniritsa zinthu zambiri zikuluzikulu zomwe anthu ambiri maka azibale akukanika kuzikwaniritsa.

OFUNA THANDIDZO NDILANKHULENI PA NUMBER IYI

WHATSAP ONLY NO CALLS
(+265) 992 275 595

HALLELUJAH

14/08/2026

MUKALOTA MALOTO AWA OSALIRA KOMA MUDZASEKELERE KWAMBIRI

Prophet Oswald Chizala
14 August, 2026

1.KULOTA MVULA

➡️Mvula Ndikukamba apa ndi mvula yogwa mwa Bata osati ya mphepo ndi matalala.

➡️Zimatanthaudza madalitso pamoyo wako.

2.KULOTA UKUPASIDWA NTHAWI

➡️Kulota ukupatsidwa nthawi kapena kulota nthawi itakwana 12 O'clock, 7 O'clock, 6 O'clock ndi zina.

➡️Zimatanthaudza kuti nthawi yako yoti udalitsike ubowoledze yakwana.

3.KULOTA ULI NDI MUNTHU WOTI MUNASIYANA KALE KALE

➡️Kulota ukuchedza ndi anthu oti unakhalapo nawo pa ubwezi kapena pa banja kaya ndi anthu oti unaphubzira nawo, unagwirapo nawo ntchito koma panopa simulumikidzana.

➡️Zimatanthaudza kubwezeletsedwa kwa zinthu zomwe zinatayika pamoyo wako bola anthuwo akhale oti siwalingalirako konse.

4.KULOTA ULI PAKATI PA ANTHU OTCHUKA KAPENA APAMWAMBA

➡️Zimatanthaudza chisomo cha kulumikidzika ndi anthu a pamwamba kwambiri.

➡️Pena zimatanthaudza kuti chomwe chiri mwa anthuwo chirinso mwa iwe.

OFUNA THANDIDZO NDILANKHULENI PA NUMBER IYI.

WhatsApp Only osaimba
(+265) 992 275 595

HALLELUJAH🙌🙏

12/08/2026

MUKALOTA IZI NDIE KUTI TSOGOLO LANU NDILAKUFA

Prophet Oswald Chizala

1.KULOTA MUTAFA

➡️Zimatanthaudza kuti tsogolo lako, moyo wako wauzimu ngwakufa.

➡️Chirichonse chomwe ungachite sichidzipita patali.

2.KULOTA ULI KUMANDA

➡️ Zimatanthaudza kuti tsogolo lako zachuma zako ndi zakufa.

➡️Zinthu zako zinaikidwa m'manda ndipo sungapite patali.

3.KULOTA UKUCHEDZA NDI ANTHU AKUFA

➡️ Zimatanthaudza kuti za iwe ndizakufa ndipo kalikonse ka iwe nkakufa.

➡️Ngakhale utalimbikira chotani koma palibe phindu lomwe ungapedze ku thukuta lako.

4.KULOTA UKUPASIDWA NDALAMA NDI MUNTHU WAKUFA

➡️Zimatanthaudza kuti zachuma zako ndizakufa ndipo Ngakhale upedze ndalama zochuruka palibe cha nzeru chomwe ungachite nazo ndalamazo.

5.KULOTA UKUPASIDWA FONI YOWONONGEKA

➡️Zimatanthaudza kufa ndi kusokonekera kwa ma connections komaso zachuma ndi zinthu zina zomwe umadalira pamoyo wako.

SIDE NOTE:
Si Maloto onse omwe amakhala ndi tanthaudzo ena anthu mumalota kamba koti mwaganiza ndi kulingalira kwambiri choncho nkofunikira kukumana ndi Mtumiki amene ali ndi Mphatso yomasulira maloto tikalota maloto.

AMBUYE AKUDALITSENI KWAMBIRI NONSE KAMBA KA NTHAWI YANU

AMEN

11/08/2026

MUKALOTA IZI NDI MZIMU WA IMFA
✍️✍️✍️

BY:Prophet Oswald Chizala
Date:11 August, 2026

1. KULOTA WODWALA ATAKWEDZANA PANJINGA NDI MUNTHU WOTI ANAFA KALE KALE ✍️✍️✍️

➡️ Zimatanthaudza kuti wodwalayo amfa ndithu.

➡️Pamafunika kuima mwamphamvu kwambiri mumapemphero komaso mkusala kudya.

2.KULOTA CONFIN IKUDZUNGULIRA KWANU✍️✍️✍️

➡️Zimatanthaudza kuti mzimu wa imfa ukufunafuna wina wake kwanuko.

➡️Muime mwamphamvu kususana ndi mzimu wa imfa.

3.KULOTA WODWALA AKUDZULA CHINANGWA
✍️✍️✍️

➡️Zimatanthaudza kuti wodwalayo nthendayo apita nayo kumanda.

➡️Muime naye mwamphamvu kwambiri mumapemphero kuphwasula zoipazi.

4.KULOTA MULI KUMAND✍️✍️✍️

➡️Kulota muli kumanda muja zikhalira pamwambo wa maliro.

➡️Zimatanthaudza kuti mizi ya kumeneko kuchitika maliro omwe agwededze anthu ambiri.

➡️Muime mwamphamvu kususana ndi izi popemphera kwambiri chitetedzo cha kuderako.

5.KULOTA MUTAYANIKA UMFA KAMVULUVULU NKUNYAMULA
✍️✍️✍️

➡️Zimatanthaudza imfa koma ya ngozi Mwachidule imfa ya zidzidzidzi.

➡️Wina wake amwalira mosayembekedzera ngati adwale sadwala nthawi yaitali koma kwambiri ndi imfa ya ngozi.

6.KULOTA MUNTHU WOTI ANAMWALIRA AKUKUITANA
✍️✍️✍️

➡️Ngati walota wakufa akukuitana zimatanthaudza kuti mzimu wa imfa ukukusaka.

➡️Wodwala akadzangoti ndimalota akuti aja anamwalira aja akundikodola akundiyitana zadziweni kuti uyuyu ali pafupi kumfa.

➡️Muime mosusana ndi izi kumapemphero amphamvu aja.

AMBUYE AKUDALITSENI KWAMBIRI NONSE KAMBA KA NTHAWI YANU

AMEN

10/08/2026

MUKALOTA IZI NDI MZIMU WA IMFA

10/08/2026

MUKALOTA IZI NDI MZIMU WA IMFA
(MALIRO)

08/08/2026

MALOTO 5 OWOPSA KWAMBIRI PAMOYO WA MUNTHU

07/08/2026

MUKALOTA IZI:
MWASALA PANG'ONO KWAMBIRI KUBOWOLEDZA

06/08/2026

MUKALOTA IZI NDINU MUNTHU WA CHIPAMBANO NDI CHIGONJETSO

05/08/2026

Maloto awonetsera kuti ndinu Munthu wa mwayi komaso Wazisomo

Address

Blantyre

Telephone

+265887096964

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when TRUTH MEDIA posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to TRUTH MEDIA:

Shortcuts

Share