Ndungunya crue

Ndungunya crue To be a good person is easy but to accomplish what friends need is not easy.

23/12/2024

Ngat ndizoona kt mumaisunga ngat ziweto please let it zikadye mwina tizale

23/12/2024

Please guys dzikoli lifunika madzi

23/12/2024

How are you guys what can we do to fight the rain shortage

KHIRISIMASI NDI KULAMBIRA MAFANO ONSE OCHITA NAWO CHIKONDWELERO CHA KHIRISIMASI KUMWAMBA SAKALOWA NAWO.Chiphuzitso ichi ...
05/12/2024

KHIRISIMASI NDI KULAMBIRA MAFANO

ONSE OCHITA NAWO CHIKONDWELERO CHA KHIRISIMASI KUMWAMBA SAKALOWA NAWO.

Chiphuzitso ichi chalembedwa pofuna kuzindikilitsa Ankhristu onse kuti KHIRISIMASI ndi chikondwelero cha chikunja choyambitsidwa ndi Satana. Ndipo cholinga cha KHIRISIMASI ndicho kutengera miyoyo yochuluka ku Gahena.

Inde pamene munthu wachita nawo chikondwelero cha KHIRISIMASI amakhala walembetsa dzina lake mu Buku la anthu opita nawo ku Gahena.

📖 Hosea 4:6 "Anthu anga akuonongeka chifukwa cha kusadziwa..."

Chaka ndi chaka tikangofika mwezi December Ankhristu kumakhala kukangalika kugula zakudya, zovala ndi zithu zina kukozekera tsiku la Chikondwelero cha KHIRISIMASI, tsiku lomwe ena amati ndi lobadwa AMBUYE Wanthu YESU KHRISTU.

Mfuso Mkumati KODI NDIZOONA KUTI YESU KHRISTU ANABADWA PA 25 DECEMBER...?

YANKHO: Ndiboza zoti YESU KHRISTU anabadwa pa 25 December Ndipo Baibulo Silinakambeko Za Izi.

Tatiyeni Tisathule Baibulo Kuti Tipezedi Umboni Wakuti YESU KHRISTU Sanabadwe pa KHIRISIMASI Pali Chiwanda China Chomwe Chimalambilidwa Pa Tsiku la KHIRISIMASI.

1** BAIBULO KUYAMBIRA KU GENESIS MPAKA CHIBVUMBULUTSO SILINATCHULE ZA TSIKU(date) LOBADWA YESU KHRISTU

📖 Luka 2:6-7 "Ndipo panali pokhala komweko, masiku ake a KUBALA(KUBEREKA) anakwanira"

"Ndipo iye anabala mwana wake wamamuna woyamba; nankulunga IYE m'nsaru namgoneka modyera ng'ombe, chifukwa kuti anasowa m'nyumba ya alendo"

Baibulo pa nkhani ya kubadwa kwa YESU KHRISTU limangotiuzako za Malo basi kuti YESU anabadwira ku BETELEHEMU mu NKHOLA LA NG'OMBE.

Ndipo mukawerenga Baibulo kuyambira Genesis mpaka Chibvumbulutso simupeza ngakhale vesi imodzi yomwe ikukamba zakuti YESU KHRISTU anabadwa pa 25 December tsiku lotchedwa KHIRISIMASI

Mfuso Nali Kwa Inuyo Bambo/Mayi, "NGATI BAIBULO SILINATCHULE ZAKUTI YESU ANABADWA PA 25 DECEMBER,..

KODI NANGA INUYO ZAKUTI YESU KHRISTU ANABADWA PA 25 DECEMBER MWAZITENGA KUTI...?

Abare kuyambira lero dziwani kuti BODZA NDI CHIDA CHOKHACHO chomwe

There is any problem on this image ?,ⓚⓚⓚⓚⓚⓚⓚⓚⓚⓚⓚⓚ
23/10/2024

There is any problem on this image ?,ⓚⓚⓚⓚⓚⓚⓚⓚⓚⓚⓚⓚ

18/01/2024
MALONDA 4n 8gb Samsung...... Yopanda battery 10pin was serious call me
18/01/2024

MALONDA
4n 8gb Samsung...... Yopanda battery 10pin was serious call me

18/01/2024

CHINTHU CHOOPSA CHICHITIKA POSACHEDWAPA

Posachedwapa kuchitika chinthu chimene chiyimitse mitu mafumu,olemera,osauka,otchuka

Palibe amene amvetsetse chifukwa chichitika mosayembekezera

Chinthu chimenecho chipangitsa anthu kusaka mawu a Mulungu

Chipangitsa anthu kusiya kutsutsa kapena kunyoza mawu a Mulungu

Chipangitsa anthu kusiya kupemphela mwachibwana

Chipangitsa anthu olemera kusiya chuma ndikunthamangira zauzimu

Chipangitsa anthu kumadzipha okha koma osafa

Chinthu chimenecho chipangitsa azimayi kusiya kumvala ma Trauza,kuphoda, kumvala gogoda,kumanga Meshi

Chinthu chimenecho chipangitsa anthu kusiya kumvala makabula,tothina, kumeta mbali mbali, kumvala jeas,kuonera zalaura,mpira, mwano,dzigololo,kuba,kusuta,kupembedza mayi mariy

Dziko lonse likhudzika, dziko lonse likhala pachisoni, dziko lonse likhala pamaliro osantha koma zikhala zopanda tchito

Mateyu 24:40
Pomwepo adzakhala awiri m'munda; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa

Chinthu chimene chikunenedwa apachi ndi MKWATULO

M'bale mkwatulo uchitike posachedwapa kudzatenga oyera mtima lero,mawa, nthawi inayiliyonse

Udzalira mowo wako onse ukadzatsala pa mkwatulo

Untha kuchita chibwana lero ndikumati ndidzalapabe koma ukadzatsala sudzaupeza mwai

Udzauda mowo wako onse sudzaukondaso Mpaka kugahena wamoto

CHISOMO CHIDAKALIPO LERO UNTHA KUKOZA MOYO WAKO, UNTHA KUMULANDILA YESU LERO CHIFUKWA MKWATULO UKAPITA PALIBE KUKHULULUKIDWA LAPANI LAPANI LAPANI ..
Ngati mukufuna mudzimva mawu a Mulungu pangani zinthu ziwiri izi

1.Ndinani mawu awa Mawu a Mulungu Omwe akuoneka poyambilirawo

2.ndipo mukatsekula ndinani kadzanja kamene mukaoneko

Chonde tumizirani azanu komaso m'magrup omwe muli uthengau kuti nawoso awerenge nawo

Muntha kulowa ku group lanthu podina mawu awa
UTHENGA WA MASIKU OTSILIZA GROUP
Ambuye Akudalitseni mochuluka

Wolemba: MOVISH MADISHUH phalombe

Did you know??😍 ```Zokhudza chikondi```   page 2Choyamba ndithokoze kwa inu amene mwandilimbikitsa ndi ma coment anu pa ...
18/01/2024

Did you know??😍

```Zokhudza chikondi``` page 2

Choyamba ndithokoze kwa inu amene mwandilimbikitsa ndi ma coment anu pa facebook ngakhale pa whatsapp kwa amene munapempha kuti ndipitilize ndi gawo limeneli lokhudza chikondi mr zack akwanikitsa tsopano tikhale limodzi.

*Nde dziwani izi....* 👉🏻

1.munthu amene amakukondani inu mu nchoona sangakuloleni kuti inu mupite ingakhale patakhala kuti pali vuto lalikuku motani.

2.ngati ubwenzi wanu watha miyezi inayi muli limodzi dziwani kuti muli mu chikondi chenicheni.

3.89% ya anthu pano pa dziko lapasi amakhala osangalala chifukwa cha chikondi enawo ndi zidakwa komaso ajuga.

4.palibe ubwenzi omwe uli okhulupilika musanamizidwe chifukwa ubwenzi uliwonse umayenera kukwele komaso utsike komano kwa munthu amene amadzupeleka kwa iwe nthawu zonse ameneyo ndiye wachikondi weniweni.

5.choyambilira pa chibwenzi ndi chikondi,kenako ukwati chofunikira kwambiri nkukhala limodzi mpaka kale komano ngati mwapanga ukwati nkumakhala molekana dziwani simunapange ukwati koma ndichionetselo chabe.

6.kukumbatilana (hagging) koposera 20 second kumapangitsa mamuna kapena nkazi kukhala mu chikhulupiro.

7.kumulembera text kapena kumuhalla pa wapp cha 6 mamawa iye nkuyankha chama 12 masana imeneyo ndi juga osati chikondi sakukonda usataye nthawi yako suntha.

8.anthu ambiri amalemba ma text mwachangu kwa munthu amene amamufuna ndikumukonda.

9.kukhala wekha ndikwabwino kumakupangitsani kukhala opanda nkhawa nkusiyana kukhala mu ubwenzi olakwika.

10.nkazi amene amakuuzani kuti amakukondani inu musananene dziwani kuti ali mu nchikondi chenicheni chifukwa kawirikawiri ndi amuna amene amatulutsa mau oti ndimakukonda kwa nkazi.

11.pa 100% iliyose ya amuna ndi 3% yokha ya amuna amene amakhala okhulupilika osawazembela achikondi awo.

12.kukumbatilana kumaonjezera chikondi ngati wachikondi wanu sakwanitsa kukumbatilani (hagging) ngakhale kwa mphindi imodzi sakukondani ndipo amangopanga pofuna kukusangalatsani.translated free Mr zack :Jomw

Address

Ndungunya 1 P. O. Box___phalombe
Phalombe

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Ndungunya crue posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share