26/03/2025
Yemwe adali membala yaCentral Commitee yachipani cholamulira chaZanu PF bambo Blessed Geza, arengeza leto kuyhi akala akuwulutsa uthenga kuanthu onse nthawi ya8:30 pm. Izi zikutsatira uthenga umene anaulutsa masiku apitawa akudzudzula mtsogoleri wadziko Emerson Mnangagwa, kuthi athlete pansies udindo wawo ngat President. AGeza anakambapo zifukwa zingapo zokudzana nimavutho aza human, njala, kusoweka kwazintchitho, zipatala zopanda mankwala ndikumangidwa kwaanthu omenyera ufu mudziko laZimbabww..zambiri timva paYoutube nthawi ya8:30pm..