Bambo A Prosper

Bambo A Prosper Where the Past Comes Alive

I like chilling with people, am friendly that's why i opened this forum named "Tiziwe Mbiri za Akatswiri" so that i must have a time to chill with people.

BREAKING NEWS 8 Malawians turned into baboons at a police station... Iyiyi ndiye itha kukhala Ina inatu ma guy πŸ˜‚πŸ˜†πŸ€£πŸ™Œ
01/06/2026

BREAKING NEWS
8 Malawians turned into baboons at a police station... Iyiyi ndiye itha kukhala Ina inatu ma guy πŸ˜‚πŸ˜†πŸ€£πŸ™Œ

Zikumveka ngati mtsogoleri wathu Peter Mutharika, watumiza ma bus kuti omwe akufuna kupita ku Malawi atha kumabanduka, s...
01/06/2026

Zikumveka ngati mtsogoleri wathu Peter Mutharika, watumiza ma bus kuti omwe akufuna kupita ku Malawi atha kumabanduka, so try to find out about that side you are staying kuti zikuti bwanji zama bus wa...
Ndikakhala Ine ndiye aah mayazi amwene, anzathu akupita mmakwao pa ndege Ine ndiye ndikayende pa bus? SingachiteπŸ€”πŸ˜

Lelo ndi 1 mwezi wa June mwezi omwe unatiliza kwambiri muchaka cha 2024 pomwe anthu onsewo anamwalila mwezi umodzi...  M...
01/06/2026

Lelo ndi 1 mwezi wa June mwezi omwe unatiliza kwambiri muchaka cha 2024 pomwe anthu onsewo anamwalila mwezi umodzi...

MAY THEIR SOULS CONTINUE RESTING IN PEACE πŸ™πŸ˜°πŸ˜₯😭

30/05/2026

Zimvere mtolo

Amzanga omwe muliku Malawi ndipo mukugubila gubila ku immigration kuti mupeze katunduyi, imvani uthengawu.Ma guy osavuti...
30/05/2026

Amzanga omwe muliku Malawi ndipo mukugubila gubila ku immigration kuti mupeze katunduyi, imvani uthengawu.

Ma guy osavutika ndikubesa ndalama zanu kuti mupangise passport olo kuti passport yanu ituruke mwachangu, inu tangopezani means yoti muzapezeke mulikuno basi...
Munthu ukafika kuno chimangogwira ntchito kwa 30 days yokha ichi, kwinako imakhala wadya mtoliro πŸ˜‚πŸ˜†πŸ€£πŸ™Œ

NOTE: Ndikunama guys osabwera kuno opanda passport muzavutika kwambiri and kuvutika muzayambira mumsewu kuti mufike kuno, ndiye kunoso ndiye worse, uwope akuba, uwope apolisi, penanso umazapezeka kuti wasemphana ndi ntchito yabwino chifukwa choti ulibe passport, so osapanga mistake yobwera kuno opanda passport πŸ‘πŸ‘πŸ‘...

I love you all @ Friends of Bambo A Prosper

Masitolo aanthu obwera mdziko la South Africa makamaka ku KwaZulu-Natal midlands, mwabedwa katundu wochuluka mosamva chi...
30/05/2026

Masitolo aanthu obwera mdziko la South Africa makamaka ku KwaZulu-Natal midlands, mwabedwa katundu wochuluka mosamva chisoni, anthu amdzikolo atakwiya kamba ka chigamulo cha bwalo la milandu lotchedwa Pietermaritzburg High Court.

Bwaloli lidagamula kuti amalonda 38 ochokera mdziko la Ethiopia atsegule masitolo awo ndikuyamba kugulitsa zinthu zomwe sizidakomere nzika za dzikolo ndipo zidakathyola masitolowo.

Anthu obwerawo adauza bwalo la milandu kudzera muchikalata chawo kuti akhala asakugulitsa katundu kopitilira mwezi tsopano akhonsolo atalanda mfungulo za masitolo awo ndipo amayembekezeka kutsegula ma sitolowo lero.

NDIZIKUPASIRANI SATANE SATANE WAKE MMENE ZITHERE...

@ Bambo A Prosper

Malingana ndi kafukufuku wanga ndapeza kuti ngati immigration department izitulutsa ma passport mwachilungamo ndekuti po...
29/05/2026

Malingana ndi kafukufuku wanga
ndapeza kuti ngati immigration department izitulutsa ma passport mwachilungamo ndekuti pofika 2035 ku Malawi kuzakhala azigogo okha okha kuphatikizapo ndi president wawo wa nthawi imeneyo.
Ndiye kuchedwetsa ma passport kuti azituluka zathandiza kwambiri kuti achinyamata ambiri tizilimabe otherwise tikanakhala tiliku maiko akunja monga Israel,USA,South Africa.

Ine yanga chipangireni 2022 paka pano sinatulukebe nde kaya akufuna azandipase ndikazamwalira kuti ndizayendele mxieeew πŸ˜¬πŸ€”

27/05/2026

Big shout out to my newest top fans! Aliq Mmsc Ibwebwe Solobeni, Fatsani David, Violet Viom Masamba, Chiku F Mndala, Morris Phiri

Mnzika za dziko la South Africa zauza a Malawi onse omwe amakhala ku Durban kuti pa sadafike pa 30 June akhale atapita k...
27/05/2026

Mnzika za dziko la South Africa zauza a Malawi onse omwe amakhala ku Durban kuti pa sadafike pa 30 June akhale atapita kwao.

Izi auza a Malawi omwe amakhala ku Durban okha chifukwa ndi kumene kuli gulu lija loumbudza. Komanso tingatengela kumbiri laizi zonkhunzana ndi xenophobic attack zi, Durban always imakhala PA top coz Madera Ena ndi enawa kunachuruka anthu obwera, osiyana mitundu like mazulu, maxhosa, MA kaladi, masuthu ndiena otelo thats why anthuwa amakanika kumvana chimodzi coz siantundu umodzi

Abahambe they sell expired food in our country,  So why are you looting expired food ? πŸ˜„... stupidπŸ˜πŸ€”
26/05/2026

Abahambe they sell expired food in our country, So why are you looting expired food ? πŸ˜„... stupidπŸ˜πŸ€”

Address

Elspark

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Bambo A Prosper posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share