14/05/2026
Mulungu amene anakulitsa malire a Yabesi akulitsenso malire ako leroli.
Mulungu amene anabereketsa nkhalamba Sarah akubereketsemso iweyo leroli
Mulungu amene anamutola Davide k*thengo ndikumukwedza kukhala Mfumu, ak*tolenso iweyo ndikukukwedza.
Mulungu amene anasintha Chigawenga Paulo kukhala Mtumiki wake wa Mphamvu asinthenso azibale ako, Amuna ako, Mkazi wako, Mwana wovuta uja.
Mulungu amene alibe sankho achite ndi moyo wako leroli
Mdzina la Yesu Khristu
AMEN
NGATI MUKUFUNA PEMPHERO LAPADERA KOMASO KUMASULIRA MALOTO KAPENA KULANDIRA YESU KHRISTU KUKHALA MBUYE NDI MPULUMUTSI WA MOYO WANU
TILANKHULENI PA👇
WHATSAP OR CALL
(+265) 992 275 595
HALLELUJAH🙏