30/04/2026
YEREMIYA 33 V 14.
Mulungu akulonjedza ana ake kuti matsiku akubwela ndipo achita zomwe analonjeza . okondedwa musatope maso anu musayang'ane nkhondo ndi mayesero popedza Mulungu wakomzeka kuchita chatsopa pa moyo wanu ndikukwanilitsa malonjezo ake.Ndipemphero langa kuti Mulungu achite chatsopano chomwe mwakhala mukupemphelera