13/09/2026
Komatu ngati ziri choncho Malawi anaopsa;
Sad News 💔 ðŸ˜
Ma report akusonyeza kuti Bambo Kalembera omwe akuluakulu ena achipani cha UTM anawagulira njinga ya moto apezeka atafa atasowa kwa masiku awiri.
Akuluakulu ena a UTM motsogozedwa ndi a Felix Njawala anasonkhetsa ndalama kuti mkuluyu aguliridwe njinga ya moto pokondwa ndimomwe amavalira makaka achipanichi akamayendetsa njinga yake ya kapalasa.