Nathenje Broadcasting Network

Nathenje Broadcasting Network Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from Nathenje Broadcasting Network, Radio Station, Nathenje.

KUBWELETSA CHILUNGAMO KU MTUNDU WA ANTHU
Your Trusted Source of Verified News From Lilongwe Rural East
www.nathenjecommunityradio.blogspot.com
WhatsApp Channel: https://whatsapp.com/channel/0029Vb5oa6KKWEKytYDK3D0W

 Mexico yayamba ndikupambana masewera ake oyamba mu 2026 FIFA World Cup pamene yatubula South Africa ndi zigoli ziwiri k...
12/06/2026



Mexico yayamba ndikupambana masewera ake oyamba mu 2026 FIFA World Cup pamene yatubula South Africa ndi zigoli ziwiri kwa duuu (2-0) pamasewero otsegulira mpikisanowu usiku wadzulo Lachinayi.

Julián Quiñones (9’) komanso Raul Jimenez (67’) ndi omwe anakhoma misomali pa Bafana Bafana kuti igonje 2 kwa chilowere pa masewero ochititsa jegunjewa.

Kupatula zigoi, Masewerowa kunaliso ma Red Card ochuluka kuposa zigoli, Sphephelo Sithole (49’) ndi Themba Zwane (79’) a South Africa komanso César Montes wa Mexico anapatsidwa ziphasozi.

Masewerowa anawoneledwa ndi anthu pafupifupi 1.1 Billion padziko lonse lapansi.

  Apolisi ku Ntchisi amanga abambo awiri, a Chikumbutso Kachinaka azaka 31, komanso a Tobias Kudowa azaka 36, powaganizi...
10/06/2026



Apolisi ku Ntchisi amanga abambo awiri, a Chikumbutso Kachinaka azaka 31, komanso a Tobias Kudowa azaka 36, powaganizira kuti adazunza komanso kusunga mokakamiza bambo wina wazaka 53, a Lloyd Banda.

Malingana ndi m'neneri wapolisi m'bomali a Salomy Zgambo, izi zidachitika pa 7 mpaka pa 8 mwezi uno m'mudzi wa Ng'ondora m'bomali.

A Zgambo ati abambo awiriwa adamenya a Banda asawamangilire komanso kuwasungu mu nkhola la mbuzi.

Iye wati apolisi adachita machawi kukapulumutsa bamboyu atatsinidwa khutu ndi anthu ena akufuna kwabwino.

Pakadali pano wolakwiridwayu akulandira thandizo lamankhwala pa chipatala chaboma cha Ntchisi ndipo ati akupeza bwino.

Wolemba Dismas Puluputu

 Bwalo la milandu la Chikwawa Magistrate lalamula bambo Francis Kagome kuti alipire chindapusa cha ndalama zokwana K700,...
10/06/2026



Bwalo la milandu la Chikwawa Magistrate lalamula bambo Francis Kagome kuti alipire chindapusa cha ndalama zokwana K700,000 atapezeka olakwa pa milandu iwiri yotsegula chipatala popanda chilolezo komanso kukhala ndi mankhwala opanda zikalata zovomerezeka.

Kagome anamangidwa pa 29 May 2026 ku Maperera, East Bank, apolisi atalandira uthenga kuchokera kwa anthu akufuna kwa bwino kuti amasunga mankhwala mosaloledwa, ndipo atafunsidwa, iye anavomera.

Popereka chigamulochi, woweruza Annie Chikhadzula ananena kuti kutsegula chipatala popanda chilolezo kumaika miyoyo ya anthu pachiwopsezo.

Choncho, analamula oimbidwa mlanduyo kulipira K700,000 kapena kukakhala ku ndende kwa miyezi 24.

Ndipo pakadali pano Kagome walipira kale chindapusacho.

Wolemba Redson Dani - Chikwawa

 Nduna yoona zaubale wadziko la Iran ndi mayiko ena a Abbas Araghchi yachenjeza asilikali am'mayiko achizungu komanso Is...
10/06/2026



Nduna yoona zaubale wadziko la Iran ndi mayiko ena a Abbas Araghchi yachenjeza asilikali am'mayiko achizungu komanso Israel womwe ali m'mayiko oyandikana ndi dzikoli kuti achoke m'maderawa.

Ndunayi yayankhula izi poyankhapo pazomwe mtsogoleri wadzilo la America a Donald Trump ananena kuti dziko la Iran lagwetsa imodzi mwa ndege yao yamtundu wa helicopter yomwe yimayendayenda pampito wotchedwa "Strait of Hormuz" womwe dziko la Iran lidatseka.

Ndunayi yati kupezeka kwa asilikaliwa kukubweretsa mantha pachitetezo cha dziko lake.

Pakadali pano dzikoli lidaponyaso mabomba m'mayiko a Bahrain, Kuwait komanso Jordan, m'madera womwe muli asilikali adziko la USA.

Wolemba Dismas Puluputu

  Mary Chilima, widow of the late Vice President Dr. Saulos Klaus Chilima, says the grief from the June 10, 2024 plane c...
10/06/2026



Mary Chilima, widow of the late Vice President Dr. Saulos Klaus Chilima, says the grief from the June 10, 2024 plane crash remains deep two years on.

In a tribute marking the second anniversary, Mrs. Chilima reflected on life without her husband and the eight others who died when their military aircraft went down in Chikangawa Forest, Mzimba District.

“It is now two years my love. Two years without your love, two years without your friendship, two years without your protection and care.

Nthawi ikupita, koma chisoni chidakali chakuya. Everyday without you is hard my love,” she said.

Despite the pain, Mrs. Chilima expressed faith and hope, praying that the souls of all nine victims rest in peace and that “we will meet again in the future.”

Dr. Chilima, 51, was Malawi’s Vice President at the time of his death. He died alongside eight other passengers and crew members, including former First Lady Shanil Dzimbiri.

The crash shocked the nation and remains one of Malawi’s deadliest aviation tragedies.

Reported by Dismas Puluputu

 Netball Association of Malawi has announced the final 16-player squad set to fly Malawi’s flag at the 2026 Commonwealth...
03/06/2026



Netball Association of Malawi has announced the final 16-player squad set to fly Malawi’s flag at the 2026 Commonwealth Games in Scotland.

Coaches picked this team believing they’ve got what it takes to represent the nation. Games run from July 23 to August 2, 2026.

Here’s the Queens squad:

Shooters
Mwai Kumwenda, Ethel Ng'ambi, Florence Jeke, Nancy Mwaulambo, Stella Matelezi, Tendai Masamba

Mid-Court
Takondwa Lwazi, Melia Soko, Thandi Galeta, Mphatso Banda, Beatrice Kumwenda

Defence
Martha Dambo, Aisha Gama, Shabel Bengo, Ruth Chimzimu, Sophilet Banda

Backroom Staff
Head Coach: Debbie Fuller
Assistant: Peace Chawinga
Strength & Conditioning: Beatrice Mpinganjira
Physio: Thomas Banda
Team Manager: Zikubwerera Washon

Report: Dismas Puluputu

03/06/2026

Big shout out to my newest top fans! Chinganji Mwinikuda Blackman Elemiah, David Greciam Kalima, Asher Gee Banda, Aleenahphy Jonacee, Modester Mhango, Rochit Singh Nkhuli, Bon Davie

  The Malawi Police Service has introduced new charges for the provision of police officers on private assignments.Accor...
03/06/2026



The Malawi Police Service has introduced new charges for the provision of police officers on private assignments.

According to a letter signed by Commissioner Evalista Mvula Chisale, the cost of hiring one police officer for a private duty has been set at MK70,000 per day, with clients also required to pay an additional service fee of MK10,000 per day.

The circular has been distributed to all regional police commissioners, who have been directed to ensure the revised rates are implemented and adhered to.

Reported by Rashid Mtumbati-Mwanza

 Boma lapempha Ochita malonda komaso anthu ena okhudzidwa ndi nkhani za chuma kuti agwilane manja ndicholinga chofuna ku...
03/06/2026



Boma lapempha Ochita malonda komaso anthu ena okhudzidwa ndi nkhani za chuma kuti agwilane manja ndicholinga chofuna kukweza Chuma cha dziko lino.

Izitu ayakhula ndi a Josephy Mwanamveka omwe ndi nduna yaza Chuma pamsonkhano okambirana momwe dziko lino lingachitire kuti chuma chake chiyambeso kuyenda bwino.

Msonkhano-wu wachitikira ku Bingu International Convention Centre ndipo unabweretsa pamodzi akulu akulu aboma, ochita zamalonda, akatswiri akafukufuku komaso maphunziro ndi ena ambiri.

a Mwanamveka anati msonkhano-wu linali zenera kuti onse okhudzidwa apereke mfundo zawo kuti chuma chadziko lino chayambeso kuyenda ngati kale.

Address

Nathenje

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Nathenje Broadcasting Network posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share

Category