Apostle E Kaliya

Apostle E Kaliya Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from Apostle E Kaliya, Digital creator, Mzuzu.

This is where we preach and share the word of God bible says idzani kwa ine nonse olema ndi othodwa ndipo ndizakupumulitsani.If you come to God he will give you everything you pray for

30/04/2026

YEREMIYA 33 V 14.

Mulungu akulonjedza ana ake kuti matsiku akubwela ndipo achita zomwe analonjeza . okondedwa musatope maso anu musayang'ane nkhondo ndi mayesero popedza Mulungu wakomzeka kuchita chatsopa pa moyo wanu ndikukwanilitsa malonjezo ake.Ndipemphero langa kuti Mulungu achite chatsopano chomwe mwakhala mukupemphelera

23/04/2026

Ndikutheka dziko ,abwenzi akuikilani malire kuti nyengo zanu sizingasithe simungapedze banja , ntchito,mpamba , machilitso, mphatso ya mwana, promotion, machilitso.Tamvetsera Natanieli anayakhulanso pa Nazareth kuti palibe chabwino chingwchokere kumeneko koma Yesu mpulumutsi anabadwila kumeneko ,Lero ndunenera chisomo pa moyo waku kuti onse amaona ngati uthera pamenepo Mulungu awakhalitse chete ndikuwachititsa manyazi in the mighty name of Jesus 🤚

Mwalandila chitomzo ,amene mumawadalira anakutayani chifukwa cha nyengo zanu koma tamvetsera mwana wa m'dalitso Mulungu ...
15/04/2026

Mwalandila chitomzo ,amene mumawadalira anakutayani chifukwa cha nyengo zanu koma tamvetsera mwana wa m'dalitso Mulungu lero akuchotsa muchotonzo chimenecho monga anachita ndi Hanna atanyozedwa ndi Penina inafika nthawi Mulungu anaseka pakamwa pa Penina.Ndikunenela zichitikenso pa moyo wako in the mighty name of Jesus Receive it 🤚

518 Followers, 268 Following, 1293 Likes - Watch awesome short videos created by apostleeckaliya

08/04/2026

NUMERI 20 V 11.

Nyengo iliyonse youma pamoyo wako Lero Mulungu aipase madzi ndipo ikhalenso ndi moyo komanso chigembekezo in the mighty name of Jesus 🤚

31/03/2026

Ana am'dalitso tamvetserani chidwi chanu musaike pa nyengo zanu kapena nkhondo zomwe mukudatsamo chifukwa Mulungu alinawe sanakusiye wekha

28/03/2026

GENESIS 37 V 4 & 5

Yosefe abale ake anamuda nampangira chiwembu chifukwa cha maloto ake, tamvetserani mwana wa m'dalitso omwe umati ndi abwenzi akhomza kukupangira choipa upo chifukwa cha maloto ndi ma plan ako omwe wawauza.Samala ndi omwe ukuwauza maloto ako.

24/03/2026

Lero ndufuna kupemphera nawe kuti undende ,maunyolo amene satana anakumanga nawo akusakwatiwa,akusapeza ntchito, promotion,mphatso ya mwana ,machilitso,kusayenda kwa business.Lero Mulungu akumasule in the mighty name of Jesus l decree and declare Receive your deliverance 🤚.If you believe type l Receive it

23/03/2026

Timphumzile kusunga nthawi ndikuyembekezela pa Ambuye ndi ,ambiri timataya madalitso chifukwa chosayembekezela pa Mulungu tikapemphera.Ambuye atithandize

17/03/2026

YESAYA 43 V 2.

Mwana wa m'dalitso tamvetselani Ambuye akulonjedza kuyenda nafe pamadzi,pamoto.Munyengo zako zonse Mulungu ayenda nawe kotero usataye mtima koma Zindikila suli wekha munyengo zako.

14/03/2026

Ambiri tinamangidwa kapena tinavekedwa nkhope za akufa kotero tikuyenda ndi mzimu okanidwa pa business,ntchito,banja,ulimi,sukulu zonse tichita sizitheka chifukwa we have this rejection spirit.Lero ndufuna ndipemphere ndi iwo amene akuziwa kuti akayesera ichi sichitheka kuti Mulungu akumasuleni ndiyakhuleni.

Address

Mzuzu

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Apostle E Kaliya posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share