NDIX VIEWS Magazine

NDIX VIEWS Magazine Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from NDIX VIEWS Magazine, Magazine, Ndirande.

23/08/2025

Don't follow us we will miss lead you

Try n See

23/08/2025

Ku Ndirande (zambia) kuli Bar ina yotchulidwa kuti Pa a M***a
Ndipo pa Malowa pa matchuka
Ndi Atsikana Oyendayenda(Mahule)
Omwe amapakulitsa Binzi pa Mitengo Yabwino(Ndirande yonse)

Ndipo ndi Mk500 yokha M***a kusangalala kwabasi

20/08/2025
Phiri la Zomba limakopa anthu ochuluka kuposa la Mulanje, anthu ambiri takwera phiri la Zomba than la Mulanje, pali chif...
20/08/2025

Phiri la Zomba limakopa anthu ochuluka kuposa la Mulanje, anthu ambiri takwera phiri la Zomba than la Mulanje, pali chifukwa, azungu anayika msewu okwera mpaka pa phiri, anamanga pamene paja Hotel, anapanga ndithu ma investment. Izizi pa phiri la Mulanje palibe.

Tanzania yamanga longest bridge, Magufuli Bridge, 3.2 kilometres pa Nyanja ya Victoria, project yomwe ikuyembekedzera kubweretsa ma millions of dollars kudzera ku alendo ochuluka omwe adzibwera kudzayenda pa bridge imeneyi.

China inamanga misewu mmapiri awo opatsa chidwi zomwe zimapangitsa anthu ochuluka kukhala ndi chidwi chopita ku China kuti akakwere mmapiri amenewa.

Phiri la Mulanje alone liri ndi kuthekera kobweretsa ndalama zochuluka koma timange misewu kukafika pa sapwita kuti anthu azitha kupanga hike mosavuta. Kwa omwe sangakwanitse tiyike ma cable cars oti azikwanitsa kuyendetsa anthu in all areas of interest kaya Sapitwa, Dziwe La Nkhalamba ndi malo ena ambiri, osayiwalanso malo abwino odyera komanso ogona nkatikati mwa phiri.

Nyanja yathu palibe sitima zabwino zonyamula anthu. There are cheap yachts zoti titha kukwanitsa kugula zitatu in 5 years. One for southern part of the lake, ina central, ina north. Chigawo chonse cha northern region of the lake chikufunika heavy investment. Chiweta is very beautiful but neglected. Ma park athu akufunika misewu yabwino ndi zinthu zambiri.

Pachifukwa ichi tikuti K500 billion pa chaka izipita kuntchito zotere. Creating jobs and long lasting investments zomwe tidzasiyire the next generations. Ine sindili pano kukupatsani ma handouts, tinagawana, zimenezo a Chakwera, ine ndili pano kuti nditukule Malawi, create jobs and businesses kwa achinyamata, amayi ndi abambo. Nzotheka kutukula Malawi, nzotheka creating jobs and businesses. Lets invest first.







20/08/2025

When S**t Hits the Fan
It has to get Messy

19/08/2025
Dr. Bingu Wa M***arika came to power through UDF, koma atawona vision yawo, anawona kuti ku UDF sangakwanitse kuzikwanir...
18/08/2025

Dr. Bingu Wa M***arika came to power through UDF, koma atawona vision yawo, anawona kuti ku UDF sangakwanitse kuzikwaniritsa and so, he had to go elsewhere where his vision and institution blend with the vision and for Bingu, anayambitsa DPP, yomwe anayipatsa culture yomwe iwowo ankayifuna.

Dr. Saulos Chilima anayambira ndale zawo ku DPP, koma later anawonanso kuti masomphenya maka othetsa katangale, tsankho lamitundu, ma reforms, sizingatheke pansi pa DPP, he moved on to form UTM.

Ine ndinayambira ndale ku DPP, tinayesayesa koma tinawona kuti ayi tisunthe. Sindinangofikira kulowa UTM, ndinayang'ana zipani zambiri, their mission statement, culture and values, ndipo ndinawona strong desire from UTM to end corruption, nepotism, reform government system, bring innovation and develop Malawi, I was convinced UTM is the right place to be.

Ndikunena ichichi ambiri timatsatira zipani mchimbulimbuli, kuwafunsa kuti awa mmawasapota chifukwa chani, munthu wa degree, masters or PhD imene amakanika kuyankha, chomwe angakuwuzeni nkuti ngwa ku Ntchisi, Dowa, Mulanje, Thyolo, Rumphi, Karonga. So, ophunzira ndi osaphunzira osasiyana.

I want to challenge everyone here, politics is life, kuchipatala kulibe mankhwala a TB, ma patient a TB ngati sakulandira mankhwala next thing ndi imfa, imfayo sisankha kuti awa ngakudedza musawaphe, iphani aku Phalombe, tonse tifa. Njala siwona Mchewa kapena Mtumbuka, imapha aliyense chimodzimodzi ilibe tsankho

Tiyambe kuwona ndale in line with our lives komanso dziko. Tikupindula chani, dziko likuyenda bwanji, titsatire chipani chomwe chili nkuthekera kofewetsa miyoyo yathu komanso kutukula dziko lathu.

Amati, you can't get different results by doing same things that failed. Pangani chisankho chopanga join this movement, for the sake of Malawi. Our country is bleeding, anthu akufa muzipatala, 65% ya imfa zathu timafa because of failed health systems. Abale athu ambiri analowa mmanda osati nthawi inakwana, koma tinalephera kuwasamala. UTM i

Ndirande's finest R'n'B artistChrisqo Chnx Ngwira Has a Masterpiece
18/08/2025

Ndirande's finest R'n'B artist
Chrisqo Chnx Ngwira
Has a Masterpiece

Happy BirthdayR I T A A
16/08/2025

Happy Birthday
R I T A A

🙌
31/07/2025

🙌

Best offer on the land
15/08/2024

Best offer on the land

Tune inAnd Don't Miss
09/08/2024

Tune in
And Don't Miss

Address

Ndirande

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when NDIX VIEWS Magazine posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share